< Matayu 24 >

1 Yesu kalawiti Mnumba nkulu ya Mlungu, pakaweriti kankugenda zakuwi, wafundwa wakuwi wamgenderiti wamlanguziya majengu ga Numba nkulu ya Mlungu.
Yesu anatuluka mʼNyumba ya Mulungu ndipo akuchoka ophunzira ake anadza kwa Iye ndi kumuonetsa mamangidwe a Nyumbayo.
2 Yesu kawagambira, “Yina, muweza kugalola goseri aga! Nakaka nuwagambirani, kwahera hata libuwi limu halisigali panu pampindi pa libuwi limonga, kila libuwi haliwusiwi.”
Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukuona zinthu zonsezi? Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti palibe mwala pano umene udzasiyidwe pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.”
3 Yesu pakalivagiti palugongu lwa Mizeyituni, wafundwa wakuwi wamgenderiti kwa bada, su wamkosiya, “Gutugambiri, hashi vitwatira avi havilawili ndii? Na hashilawiri shishi kulanguziya ndo shipindi sha kwiza kwaku na shipindi sha upeleru pasipanu.” (aiōn g165)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
4 Yesu kawankula, “Mulikali weri, muntu nakiza kuwapayirani.
Yesu anayankha kuti, “Onetsetsani kuti wina asakunyengeni.
5 Wantu wavuwa hawalawili na kulonga kila yumu, ndo Kristu Mlopoziya na hawawazyangi wantu wavuwa.
Pakuti ambiri adzabwera mʼdzina langa nadzati, ‘Ndine Khristu,’ ndipo adzanyenga ambiri.
6 Hampikaniri kuusu ngondu pakwegera na visoweru vya ngondu, kumbiti namulihola. Toziya vitwatira mpaka vilawiri, kumbiti upeleru weni wankali kwiza.
Mudzamva za nkhondo ndi mbiri za nkhondo, koma onetsetsani kuti musadzidzimuke nazo. Zotere ziyenera kuchitika, koma chimaliziro sichinafike.
7 Isi yimu hailikomangi na isi yimonga na ufalumi wumu hawulikomangi na ufalumi umonga. Panu na palii hapaweri na njala na malendemeru ga isi kila pahala.
Mtundu ndi mtundu udzawukirana, ndipo ufumu ndi ufumu udzawukirana. Kudzakhala njala ndi zivomerezi mʼmalo osiyanasiyana.
8 Vitwatila vyoseri avi vilifana gambira kutama pakwanja pakulera mwana.
Zonsezi ndi chiyambi chabe cha zowawa.
9 “Shakapanu hawawalaviyani su wawatabisiyi na kuwalaga. Isi zoseri haziwakalaliri toziya ya litawu lyaneni.
“Pamenepo adzakuperekani kuti mukazunzidwe ndi kuphedwa, ndipo mitundu yonse idzakudani chifukwa cha Ine.
10 Mushipindi ashi wantu wavuwa hawaleki myoyu yawu, hawagambulikani weni kwa weni na kukalalirana weni kwa weni.
Pa nthawi imeneyo ambiri adzasiya chikhulupiriro ndipo adzadana ndi kuperekana wina ndi mnzake,
11 Hawalawili wambuyi wa upayira, pawapotuziya wantu wavuwa.
ndipo aneneri onama ambiri adzaoneka ndi kunyenga anthu ambiri.
12 Su vitwatira vifaa ndiri havyongereki, mafiliru ga wantu wavuwa hauweri tisutisu.
Chifukwa cha kuchuluka kwa zoyipa, chikondi cha ambiri chidzazirala,
13 Kumbiti muntu yakahepelera mpaka lupeleru hakalopoziwi.
koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka.
14 Na Shisoweru Shiwagira sha Ufalumi wa Mlungu hashibwerwi pasipanu poseri muwukapitawu kwa wantu wa makabila goseri na upeleru hawizi.
Ndipo uthenga wa ufumu udzalalikidwa ku dziko lonse lapansi ngati umboni kwa mitundu yonse, ndipo pomwepo chimaliziro chidzafika.”
15 “Su, hamuwoni ‘Shintu shidoda shashihalabisiya’ shakatakuliti Danieli mbuyi gwa Mlungu, shigoloka pahala pananagala.” Yakabetula kavimani mana yakuwi!
“Tsono mukadzaona chinthu chonyansa chosakaza chitayima pamalo oyera chimene anayankhula mneneri Danieli, owerengayo azindikire.
16 Panu, yawawera Yudeya su watugili muvigongu.
Pamenepo amene ali ku Yudeya athawire ku mapiri.
17 Yakawera pashitwiku sha numba nakasuluka kutola shintu mnumba mwakuwi.
Yemwe ali pa denga la nyumba yake asatsike kukatulutsa chinthu chilichonse mʼnyumba.
18 Yakaweriti kulirambu nakawuya kumbeli kutola nguwu yakuwi.
Yemwe ali ku munda asapite kukatenga mkanjo wake.
