< II Królewska 10 >

1 A miał Achab siedmdziesiąt synów w Samaryi. I napisał Jehu list, a posłał go do Samaryi do książąt Jezreelskich, i do starszych i do tych, którzy wychowywali syny Achabowe, w te słowa:
Tsono Ahabu anali ndi ana aamuna 70 a ku Samariya. Ndipo Yehu analemba makalata nawatumiza ku Samariya kwa atsogoleri a mu mzinda wa Yezireeli, kwa akuluakulu ndiponso kwa amene ankalera ana a Ahabu, nati,
2 Skoro was dojdzie ten list, gdyż u was są synowie pana waszego, i u was wozy, i konie, i miasto obronne, i rynsztunek;
“Inu mukangolandira kalatayi, popeza ana a mbuye wanu ali ndi inu ndiponso muli ndi magaleta ndi akavalo, mzinda wotetezedwa ndi zida zankhondo,
3 Obierzcież najgodniejszego i najsposobniejszego z synów pana waszego, a posadźcie na stolicy ojca jego, i walczcie o dom pana waszego.
sankhani mwana wa mbuye wanu amene ndi wooneka bwino ndiponso woyenera, mulowetseni ufumu wa abambo ake. Kenaka muchite nkhondo kuteteza nyumba ya mbuye wanu.”
4 Ale się oni bardzo bojąc rzekli: Oto dwaj królowie nie ostali się przed nim, a jakoż my się ostoimy?
Koma anthuwo anachita mantha kwambiri ndipo anati, “Taonani, mafumu awiri sanathe kulimbana naye, nanga ife tingathe bwanji?”
5 A tak posłał ten, który był sprawcą domu, i ten, który był sprawcą miasta, i starsi, i ci, którzy wychowywali syny królewskie, do Jehu, mówiąc: Słudzyśmy twoi, a co nam rozkażesz, uczynimy. Nie postanowiemy króla żadnego; co dobrego jest w oczach twoich, czyń.
Choncho woyangʼanira nyumba ya mfumu, bwanamkubwa wa mzinda, akuluakulu ena ndiponso olera anawo anatumiza uthenga uwu kwa Yehu: “Ife ndife atumiki anu ndipo tidzachita chilichonse chomwe mutiwuze. Sitidzasankha munthu wina aliyense kukhala mfumu ndipo chitani chimene mukuganiza kuti nʼchabwino kwa inu.”
6 I napisał do nich list drugi, mówiąc: Jeźliście moi, a głosu mego słuchacie, weźmijcież głowy synów pana waszego, a przyjdźcie do mnie jutro o tym czasie do Jezreel. A synów królewskich było siedmdziesiąt mężów u najprzedniejszych w mieście, którzy je wychowywali.
Ndipo Yehu anawalembera kalata yachiwiri yonena kuti, “Ngati inu muli mbali yanga ndi kuti mudzandimvera, mudule mitu ya ana a mbuye wanu ndipo mubwere nayo kwa ine ku Yezireeli mawa nthawi ngati yomwe ino.” Tsono ana a mfumu onse 70 anali pamodzi ndi akuluakulu a mu mzindamo, amene ankawalera.
7 A gdy ich list doszedł, wziąwszy syny królewskie, pobili onych siedmdziesiąt mężów, a składłszy głowy ich do koszów, posłali je do niego do Jezreela.
Kalatayo itafika, anthuwo anatenga ana a mfumu 70 aja ndi kuwapha onse. Anayika mitu yawo mʼmadengu ndi kuyitumiza ku Yezireeli kwa Yehu.
8 I przyszedł poseł, który mu oznajmił, mówiąc: Przyniesiono głowy synów królewskich. A on rzekł: Składźcie je na dwie kupie u wejścia bramy aż do poranku.
Mthenga uja atafika, anamuwuza Yehu kuti, “Abweretsa mitu ya ana a mfumu.” Ndipo Yehu analamula kuti, “Unjikani mituyo mʼmilu iwiri pa chipata cha mzinda ndipo ikhale pamenepo mpaka mmawa.”
