< مزامیر 48 >
سرود. مزمور پسران قورَح. خداوند بزرگ است و باید او را در کوه مقدّسش در اورشلیم، ستایش کرد. | 1 |
Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
چه زیباست صهیون، آن کوه بلند خدا، آن شهر پادشاه بزرگ، که موجب شادی تمام مردم جهان میباشد! | 2 |
Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
خدا در دژهای اورشلیم است، او خود را همچون محافظ آن نمایان خواهد ساخت. | 3 |
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
پادشاهان جهان متحد شدند تا به اورشلیم حمله کنند. | 4 |
Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
اما وقتی آن را دیدند، شگفتزده شده، گریختند. | 5 |
iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
در آنجا ترس، آنان را فرا گرفت و همچون زنی در حال زایمان، وحشتزده شدند. | 6 |
Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
تو ای خدا، آنان را مانند کشتیهای تَرشیش که باد شرقی آنها را در هم میکوبد، نابود کردی. | 7 |
Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
آنچه دربارهٔ کارهای خداوند شنیده بودیم، اینک با چشمان خود در شهر خداوند لشکرهای آسمان میبینیم: او اورشلیم را برای همیشه پایدار نگه خواهد داشت. | 8 |
Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
ای خدا، ما در داخل خانهٔ تو، به رحمت و محبت تو میاندیشیم. | 9 |
Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
تو مورد ستایش همهٔ مردم هستی؛ آوازهٔ تو به سراسر جهان رسیده است؛ دست راستت سرشار از عدالت است. | 10 |
Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
بهسبب داوریهای عادلانهٔ تو ساکنان صهیون شادی میکنند و مردم یهودا به وجد میآیند. | 11 |
Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
ای قوم خدا، صهیون را طواف کنید و برجهایش را بشمارید. | 12 |
Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
به حصار آن توجه کنید و قلعههایش را از نظر بگذرانید. آن را خوب نگاه کنید تا بتوانید برای نسل آینده آن را بازگو کنید و بگویید: | 13 |
Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
«این خدا، خدای ماست و تا به هنگام مرگ او ما را هدایت خواهد کرد.» | 14 |
Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.