< مزامیر 125 >
سرود زائران به هنگام بالا رفتن به اورشلیم. آنانی که بر خداوند توکل دارند، مانند کوه صهیون، همیشه ثابت و پا برجا هستند. | 1 |
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
چنانکه کوهها گرداگرد شهر اورشلیم هستند، همچنان خداوند گرداگرد قوم خود است و تا ابد از آنها محافظت میکند! | 2 |
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
گناهکاران در سرزمین نیکوکاران همیشه حکمرانی نخواهند کرد، و گرنه نیکوکاران نیز دست خود را به گناه آلوده خواهند کرد. | 3 |
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
ای خداوند، به نیکوکاران و آنانی که دلشان با تو راست است، احسان کن، | 4 |
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
اما آنانی را که به راههای کج خود میروند، با سایر بدکاران مجازات کن. صلح و سلامتی بر اسرائیل باد! | 5 |
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.