< I Kronik 25 >
1 I odłączył Dawid i hetmani wojska na posługiwanie synów Asafowych i Hemanowych, i Jedytunowych, którzy prorokowali przy cytrach, i przy harfach, i przy cymbałach. A była liczba ich, to jest mążów pracujących w usłudze swej:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Z synów Asafowych: Zachur, i Józef, i Natanijasz, i Asarela. Synowie Asafowi byli pod ręką Asafową, który prorokował na rozkazanie królewskie.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Z Jedytuna: Synowie Jedytunowi: Godolijasz, i Zery, i Jesajasz, Hasabijasz, i Matytyjasz, i Symej, sześć, pod ręką ojca ich Jedytuna, który prorokował przy harfie, wyznawając i chwaląc Pana.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Z Hemana: Synowie Hemanowi: Bukkijasz, Matanijasz, Husyjel, Zebuel, i Jerymot, Chananijasz, Chanani, Eliata, Gieddalty, i Romantyjeser, i Jasbekassa, Malloty, Hotyr, Machazyjot.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Ci wszyscy byli synowie Hemana, widzącego królewskiego w słowach Bożych, ku wywyższeniu rogu: bo dał Bóg czternaście synów Hemanowych, i trzy córki.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Ci wszyscy byli pod sprawą ojca swego przy śpiewaniu w domu Pańskim na cymbałach, na lutniach, i na cytrach ku służbie w domu Bożym, jako rozkazał król, i Asaf, Jedytun, i Heman.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 A był poczet ich z braci ich, którzy byli ćwiczonymi w pieśniach Pańskich, wszystkich mistrzów dwieście ośmdziesiąt i ośm.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 I miotali losy, straż przeciwko straży, tak mały jako i wielki, tak mistrz jako i uczeń.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 I padł los pierwszy w domu Asafowym na Józefa; na Godolijasza wtóry, z braćmi jego i z synami jego, których było dwanaście.
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 Na Zachura trzeci, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 Czwarty na Isrego, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 Piąty na Natanijasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 Szósty na Bukkijasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 Siódmy na Jesarela, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 Osmy na Jesajasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 Dziewiąty na Matanijasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 Dziesiąty na Symejasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 Jedenasty na Asarela, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 Dwunasty na Hasabijasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 Trzynasty na Subajela, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 Czternasty na Matytyjasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 Piętnasty na Jerymota, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 Szesnasty naChananijasza, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 Siedemnasty na Jesbekassa, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 Ośmnasty na Chananijego, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 Dziewiętnasty na Mallotego, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 Dwudziesty na Elijata, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 Dwudziesty i pierwszy na Hotyra, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 Dwudziesty i wtóry na Gieddaltego, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 Dwudziesty i trzeci na Machazyjota, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 Dwudziesty i czwarty na Romantyjesera, na synów jego i na braci jego dwanaście.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.