< ایوب 40 >

آیا هنوز هم می‌خواهی با من که خدای قادر مطلق هستم مباحثه کنی؟ تو که از من انتقاد می‌کنی آیا می‌توانی جوابم را بدهی؟ ایوب به خداوند چنین پاسخ داد: 1
Yehova anati kwa Yobu:
2
“Kodi iwe ufuna kukangana ndi Wamphamvuzonse? Iwe amene unatsutsana ndi Mulungu umuyankhe Iyeyo!”
3
Pamenepo Yobu anayankha Yehova:
من کوچکتر از آنم که بتوانم به تو جواب دهم. دست بر دهانم می‌گذارم 4
“Ine sindili kanthu konse, kodi ndingathe kukuyankhani chiyani? Ndagwira pakamwa panga.
و دیگر سخن نمی‌گویم. 5
Ndinayankhula kamodzi, koma pano ndilibe yankho, ndinayankha kawiri, koma sindiwonjezeranso mawu ena.”
آنگاه خداوند از میان گردباد بار دیگر به ایوب چنین گفت: 6
Ndipo Yehova anayankha Yobu mʼkamvuluvulu kuti,
اکنون مثل یک مرد بایست و به سؤال من جواب بده. 7
“Tsopano vala dzilimbe ngati mwamuna; ndikufunsa mafunso ndipo iwe undiyankhe.
آیا مرا به بی‌عدالتی متهم می‌سازی و مرا محکوم می‌کنی تا ثابت کنی که حق با توست؟ 8
“Kodi iwe unganyoze chiweruzo changa cholungama? Kodi ungandidzudzule kuti iweyo ukhale wolungama?
آیا تو مانند خدا توانا هستی؟ آیا صدای تو می‌تواند مانند رعد او طنین اندازد؟ 9
Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu, ndipo mawu ako angagunde ngati mphenzi monga a Mulungu?
اگر چنین است پس خود را به فّر و شکوه ملبس ساز و با جلال و عظمت به پا خیز. 10
Ngati zili choncho udzikometsere ndi ulemerero ndi kukongola, ndipo udziveke ulemu ndi ulemerero waufumu.
به متکبران نگاه کن و با خشم خود آنها را به زیر انداز. 11
Tsanula ukali wako wosefukirawo, uyangʼane aliyense wodzikuza ndipo umuchepetse,
با یک نگاه، متکبران را ذلیل کن و بدکاران را در جایی که ایستاده‌اند پایمال نما. 12
Uyangʼane aliyense wodzikweza ndipo umutsitse, uwapondereze oyipa onse pamalo pomwe alilipo.
آنها را با هم در خاک دفن کن و ایشان را در دنیای مردگان به بند بکش. 13
Onsewo uwakwirire pamodzi mfumbi; ukulunge nkhope zawo mʼmanda.
اگر بتوانی این کارها را بکنی، آنگاه من قبول می‌کنم که با قوت خود می‌توانی نجات یابی. 14
Ukatero Ine ndidzakuvomereza kuti dzanja lako lamanja lakupulumutsadi.
نگاهی به بهیموت بینداز! من او را آفریده‌ام، همان‌طور که تو را آفریده‌ام! او مثل گاو علف می‌خورد. 15
“Taganiza za mvuwu, imene ndinayipanga monga momwe ndinapangira iwe, ndipo imadya udzu ngati ngʼombe.
کمر پرقدرت و عضلات شکمش را ملاحظه کن. 16
Mphamvu zake ndi zazikulu kwambiri, thupi lake ndi lanyonga kwambiri!
دمش مانند درخت سرو، راست است. رگ و پی رانش محکم به هم بافته شده است. 17
Mchira wake umayima tolotolo ngati mtengo wamkungudza; mitsempha ya ntchafu zake ndi yogwirana bwino.
استخوانهایش مانند تکه‌های مفرغ و دنده‌هایش چون میله‌های آهن، محکم می‌باشند. 18
Mafupa ake ali ngati mapayipi amkuwa, nthiti zake zili ngati mipiringidzo yachitsulo.
او سرآمدِ کارهای دست خداست، و تنها خالقش می‌تواند با شمشیرش به او نزدیک شود. 19
Mvuwuyo ndi yayikulu mwa zolengedwa za Mulungu, komatu mlengi wake amatha kuyiopseza ndi lupanga lake.
کوهها بهترین علوفهٔ خود را به او می‌دهند و حیوانات وحشی در کنار او بازی می‌کنند. 20
Imapeza chakudya chake ku mtunda ndipo nyama zakuthengo zonse zimasewera pambali pake.
زیر درختانِ کُنار، در نیزارها دراز می‌کشد 21
Imagona pa tsinde pa zitsamba za mipeta, imabisala mʼbango ndiponso pa thawale.
و سایهٔ آنها او را می‌پوشانند و درختان بید کنار رودخانه او را احاطه می‌کنند. 22
Imaphimbika ndi mthunzi wazitsamba za mipeta; imazunguliridwa ndi misondozi ya mu mtsinje.
طغیان رودخانه‌ها او را مضطرب نمی‌سازد و حتی اگر امواج جوشان رود اردن بر سرش بریزد، ترس به خود راه نمی‌دهد. 23
Madzi a mu mtsinje akakokoma, sichita mantha, iyo sitekeseka, ngakhale madzi a mu Yorodani afike mʼkhosi mwake.
هیچ‌کس نمی‌تواند قلاب به بینی او بزند و او را به دام اندازد. 24
Kodi alipo amene angathe kukola mvuwu ndi mbedza kapena kuyikola mu msampha?

< ایوب 40 >