< Izajasza 58 >
1 Wołaj wszystkiem gardłem, nie zawściągaj; wynoś głos swój jako trąba, a opowiedz ludowi mojemu przestępstwa ich, a domowi Jakóbowemu grzechy ich;
“Fuwula kwambiri, usaleke. Mawu ako amveke ngati lipenga. Uwawuze anthu anga za kulakwa kwawo; uwuze nyumba ya Yakobo za machimo awo.
2 Chociaż mię każdego dnia szukają, a znać chcą drogi moje, jako naród, który sprawiedliwość czyni, a sądu Boga swego nie opuszcza; pytają mię o sądach sprawiedliwości a przgną się przybliżyć do Boga mówiąc:
Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine; amaoneka ngati a chidwi chofuna kudziwa zimene ndimafuna, kukhala ngati kuti ndi dziko limene limachita zolondola ndipo silinasiye zolamulira za Mulungu wake. Amandipempha kuti ndigamule mlandu wawo mwachilungamo ndipo amaonetsa chidwi chofuna kukhala pafupi ndi Mulungu.
3 Przeczże pościmy, gdyż na to nie patrzysz? trapimy duszę naszę, a nie widzisz? Oto w dzień postu waszego przewodzicie wolę swoję, a wszystkie prace swoje wyciągacie.
Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala kudya pamene Inu simukulabadirapo? Kodi ife tavutikiranji nʼkudzichepetsa pamene Inu simunasamalepo?’” Yehova akuti, “Komatu tsiku lanu losala kudya, mumachita zinthu zokukondweretsani, ndipo mumazunza antchito anu onse.
4 Oto pościcie na swary, i na zwady, i bijecie pięścią niemiłościwie; nie pościcie, jak się godzi tych dni, aby był słyszany na wysokości głos wasz.
Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana, mpaka kumenyana ndi nkhonya zopweteka. Kusala kudya mukuchitiramu musayembekezere kuti mawu anu amveka kumwamba.
5 Izali to jest takowy post, jakim obrał, a dzień, w któryby trapił człowiek duszę swoję? żeby zwiesił jako sitowie głowę swoję, a wór i popiół sobie podścielał? Toż to nazwiesz postem, i dniem przyjemnym Panu?
Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku, kungokhala tsiku loti munthu adzichepetse basi? Kodi ndi tsiku loti munthu angowerama pansi ngati bango ndi kumayala ziguduli nʼkuthirapo phulusa nʼkugonapo? Kodi ndiye mumati kusala kudya kumeneko, tsiku lokondweretsa Yehova?
6 Ale to jest post, którym obrał: Rozwiąż związki niepobożności, rozwiąz brzemiona ciężkie, i wolno puść skruszonych, a tak wszelakie jarzmo rozerwij;
“Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna: Kumasula maunyolo ozunzizira anthu ndi kumasula zingwe za goli, kupereka ufulu kwa oponderezedwa ndi kuphwanya goli lililonse?
7 Ułamuj łaknącemu chleba twego, a ubogich wygnańców wprowadź do domu twego; ujrzyszli nagiego, przyodziej go, a przed ciałem swojem nie ukrywaj się.
Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu? Osowa ndi ongoyendayenda, kodi mwawapatsa malo ogona? Munthu wausiwa kodi mwamupatsa chovala?
8 Tedy wyniknie jako zorza ranna światłość twoja, a zdrowie twoje prędko zakwitnie! i pójdzie przed tobą sprawiedliwość twoja, a chwała Pańska zbierze cię.
Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha, ndipo mabala anu adzachira msangamsanga; chilungamo chanu chidzakutsogolerani ndipo ulemerero wa Yehova udzakhala chokutchinjirizani kumbuyo kwanu.
9 Tedy wzywać będziesz, a Pan wysłucha; zawołasz, a odpowieć: Owom Ja. Jeźli odejmiesz z pośrodku siebie i jarzmo, a przestaniesz palca wyciągać, i mówić nieprawości;
Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani; mukadzapempha thandizo, Iye adzati: Ine ndili pano. “Ngati muleka kuzunza anzanu, ngati musiya kuloza chala ndiponso kunena zoyipa za anzanu.
10 Jeźli wylejesz łaknącemu duszę swoję, a duszę utrapioną nasycisz: tedy wejdzie w ciemności światłość twoja, a zmierzk twój będzie jako południe.
Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala, ndi kuthandiza anthu oponderezedwa, pamenepo kuwala kwanu kudzaonekera mu mdima, ndipo usiku wanu udzakhala ngati usana.
11 Bo cię Pan ustawicznie poprowadzi, i nasyci pod największą suszą duszę twoję, a kości twoje utuczy, i będziesz jako ogród wilgotny, a jako zdrój wód, którego wody nie ustawają.
Yehova adzakutsogolerani nthawi zonse; adzakwaniritsa zosowa zanu mʼdziko longʼalukangʼaluka dzuwa ndipo adzalimbitsa matupi anu. Mudzakhala ngati dimba la madzi ambiri, ngati kasupe amene madzi ake saphwa.
12 I pobudują spłodzeni od ciebie pustynie starodawne, grunty od narodu do narodu wywiedziesz; i nazwą cię naprawcą obalin, i przeprawcą ścieżek ku mieszkaniu.
Anthu ako adzamanganso nyumba zimene zakhala mabwinja nthawi yayitali, ndipo adzamanganso pa maziko akalekale; inu mudzatchedwa okonza makoma opasuka. Anthu okonza misewu ndi nyumba zake.
13 Jeźliże odwrócisz od sabatu nogę swoję, abyś nie przewodził woli swojej w dzień mój święty; i jeżeli nazwiesz sabat rozkoszą, dniem świętym a Panu sławnym, i będzieszli go miał w uczciwości, tak, abyś weń nie czynił dróg swoich, i nie przewodził woli swej, i nie mówił słowo próżnego:
“Muzisunga osaphwanya Sabata; musamachite zimene mukufuna pa masiku anga opatulika, tsiku la Sabata lizikhala tsiku lachisangalalo. Tsiku lopatulika la Yehova muzililemekeza posayenda mʼnjira zanu, kapena kuchita zimene mukufuna ndi kuyankhula zopandapake,
14 Tedy będziesz rozkoszował w Panu; i wprowadzą cię na wysokie miejsca ziemi, i sprawię to, abyś pożywał dziedzictwa Jakóba, ojca twego; bo usta Pańskie mówiły.
mukatero mudzapeza chimwemwe mwa Yehova, ndipo ndidzakukwezani ndi kukupambanitsani pa dziko lonse lapansi. Mudzadyerera dziko limene ndinapatsa Yakobo kholo lanu.” Yehova wayankhula ndi pakamwa pake.