9 A gdy rano wyszedł, stanął, i rzekł do wszystkiego ludu: Sprawiedliwiście wy. Otom się ja sprzysiągł przeciwko panu memu, i zabiłem go; ale te wszystkie któż pobił?
Mmawa mwake Yehu anatuluka. Iye anayimirira pamaso pa anthu onse ndipo anati, “Inu ndinu osalakwa. Ndine amene ndinachita chiwembu mbuye wanu ndi kumupha, koma kodi wapha anthu onsewa ndani?
10 Wiedzcież teraz, że nie upadło próżno żadne z słów Pańskich na ziemię, które mówił Pan przeciwko domowi Achabowemu, gdyż uczynił Pan, co był powiedział przez sługę swego Elijasza.
Koma dziwani tsono, kuti mawu amene Yehova anayankhula kunena za banja la Ahabu sadzapita padera. Yehova wachita chimene analonjeza kudzera mwa mtumiki wake Eliya.”
11 A tak pobił Jehu wszystkie, którzy pozostali z domu Achabowego w Jezreelu, i wszystkie najprzedniejsze jego, i przyjaciele jego, i kapłany jego, tak iż nie zostawił po nim żadnego żywego.
Choncho Yehu anapha onse amene anatsala a mʼbanja la Ahabu ku Yezireeli, pamodzinso ndi akuluakulu ake onse, abwenzi ake ndiponso ansembe ake, sanasiyeko ndi mmodzi yemwe wamoyo.
12 Potem wstawszy odszedł, i pojechał do Samaryi. A gdy był a domu, gdzie pasterze strzygali owce na drodze,
Kenaka Yehu ananyamuka kupita ku Samariya. Atafika pa malo otchedwa Beti-Ekedi wa abusa,
13 Tedy Jehu znalazł u braci Ochozyjasza króla Judzkiego, i rzekł: Któście wy? I odpowiedzieli: Braciaśmy Ochozyjaszowi, a idziemy, abyśmy pozdrowili syny królewskie, i syny królowej.
Yehu anakumana ndi abale ena a Ahaziya mfumu ya Yuda nawafunsa kuti, “Kodi ndinu yani?” Iwo anayankha kuti, “Ndife abale ake a Ahaziya, ndipo tabwera kulonjera banja la mfumu ndi ana a mfumukazi.”
14 Tedy rzekł: Pojmajcie je żywo. I pojmali je żywo, i pobili je u studni onegoż domu, gdzie strzygano owce, czterdziestu i dwóch mężów, i nie zostawił żadnego z nich.
Yehu analamula kuti, “Atengeni amoyo!” Choncho anawatenga amoyo ndipo anakawaphera ku chitsime cha ku malo otchedwa Beti-Ekedi wa abusa; anthu onse 42. Iye sanasiyepo ndi mmodzi yemwe wamoyo.
15 Potem odjechawszy stamtąd, trafił Jonadaba, syna Rechabowego, idącego przeciwko sobie, a pozdrowił go i rzekł do niego: Jestże serce twoje szczere, jako serce moje z sercem twojem? I odpowiedział mu Jonadab: Jest. A jest? rzekł Jehu, dajże mi rękę twoję. Tedy mu dał rękę swą; i kazał mu wsiąść do siebie na wóz.
Yehu atachoka kumeneko anakumana ndi Yehonadabu mwana wa Rekabu, amene amabwera kudzakumana naye. Yehu anamulonjera nati kwa iye, “Kodi mtima wako uli bwino monga momwe mtima wanga ugwirizana nawo mtima wako?” Yehonadabu anayankha kuti, “Inde ndikugwirizana nawe.” Yehu anati, “Ngati ndi choncho, gwire dzanja.” Ndipo iye anaterodi, ndipo Yehu anamugwira dzanja namulowetsa mʼgaleta lake.
16 I rzekł: Jedź ze mną, a przypatrz się gorliwości mojej za Pana. A tak wiózł go na wozie swoim.
Yehu anati, “Tiye kuno uwone mmene ndikudziperekera kwa Yehova.” Ndipo anayenda naye mʼgaleta mwake.