19 Shondi shondi wamawu yawawera na yinda na walii yawanoniziya mumashaka galii!
Kudzakhala koopsa kwambiri masiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi kwa oyamwitsa!
20 Mumluwi Mlungu, su kutuga kwa mwenga nakuwera mashaka ga mpepu ama lishaka lya Kwoyera!
Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzachitike nthawi yozizira kapena pa Sabata.
21 Toziya mushipindi ashi hakuweri na uhushu mkulu ndoweni wankali kulawira, kwanjira kunyawa kwa pasipanu mpaka leru, wala hapeni ilawiri kayi.
Popeza kudzakhala masautso aakulu, omwe safanana ndi ena ali onse chiyambireni cha dziko lapansi mpaka lero lino ndipo sadzafanananso ndi ena.
22 Kumbiti Mlungu kagapunguriti kala shiyasi sha mashaka aga, mekatendi ndiri, kwahera muntu yoseri mekalikali. Toziya ya wantu yawasyagulitwi, Mlungu hakagapunguli mashaka aga.
Ngati masiku amenewo sakanafupikitsidwa, palibe mmodzi akanapulumuka, koma chifukwa cha osankhidwawo masiku amenewo adzafupikitsidwa.
23 “Su, muntu yoseri pakawagambirani, ‘Guloli Kristu Mlopoziya kapanu’ ama ‘Kapalii!’ Namjimira.
Pa nthawi imeneyo ngati wina adzati kwa inu, ‘Onani, Khristu ali pano!’ Kapena, ‘Uyo ali ukoyo!’ Musakhulupirire.
24 Hawalawili ashina Kristu wa upayira na wambuyi wa upayira, hawatendi mauzauza makulu na gakulikangasha su wawazyangi payiwezekana ata yawasyagulitwi na Mlungu.
Chifukwa akhristu onama ndi aneneri onama adzaoneka ndipo adzachita zizindikiro zazikulu ndi zodabwitsa kuti akanyenge ngakhale osankhidwawo ngati kukanakhala kotheka kutero.
25 Mpikanili! Nuwagambirani pamberi pa shipindi kwiza.
Onani, ndakuwuzani izi nthawi isanafike.
26 “Ama, pawawagambirani, ‘Mloli, ka kushiwala!’ Namgenda aku, ama pawalonga, ‘Mloli, kalififa panu!’ Namjimira.
“Ndiye ngati wina akuwuzani inu kuti, ‘Uyo ali ku chipululu,’ inu musapiteko; kapena akati, ‘Uyu ali kuno mʼchipinda chamʼkati,’ musakhulupirire.
27 Mwana gwa Muntu hakizi gambira gulangala gambira lumeta kulyera kulawa kwagulawa mshenji mpaka kwaguzyeta mshenji.
Monga momwe mphenzi ingʼanima kuchokera kummawa kupita kumadzulo, momwemonso kudzakhala kubwera kwa Mwana wa Munthu.
28 “Palii paweriti na shashifuwiti, ndo pawajojinika wandapu.”
Kulikonse kuli chinthu cha kufa, makwangwala adzasonkhanako.
29 “Palaa palii, pa mashaka ga kutabisiya, mshenji haguweri ntiti, na lyezi haliweri ndiri na gulangala na ntondu hazituluki kulawa kulyera na likakala lya kumpindi halilibegizii.
“Akadzangotha mavuto a masiku amenewo, “‘dzuwa lidzadetsedwa, ndipo mwezi sudzawala; nyenyezi zidzagwa kuchokera kumwamba, ndipo mphamvu za mmwamba zidzagwedezeka.’
30 Shakapanu, lilangaliru lya Mwana gwa Muntu halilawiri kulyera na wantu woseri wa pasipanu hawalili pawamwona Mwana gwa Muntu pakiza mumawundi ga kumpindi pamuhera na makakala makulu.
“Pa nthawi imeneyo chizindikiro cha Mwana wa Munthu chidzaoneka mlengalenga, ndipo mitundu yonse ya pa dziko lapansi idzalira. Idzaona Mwana wa Munthu akubwera ndi mitambo, mphamvu ndi ulemerero waukulu.
31 Mliru mkulu gwa mbalapi hagupikaniki na yomberi hakawatumi wantumintumi wa kumpindi wakuwi muwega za msheshi za pasipanu na hawawajojiniri wantu kulawa lupeleru lumu lwa pasipanu mpaka lupeleru lumonga lwa pasipanu.
Ndipo adzatuma angelo ake, ndi kulira kwa lipenga kwakukulu, nadzasonkhanitsa osankhidwa ake kuchokera ku mphepo zinayi, ndi kuchokera kumathero a thambo kufika mbali ina.
32 “Mleki mtera gwa mkuyu guwafundi. Mitambi ya mitera payiyanja kutomola mahamba, muvimani kuwera shipindi sha kutowa vula shapakwegera.
“Tsopano kuchokera ku mtengo wamkuyu phunzirani ichi: Pamene uyamba kuphukira, masamba ake akatuluka, mumadziwa kuti dzinja layandikira.
33 Ntambu ira ayi mwenga pamwona vitwatira vyoseri avi, muvimani handa shipindi shapakwegera nentu.
Momwemonso, pamene mudzaona zinthu zonsezi mudzadziwe kuti ali pafupi pa khomo penipeni.
34 Muliholi kuwera vitwatira vyoseri avi havilawili pamberi pa kuhowa wantu yawalikala vinu.
Zoonadi, ndikuwuzani kuti mʼbado uwu sudzatha mpaka zinthu zonse zitachitika.
35 Kumpindi kwa Mlungu na pasipanu hazipiti, kumbiti visoweru vyaneni hapeni vipiti.
Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
36 “Kwahera muntu yoseri yakavimana lishaka ama lisaa paviza, ama wantumintumi wa kumpindi kwa Mlungu ama Mwana. Tati gweka yakuwi ndo yakavimana.
“Palibe amene adziwa za tsikulo kapena nthawi, angakhale angelo akumwamba, angakhale Mwana, koma Atate okha.
37 Kwiza kwa Mwana gwa Muntu hakuweri gambira shilii shashilawiriti mushipindi sha Nuhu.
Monga momwe zinalili nthawi ya Nowa, momwemonso zidzatero pobwera kwa Mwana wa Munthu.
38 Mumashaka galii pamberi pa wantu kuhowa mumafuriku waweriti wankuliya na kulanda, wantu waweriti wankuwayuga na kuyugwa mpaka Nuhu pakingiriti mumtumbwi,
Pakuti masiku amenewo chisanafike chigumula, anthu amadya ndi kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa, mpaka tsiku limene Nowa analowa mʼchombo;
39 wavimaniti ndiri hashilawiri shishi mpaka mafuliku pagiziti na kuwajola woseri. Ntambu ayi hayiweri pakiza Mwana gwa Muntu.
ndipo sanadziwe za chimene chikanachitika mpaka pamene chigumula chinafika ndi kuwamiza onse. Umu ndi mmene zidzakhalira pobwera kwa Mwana wa Munthu.
40 Shipindi ashi wantu wawili hawaweri mulirambu, yumu hakatolwi na yumonga hakalekwi.
Amuna awiri adzakhala mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
41 Wadala wawili hawaweri wankusyaga usaka palwala, yumu hakatolwi na yumonga hakalekwi.
Amayi awiri adzakhala akusinja pa mtondo; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
42 “Su gulikali weri, toziya guvimana ndiri lishaka lya kwiza Mtuwa gwenu.
“Chifukwa chake yangʼanirani, popeza simudziwa tsiku lanji limene Ambuye anu adzabwera.
43 Handa yakana numba mekavimani shipindi sha kwiza kwa mpoka, mekalikali masu na mekaleki ndiri mpoka kabomolangi numba yakuwi.
Koma zindikirani ichi: Ngati mwini nyumba akanadziwa nthawi yanji ya usiku imene mbala imabwera, sakanagona ndipo sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
44 Su na mwenga viraa muweri kala, toziya Mwana gwa Muntu hakizi mulisaa lyagulimana ndiri.”
Inunso tsono muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa nthawi imene inu simukumuyembekezera.
45 “Yesu kendeleyiti kutakula, Ndo gaa ntumintumi yakaaminika na kana luhala, ndo mtuwa gwakuwi hakamtuli pampindi pa wantu wakuwi, kawapanani shiboga kwa shipindi shakuwi?
“Kodi wantchito wokhulupirika ndi wanzeru amene ambuye ake anamuyika kukhala woyangʼanira antchito a mʼnyumba kuti awapatse chakudya chawo pa nthawi yake ndani?
46 Mbaka ntumintumi uliya mweni mtuwa gwakuwi pakiza hakamwoni kankutenda hangu.
Chidzakhala chabwino kwa wantchitoyo ngati mbuye wake pofika adzamupeza akuchita zimenezi.
47 Nukugambirani nakaka, katamtula ntumini ayu kagolokeri ulunda wakuwi woseri.
Zoonadi, ndikuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
48 Kumbiti handa ndo ntumintumi kadoda, hakaligambiziyi mweni kuwera mtuwa gwakuwi hakashelewi kuwuya,
Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo ndi woyipa, nati kwa iye yekha, ‘Mbuye wanga akuchedwa kubwera,’
49 na hakanji kuwakomanga wantumintumi wayaguwi na kanja kuliya na kulanda pamuhera na waloweru.
nayamba kumenya antchito anzake, nadya ndi kumwa ndi zidakwa.
50 Shakapanu mtuwa gwakuwi ntumintumi ulii pakizaku lishaka lyankali kulimana na shipindi shakashimana ndiri.
Mbuye wa wantchitoyo adzabwera pa tsiku limene iye samamuyembekezera ndi pa nthawi imene iye sakuyidziwa.
51 Mtuwa hakamwazibu nentu na kumtula shipinga shimu na wafyangu. Aku hakalili na kugayagaya menu gakuwi.”
Adzamulanga koopsa ndipo adzamuyika kokhala anthu achiphamaso, kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.”

< Matayu 24 >