< عِزرا 1 >

در سال اول سلطنت کوروش، پادشاه پارس، خداوند آنچه را که توسط ارمیای نبی فرموده بود، به انجام رساند. خداوند کوروش را بر آن داشت تا فرمانی صادر کند و آن را نوشته به سراسر سرزمین پهناورش بفرستد. این است متن آن فرمان: 1
Mʼchaka choyamba cha ufumu wa Koresi mfumu ya Perisiya, pofuna kukwaniritsa zimene anayankhula kudzera mwa Yeremiya, Yehova anayika maganizo mu mtima mwa Koresi mfumu ya Perisiya kuti alengeze mʼdziko lake lonse ndi mawu apakamwa ngakhalenso ochita kulemba.
«من، کوروش پادشاه پارس، اعلام می‌دارم که یهوه، خدای آسمانها، تمام ممالک جهان را به من بخشیده است و به من امر فرموده است که برای او در شهر اورشلیم که در یهوداست خانه‌ای بسازم. 2
Iye anati, “Koresi mfumu ya Perisiya ikunena kuti, “‘Yehova, Mulungu wakumwamba wandipatsa maufumu onse a dziko lapansi, ndipo wandipatsa udindo woti ndimumangire Nyumba ku Yerusalemu mʼdziko la Yuda.
بنابراین، از تمام یهودیانی که در سرزمین من هستند، کسانی که بخواهند می‌توانند به آنجا بازگردند و خانۀ یهوه، خدای اسرائیل را در اورشلیم بنا کنند. خدا همراه ایشان باشد! 3
Aliyense wa inu amene ali wa Yehova, Mulungu wakeyo akhale naye. Tsono aliyense wa inu apite ku Yerusalemu, mʼdziko la Yuda kuti akamange Nyumba ya Yehova, Mulungu wa Israeli. Iyeyu ndi Mulungu amene ali mu Yerusalemu.
همسایگان این یهودیان باید به ایشان طلا و نقره، توشه راه و چارپایان بدهند و نیز هدایا برای خانهٔ خدا تقدیم کنند.» 4
Ndipo kumalo kulikonse kumene otsalawo akukhala, athandizidwe ndi eni dzikolo powapatsa siliva, golide, katundu ndi ziweto ndi zopereka za ufulu zoti akapereke ku Nyumba ya Yehova imene ili ku Yerusalemu.’”
از طرف دیگر، خدا اشتیاق فراوان در دل رهبران طایفه‌های یهودا و بنیامین، و کاهنان و لاویان ایجاد کرد تا به اورشلیم بازگردند و خانهٔ خداوند را دوباره بنا کنند. 5
Choncho atsogoleri a mabanja afuko la Yuda ndi la Benjamini komanso ansembe ndi Alevi, aliyense amene Mulungu anawutsa mtima wake, anayamba kukonzeka kupita kukamanga Nyumba ya Yehova imene ili ku Yerusalemu.
تمام همسایگان، علاوه بر هدایایی که برای خانهٔ خدا تقدیم نمودند، هدایایی نیز از طلا و نقره، توشه راه و چارپایان به مسافران دادند. 6
Onse oyandikana nawo anawathandiza powapatsa ziwiya za siliva ndi zagolide, kuphatikizaponso katundu ndi ziweto, ndiponso mphatso zamtengo wapatali, kuwonjezera pa zopereka zaufulu zija.
کوروش نیز اشیاء قیمتی خانهٔ خداوند را که نِبوکَدنِصَّر آنها را از اورشلیم آورده و در معبد خدایان خود گذاشته بود، به یهودیان پس داد. 7
Nayenso mfumu Koresi anatulutsa ziwiya za mʼNyumba ya Yehova zimene Nebukadinezara anazitenga kuzichotsa ku Yerusalemu ndi kuziyika mʼnyumba ya milungu yake.
کوروش به خزانه‌دار خود، «میتراداد»، دستور داد که تمام این اشیاء قیمتی را از خزانه بیرون بیاورد و به شِیشبَصَّر، سرپرست یهودیانی که به سرزمین یهودا بازمی‌گشتند، تحویل بدهد. 8
Koresi, mfumu ya ku Perisiya inatulutsa ziwiyazi ndi kuzipereka kwa Miteridati, msungichuma amene anaziwerenga pamaso pa Sesibazara nduna yayikulu ya dziko la Yuda.
این اشیاء قیمتی عبارت بودند از: سینی طلا ‏ ۳۰ عدد سینی نقره ‏ ۱٬۰۰۰ عدد سینی‌های دیگر ‏ ۲۹ عدد جام طلا ‏ ۳۰ عدد جام نقره ‏ ۴۱۰ عدد ظروف دیگر ‏ ۱٬۰۰۰ عدد 9
Chiwerengerochi chinali motere: Mabeseni agolide 30 mabeseni asiliva 1,000 a zopereka 29
10
timiphika tagolide 230 timiphika tasiliva 410 ziwiya zina 1,000.
روی‌هم‌رفته ۵٬۴۰۰ ظروف قیمتی از طلا و نقره به شِیشبَصَّر سپرده شد و او آنها را با اسیرانی که از بابِل به اورشلیم می‌رفتند، برد. 11
Ziwiya zonse zagolide ndi siliva pamodzi zinalipo 5,400. Zonsezi ndi zimene Sezi-Bazara anabwera nazo pamene otengedwa ukapolo aja ankabwerera ku Yerusalemu kuchokera ku Babuloni.

< عِزرا 1 >