17 A gdy przyjechał do Samaryi, bił wszystkie, którzy byli pozostali z domu Achabowego w Samaryi, i wytracił je według słowa Pańskiego, który mówił do Elijasza.
Yehu atafika ku Samariya, anapha onse amene anatsala a mʼbanja la Ahabu ku Samariya; anawawonongeratu potsata mawu a Yehova amene anayankhula kudzera mwa Eliya.
18 Zatem zebrał Jehu wszystek lud, i rzekł do niego: Achab służył Baalowi mało, Jehu mu będzie służył więcej.
Ndipo Yehu anasonkhanitsa anthu onse pamodzi nawawuza kuti, “Ahabu ankatumikira Baala pangʼono chabe; Yehu adzamutumikira kwambiri.
19 Przetoż teraz wszystkich proroków Baalowych, i wszystkich sług jego, i wszystkich kapłanów jego, zwołajcie do mnie aż do jednego; albowiem ofiarę wielką będę sprawował Baalowi. Ktoby się kolwiek nie stawił, nie zostanie żyw. A to Jehu chytrze czynił, chcąc wytracić chwalce Baalowe.
Tsopano itanani aneneri a Baala onse, atumiki ake onse ndi ansembe ake onse. Pasapezeke ndi mmodzi yemwe wotsala chifukwa ine ndidzapereka nsembe yayikulu kwa Baala. Aliyense amene alephere kubwera adzaphedwa.” Koma Yehu anachita zimenezi mwachinyengo ndi cholinga choti awononge atumiki onse a Baala.
20 Nadto rzekł Jehu: Zapowiedzcie święto Baalowi. I obwołano je.
Yehu anati, “Itanitsani msonkhano wodzalemekeza Baala.” Ndipo analengeza za msonkhanowo.
21 I rozesłał Jehu do wszystkiego Izraela. I zeszli się wszyscy chwalcy Baalowi, tak że nie został żaden, któryby nie przyszedł. I weszli do kościoła Baalowego, a napełniony był dom Baalowy od końca aż do końca.
Pamenepo Yehu anatumiza mawu ku dziko lonse la Israeli ndipo atumiki onse a Baala anabwera; palibe ndi mmodzi yemwe amene anatsala. Iwo anadzaza nyumba ya Baala. Nyumbayo inadzaziratu kuchokera ku khoma lina mpaka ku khoma lina.
22 Tedy rzekł temu, który był nad szatami: Wynieś szaty wszystkim chwalcom Baalowym. I wyniósł im szaty.
Ndipo Yehu anawuza munthu wosunga mikanjo kuti, “Bweretsa mikanjo yokwanira atumiki onse a Baala.” Ndipo iye anabweretsa mikanjoyo.
23 Zatem wszedł Jehu i Jonadab, syn Rechabowy, do domu Baalowego, i rzekł chwalcom Baalowym: Dowiedzcie się, a obaczcie, by snać nie był kto z wami z chwalców Pańskich, oprócz samych chwalców Baalowych.
Kenaka Yehu ndi Yehonadabu mwana wa Rekabu analowa mʼnyumba ya Baala. Yehu anawawuza atumiki a Baala kuti, “Yangʼanitsitsani ndipo muone kuti muno musapezeke atumiki a Yehova, koma mukhale atumiki okhawo a Baala.”
24 A tak weszli, aby sprawowali ofiary, i całopalenia. Ale Jehu sporządził był sobie na dworze ośmdziesiąt mężów, którym był rzekł: Jeźliby kto uszedł z ludu tego, który ja podawam w ręce wasze, dusza wasza będzie za duszę onego.
Choncho Yehu analowa kukapereka nsembe zina ndi nsembe zopsereza. Nthawi iyi nʼkuti Yehu atayika anthu 80 kunja kwa nyumbayo ndi chenjezo lakuti, “Ngati wina aliyense wa inu adzathawitsa wina aliyense wa anthu amene ndayika kuti muziwayangʼanira, munthu woteroyo adzaphedwa.”
25 A gdy się dokończyły ofiary całopalenia, rzekł Jehu żołnierzom i rotmistrzom swym: Wnijdzcie, a pomordujcie je, aby żaden nie uszedł. A tak pomordowali je ostrzem miecza, i rozrzucili je żołnierze i rotmistrze; potem odeszli do każdego miasta, gdzie był dom Baalowy.
Yehu atangotsiriza kupereka nsembe yopsereza, analamula alonda ndi akulu a ankhondo kuti, “Lowani ndipo mukawaphe ndipo musalole kuti wina athawe.” Choncho iwo anawapha ndi lupanga. Alonda ndi akulu a ankhondo anaponya mitembo ya anthuwo panja ndipo anakalowa mʼkati mwenimweni mwa nyumba ya Baala.
26 A wyrzuciwszy bałwany z domu Baalowego, popalili je.
Iwo anakatulutsa mwala wopatulika umene unali mʼnyumba ya Baala ndipo anawutentha.
27 Obalili też słup Baalowy, obalili i dom jego, a uczynili z niego wychody, aż do tego czasu.
Anawononga mwala wopatulika wa Baala ndi kugwetsa nyumba ya Baala, ndipo anthu anayisandutsa chimbudzi mpaka lero lino.
28 A tak wygładził Jehu Baala z Izraela.
Motero Yehu anawononga Baala mu Israeli.
29 Wszakże od grzechów Jeroboama, syna Nabatowego, który do grzechu przywiódł Izraela, nie odstąpił Jehu, ani opuścił cielców złotych, które były w Betel, i które były w Dan.
Koma Yehuyo sanaleke machimo a Yeroboamu mwana wa Nebati amene anachimwitsa nawo Israeli kupembedza mafano a golide a ana angʼombe ku Beteli ndi ku Dani.
30 Tedy rzekł Pan do Jehu: Ponieważeś się pilnie starał, abyś uczynił, co dobrego jest w oczach moich, według wszystkiego, co było w sercu mojem, uczyniłeś domowi Achabowemu: synowie twoi aż do czwartego pokolenia siedzieć będą na stolicy Izraelskiej.
Yehova anati kwa Yehu, “Chifukwa wachita bwino pokwaniritsa kuchita zabwino pamaso panga ndipo wachitira banja la Ahabu zonse zimene zinali mʼmaganizo anga, zidzukulu zako zidzakhala pa mpando waufumu wa Israeli mpaka mʼbado wachinayi.”
31 Ale Jehu nie strzegł tego, aby chodził w zakonie Pana, Boga Izraelskiego, ze wszystkiego serca swego, ani odstąpił od grzechów Jeroboamowych, który do grzechu przywiódł Izraela.
Komatu Yehu sanasamalire kusunga lamulo la Yehova Mulungu wa Israeli ndi mtima wake wonse. Iyeyo sanaleke machimo a Yeroboamu amene anachimwitsa nawo Israeli.
32 W one dni począł Pan umniejszać Izraela: bo je poraził Hazael po wszystkich granicach Izraelskich:
Masiku amenewo Yehova anayamba kuchepetsa dziko la Israeli. Hazaeli anagonjetsa Aisraeli,
33 Od Jordanu aż na wschód słońca, wszystkę ziemię Galaadską, Gadową, i Rubenową, i Manasesową od Aroer, które jest u potoku Arnon, i Galaad, i Basan.
kuyambira kummawa kwa Yorodani, dziko lonse la Giliyadi (chigawo cha Gadi, Rubeni ndi Manase), kuchokera ku Aroeri pafupi ndi chigwa cha Arinoni kudutsa Giliyadi mpaka ku Basani.
34 Ale ostatek spraw Jehu, i wszystko, co czynił, i wszystka moc jego, azaż tego nie napisano w kronikach królów Izraelskich?
Ntchito zina za Yehu ndi zonse zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Israeli?
35 I zasnął Jehu z ojcami swymi, i pochowali go w Samaryi; a królował Joachaz, syn jego, miasto niego.
Yehu anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake ku Samariya. Ndipo Yehowahazi mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
36 A czas, którego królował Jehu nad Izraelem w Samaryi, było dwadzieścia i ośm lat.
Yehu analamulira Aisraeli ku Samariya zaka 28.

< II Królewska 10 >