< Izajasza 65 >

1 Objawiłem się tym, którzy się o mię nie pytali; znalezionym jest od tych, którzy mię nie szukali; do narodu, który się nie nazywał imieniem mojem. rzekłem: Otom Ja! otom Ja!
“Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu; ndipo ndinalola kuti anthu amene ankandifunafuna kuti andipeze. Kwa mtundu wa anthu umene sunkapempha chithandizo kwa Ine, ndinati, ‘Ine ndili pano, Ine ndili pano.’
2 Rozciągnąłem ręce moje na każdy dzień do ludu upornego, który chodzi drogą nie dobrą za myślami swemi;
Tsiku lonse ndatambasulira manja anga anthu owukira aja, amene amachita zoyipa, natsatira zokhumba zawo.
3 Do ludu, który mię jawnie wzrusza do gniewu, ustawicznie ofiarując w ogrodach, a kadząc na cegłach;
Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa mopanda manyazi. Iwo amapereka nsembe mʼminda ndi kufukiza lubani pa maguwa ansembe a njerwa.
4 Którzy siadają przy grobach, a przy bałwanach swoich nocują; którzy jedzą świnie mięso, i polewkę obrzydłą z naczynia swego.
Amakatandala ku manda ndipo amakachezera usiku wonse kumalo obisika. Amadya nyama ya nkhumba, ndipo mʼmiphika mwawo muli msunzi wa nyama yodetsedwa.
5 Mówiąc: Odstąp precz, nie przystępuj do mnie; bom jest świętobliwszy niżeli ty. Cić są dymem w nozdrzach moich, i ogniem pałającym przez cały dzień.
Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire, chifukwa ungatengere kupatulika kwanga!’ Ukali wanga pa anthu otere uli ngati utsi mphuno zanga, ngati moto umene umayaka tsiku lonse.
6 Oto zapisano to przedemną: Nie zamilczę, ale oddam i odpłacę na łono ich.
“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo; sindidzakhala chete koma ndidzawalanga kwathunthu chifukwa cha machimo awo
7 Nieprawości wasze, także i nieprawości ojców waszych, mówi Pan, którzy kadzili po górach, a na pagórkach hańbili mię; przetoż odmierzę sprawę ich pierwszą na łono ich.
ndi a makolo awo,” akutero Yehova. “Chifukwa anapereka nsembe zopsereza pa mapiri ndi kundinyoza Ine pa zitunda zawo, Ine ndidzawalanga kwathunthu potsata zimene anachita kale.”
8 Tak mówi Pan: Jako gdyby kto znalazł wino w gronie, i rzekłby: Nie psuj go, bo błogosławieństwo jest w niem; tak i Ja uczynię dla sług moich, że ich wszystkich nie wygubię.
Yehova akuti, “Pamene madzi akanapezeka mu phava la mphesa ndipo anthu amati, ‘Musawononge phavalo, popeza madzi ena abwino akanalimobe mʼphavalo,’ Inenso chifukwa cha mtumiki wanga; sindidzawononga onse.
9 Bo wywiodę z Jakóba nasienie, a z Judy dzierżawcę gór moich; i posiędą ją wybrani moi, a słudzy moi tam mieszkać będą.
Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo, ndipo a banja la Yuda adzalandira mapiri anga ngati cholowa chawo. Anthu anga osankhidwa adzalandira zimenezi, ndipo atumiki anga adzakhala kumeneko.
10 A Saron będzie za pastwisko owcom, a dolina Achor za legowisko wołów ludu mojego, którzy mię szukali.
Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa, ndipo chigwa cha Akori chidzakhala malo opumirako ngʼombe kwa anthu anga ondifunafuna Ine.
11 Ale was, którzyście opuścili Pana, którzy zapominacie na górę świętobliwości mojej, którzy gotujecie temu wojsku stół, a którzy oddawacie temu pocztowi mokre ofiary:
“Koma inu amene mumasiya Yehova ndi kuyiwala phiri langa lopatulika, amene munamukonzera Gadi chakudya ndi kuthirira Meni chakumwa,
12 Was, mówię policzę pod miecz, tak, że wy wszyscy do zabicia schylać się będziecie, przeto, żem wołał, a nie ozwaliście mi się, mówiłem, a nie słyszeliście, aleście czynili, co złego jest przed oczyma mojemi, a czegom Ja nie chciał, obieraliście.
ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe, ndipo nonse mudzaphedwa; chifukwa simunayankhe pamene ndinakuyitanani, ndinayankhula koma simunamvere. Munachita zoyipa pamaso panga ndipo munasankha kuchita zoyipa zomwe sindikondwera nazo.”
13 Przetoż tak mówi panujący Pan: Oto słudzy moi jeść będą, a wy łaknąć będziecie; oto słudzy moi pić będą, a wy pragnąć będziecie; oto słudzy moi weselić się będą, a wy zawstydzeni będziecie.
Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, “Atumiki anga adzadya, koma inu mudzakhala ndi njala; atumiki anga adzamwa, koma inu mudzakhala ndi ludzu; atumiki anga adzakondwa, koma inu mudzakhala ndi manyazi.
14 Oto słudzy moi wykrzykać będą od radości serdecznej, a wy będziecie wołać od boleści serca, i od skruszenia ducha wyć będziecie.
Atumiki anga adzayimba mosangalala, koma inu mudzalira kwambiri chifukwa chovutika mu mtima ndipo mudzalira mofuwula chifukwa mudzamva kuwawa mu mtima.
15 I zostawicie imię wasze na przeklinanie wybranym moim, gdy was pomorduje panujący Pan, a sługi swe nazwie innem imieniem.
Anthu anga osankhidwa adzatchula dzina lanu potemberera. Ambuye Yehova adzakuphani, koma atumiki ake adzawapatsa dzina lina.
16 Ten, który sobie będzie błogosławił na ziemi, będzie sobie błogosławił w Bogu prawdziwym; a kto będzie przysięgał na ziemi, będzie przysięgał przez Boga prawdziwego; w zapomnienie zaiste przyjdą te uciski pierwsze, a będą zakryte od oczów moich.
Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo adzachita zimenezo kwa Mulungu woona; ndipo aliyense wochita malumbiro mʼdzikomo adzalumbira mwa Mulungu woona. Pakuti mavuto akale adzayiwalika ndipo adzachotsedwa pamaso panga.
17 Albowiem oto Ja tworzę niebiosa nowe, i ziemię nową, a nie będą wspominane rzeczy pierwsze, ani wstąpią na serce.
“Taonani, ndikulenga mlengalenga mwatsopano ndi dziko lapansi latsopano. Zinthu zakale sizidzakumbukika, zidzayiwalika kotheratu.
18 Owszem weselcie się, a radujcie się na wieki wieków z tego, co Ja stworzę; bo oto Ja stworzę Jeruzalem na radość, a lud jego na wesele.
Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya chifukwa cha zimene ndikulenga, pakuti ndikulenga Yerusalemu kukhala malo wosangalatsa ndipo anthu ake adzakhala achimwemwe.
19 I rozraduję się w Jeruzalemie, a weselić się będę w ludu moim; a nie będzie słychać w nim głosu płaczu i głosu narzekania.
Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu ndipo ndidzasangalala chifukwa cha anthu anga. Kumeneko sikudzamvekanso kulira ndi mfuwu wodandaula.
20 Nie będzie tam więcej nikogo w wieku dziecinnym, ani starca, któryby nie dopełnił dni swoich; bo dziecię we stu latach umrze; ale grzesznik, choćby miał i sto lat, przeklęty będzie.
“Ana sadzafa ali akhanda ndipo nkhalamba zonse zidzakwaniritsa zaka zawo zonse. Wamngʼono mwa iwo adzafa ali ndi zaka 100. Amene adzalephere kufika zaka 100 adzatengedwa kukhala wotembereredwa.
21 Pobudują też domy, a będą w nich mieszkali; nasadzą też winnic, a będą jeść owoce ich.
Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo, adzadzala mpesa ndipo adzadya zipatso zake.
22 Nie będą budować tak, aby tam inszy mieszkał; nie będą szczepić, aby inny jadł; bo dni ludu mojego będą jako dni drzewa, a dzieła rąk swoich do zwietszenia używać będą wybrani moi.
Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo, kapena kudzala ndi ena nʼkudya. Pakuti anthu anga adzakhala ndi moyo wautali ngati mitengo. Osankhidwa anga adzakondwera ndi ntchito ya manja awo nthawi yayitali.
23 Nie będą robić próżno, ani płodzić będą na postrach; bo będą nasieniem błogosławionych od Pana, oni i potomkowie ich z nimi.
Sadzagwira ntchito pachabe kapena kubereka ana kuti aone tsoka; chifukwa adzakhala anthu odalitsidwa ndi Yehova, iwowo pamodzi ndi adzukulu awo omwe.
24 Nadto stanie się, że pierwej niż zawołają, Ja się ozwę; jeszcze mówić będą, a Ja wysłucham.
Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe. Pamene akuyankhula kumene Ine ndidzakhala nditamva kale.
25 Wilk z barankiem paść się będą społem; lew jako wół plewy jeść będzie, a wężowi proch będzie chlebem jego; nie będą szkodzić ani zatracać na wszystkiej górze świętej mojej, mówi Pan.
Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi. Mkango udzadya udzu monga ngʼombe, koma fumbi ndiye chidzakhale chakudya cha njoka. Pa phiri langa lopatulika sipadzakhala chinthu chopweteka kapena chowononga,” akutero Yehova.

< Izajasza 65 >