< حِزِقیال 25 >
پیغام دیگری از طرف خداوند به من رسید: «ای پسر انسان، روی خود را به سوی سرزمین عَمّون برگردان و بر ضد اهالی آنجا پیشگویی کن. | 1 |
Yehova anandiyankhula kuti:
“Iwe mwana wa munthu, tembenukira anthu a ku Amoni ndipo unenere mowadzudzula.
به ایشان بگو که به آنچه خداوند یهوه میفرماید، گوش دهند: وقتی خانهٔ من و سرزمین اسرائیل ویران میگشت و یهودا به اسارت برده میشد شما شادی میکردید؛ | 3 |
Awawuze kuti, ‘Inu anthu a ku Amoni, imvani zimene Ambuye Yehova akunena. Iye akuti: Inu munanena mawu onyoza pamene Nyumba yanga yopatulika inkayipitsidwa. Munanyozanso dziko la Israeli pamene linaguga ndiponso anthu a ku Yuda pamene anatengedwa ukapolo.
پس من نیز شما را به دست چادرنشینهای صحرا که در سمت شرقی مملکتتان قرار دارند تسلیم میکنم تا سرزمینتان را اشغال کنند. آنها چادرهای خود را در میان شما بر پا خواهند کرد، تمام محصولاتتان را برای خود جمع خواهند نمود و شیر دامهای شما را خواهند نوشید. | 4 |
Nʼchifukwa chake Ine ndidzakuperekani mʼmanja mwa anthu akummawa ngati cholowa chawo. Iwo adzamanga misasa yawo ndi kukhoma matenti awo pakati panu. Adzadya zipatso zanu ndi kumwa mkaka wanu.
شهر رَبّه را چراگاه شتران میکنم. تمام مملکت عمونیها را به صورت بیابان درمیآورم تا گلههای گوسفند در آن بچرند. آنگاه خواهید دانست که من یهوه هستم.» | 5 |
Ndidzasandutsa Raba kuti akhale busa la ngamira ndi mizinda ya Aamoni kuti ikhale makola a nkhosa. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
خداوند یهوه میفرماید: «چون شما به هنگام نابودی قوم من کف زدید و شادی کردید و رقصیدید، | 6 |
Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi: