< Psalm 68 >

1 KOT en kotida, pwe a imwintiti en kamueit pasang, o me kailongki i, en tang wei.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Adzuke Mulungu, adani ake amwazikane; adani ake athawe pamaso pake.
2 Kom kotin paki irail wei dueta adiniai, dueta kris kin pei pasang nan kisiniai, iduen me doo sang Kot akan en soredi.
Monga momwe mphepo imachotsera utsi; Inu muwawulutsire kutali. Monga phula limasungunukira pa moto, oyipa awonongeke pamaso pa Mulungu.
3 A me pung kan en pereperen o popol mon silang en Kot o ren pereperen melel.
Koma olungama asangalale ndi kukondwera pamaso pa Mulungu; iwo akondwere ndi kusangalala.
4 Kauli ong Kot, kauli ong mar a! Kaonopada al o ong i, me kotiwei nan sap tan, a maraneki Ieowa — komail perenki i!
Imbirani Mulungu imbirani dzina lake matamando, mukwezeni Iye amene amakwera pa mitambo; dzina lake ndi Yehova ndipo sangalalani pamaso pake.
5 Pwe i Sam en me sapoupou kan o saunkapung en li odi kan. I Kot nan sapwilim a tanpas saraui.
Atate wa ana amasiye, mtetezi wa akazi amasiye, ndiye Mulungu amene amakhala mʼmalo oyera.
6 Kot me kotin kadire kila seri ko im en me kin kelep, me kin lapwada me salidi kan, pwen pwaida o pereperen a me katiwo kan pan mimieta nan wasan lek.
Mulungu amakhazikitsa mtima pansi osungulumwa mʼmabanja, amatsogolera amʼndende ndi kuyimba; koma anthu osamvera amakhala ku malo owuma a dziko lapansi.
7 Maing Kot, ni ansau kom kotiwei mon sapwilim omui aramas akan, ni omui kotiwei nan sap tan! (Sela)
Pamene munatuluka kutsogolera anthu anu, Inu Mulungu, pamene munayenda kudutsa chipululu,
8 I ansau sap o rerer, o audepan lang kan moredier mon silang en Kot, nana Sinai mon silang en Kot en Israel.
dziko lapansi linagwedezeka, miyamba inakhuthula pansi mvula, pamaso pa Mulungu, Mmodzi uja wa ku Sinai. Pamaso pa Mulungu, Mulungu wa Israeli.
9 Maing Kot, kom kotin kamoredier katau mau, o kom kotin kamauradar sapwilim omui soso, me mongedier,
Munapereka mivumbi yochuluka, Inu Mulungu; munatsitsimutsa cholowa chanu cholefuka.
10 Pwe sapwilim omui pwin diar wasa, me a kak kotikot ia. Maing Kot, kom kotin apwalilar me luet akan duen omui kalangan.
Anthu anu anakhala mʼmenemo ndipo munapatsa anthu osauka zimene zinkawasowa chifukwa cha ubwino wanu Mulungu.
11 Ieowa kotikidier a masan ki pwin en wanporon kalaimun akan.
Ambuye analengeza mawu, ndipo gulu linali lalikulu la iwo amene anapita kukawafalitsa;
12 Nanmarki en karis toto tang wei madang, o waun im akan nek pasanger, me re atia sang ar imwintiti kan.
“Mafumu ndi ankhondo anathawa mwaliwiro; mʼmisasa anthu anagawana zolanda pa nkhondo.
13 Ni omail kairu nan pung en noumail pwin man akan, komail rasong pa en muroi men, me lingan dueta silper o pa a kan dueta kold lingan.
Ngakhale mukugona pakati pa makola a ziweto, mapiko a nkhunda akutidwa ndi siliva, nthenga zake ndi golide wonyezimira.”
14 Ma me Manaman o lao kotin kamueit pasang nanmarki kan, nana Salmon rotorot ap pan marainla.
Pamene Wamphamvuzonse anabalalitsa mafumu mʼdziko, zinali ngati matalala akugwa pa Zalimoni.
15 Nana Pasan iei nana en Kot; Pasan nana kalaimun eu.
Mapiri a Basani ndi mapiri aulemerero; mapiri a Basani, ndi mapiri a msonga zambiri.
16 Menda komail nana kalaimun akan kin kilekilang ap peirin ong nana, me Kot kotin piladar en kotikot ia? O Ieowa pan kotikot wasa o kokolata.
Muyangʼaniranji mwansanje inu mapiri a msonga zambiri, pa phiri limene Mulungu analisankha kuti azilamulira, kumene Yehova mwini adzakhalako kwamuyaya?
17 War en Kot me kid toto pan pak kid; Ieowa kotikot re’rail ni nana Sinai.
Magaleta a Mulungu ndi osawerengeka, ndi miyandamiyanda; Ambuye wabwera kuchokera ku Sinai, walowa mʼmalo ake opatulika.
18 Komui kotidalang poa o saliedier me salidi kan, o kom kotin ale ong aramas pai kan, pil ong ir me katiwo kan, pwe Ieowa en kotikot wasa o.
Pamene Inu munakwera mmwamba, munatsogolera a mʼndende ambiri; munalandira mphatso kuchokera kwa anthu, ngakhale kuchokera kwa owukira, kuti Inu Mulungu, mukhale kumeneko.
19 Kapinga Ieowa nin ran akan karos; Kot kin kotiki ong kitail katoutou patail, ap pil kotin sauasa kitail. (Sela)
Matamando akhale kwa Ambuye, kwa Mulungu Mpulumutsi wathu amene tsiku ndi tsiku amasenza zolemetsa zathu.
20 Atail Kot iei sauas patail, o Ieowa Kaun kin kotin dorela sang mela.
Mulungu wathu ndi Mulungu amene amapulumutsa; Ambuye Wamphamvuzonse ndiye amene amatipulumutsa ku imfa.
21 Melel, Kot pan kotin kawela mongan a imwintiti kan, o a pan kotin leser pasang takain mongan ir, me dadaurata ar katiwo.
Ndithu Mulungu adzaphwanya mitu ya adani ake, zipewa za ubweya za iwo amene amapitiriza kuchita machimo awo.
22 Ieowa kotin masanier: I pan kapure dong ir sang nan Pasan, I pan wa ir do sang nan kapin madau;
Ambuye akunena kuti, “Ndidzawabweretsa kuchokera ku Basani; ndidzawabweretsa kuchokera ku nyanja zozama.
23 Pwe koe en tiakedi ong nan ntan imwintiti kan, o noum kidi kan en tamotamo.
Kuti muviyike mapazi anu mʼmagazi a adani anu, pamene malilime a agalu anu akudyapo gawo lawo.”
24 Maing Kot, a sansal duen omui kotikot sili, duen omui kotikot sili nan mol omui saraui, ai Kot o ai Nanmarki.
Mayendedwe aulemu a anthu anu aonekera poyera, Inu Mulungu; mayendedwe olemekeza Mulungu wanga ndi Mfumu yanga yokalowa mʼmalo opatulika.
25 Pwin en kaul kin tiong, ap pwin en saunkasang nan pung en peinakap akan, me wiadar aip.
Patsogolo pali oyimba nyimbo pakamwa, pambuyo pawo oyimba nyimbo ndi zipangizo; pamodzi ndi iwo pali atsikana akuyimba matambolini.
26 Kapinga Kot Ieowa nan momodisou kan, komail me kisan parer en Israel.
Tamandani Mulungu mu msonkhano waukulu; tamandani Yehova mu msonkhano wa Israeli.
27 Peniamin tikitik kin kakaun nan pung ar, saupeidi en Iuda iangaki sapwilim ar akan toto, saupeidi en Sepulon, o saupeidi en Naptali.
Pali fuko lalingʼono la Benjamini, kuwatsogolera, pali gulu lalikulu la ana a mafumu a Yuda, ndiponso pali ana a mafumu a Zebuloni ndi Nafutali.
28 Omail Kot kotin kauadar omail wei; Maing Kot, i me komui en kotin katengetengedi, pwe sapwilim omui dodok.
Kungani mphamvu zanu Mulungu; tionetseni nyonga zanu, Inu Mulungu, monga munachitira poyamba.
29 Nanmarki kan pan wa dong uk ar kisakis pweki omail im en kaudok nan Ierusalem.
Chifukwa cha Nyumba yanu ku Yerusalemu, mafumu adzabweretsa kwa Inu mphatso.
30 Kom kotin lipor ong man en nan rau, o pwin kau ol iangaki na kan, o wei kan, me kin pepei pweki kisin moni. Kotin kamueit pasang wek kan, me kin men mauin.
Dzudzulani chirombo pakati pa mabango, gulu la ngʼombe zazimuna pakati pa ana angʼombe a mitundu ya anthu. Mochititsidwa manyazi, abweretse mitanda ya siliva. Balalitsani anthu a mitundu ina amene amasangalatsidwa ndi nkhondo.
31 Saupedi en Äkipten pan pwarado; men Moren pan pokadang Kot pa’rail.
Nthumwi zidzachokera ku Igupto; Kusi adzadzipereka yekha kwa Mulungu.
32 Komail wei kan nin sappa kauli ong Kot, kakaul o kapinga Ieowa. (Sela)
Imbirani Mulungu Inu mafumu a dziko lapansi imbirani Ambuye matamando. (Sela)
33 I, me kin kotikot sili nanlang, nanlang en masia! Kilang, a kin kotiki ong sapwilim a nansapwe manaman.
Kwa Iye amene amakwera pa mitambo yakalekale ya mmwamba amene amabangula ndi mawu amphamvu.
34 Komail kamelele mana en Kot! A lingan mi ren Israel, o a mana mi nan tapok kan.
Lengezani za mphamvu za Mulungu, amene ulemerero wake uli pa Israeli amene mphamvu zake zili mʼmitambo.
35 Kot meid kapuriamui nan mole saraui. I Kot en Israel. A pan kotiki ong aramas akan mana o kelail. Kapinga Kot!
Ndinu woopsa, Inu Mulungu mʼmalo anu opatulika; Mulungu wa Israeli amapereka mphamvu ndi nyonga kwa anthu ake. Matamando akhale kwa Mulungu!

< Psalm 68 >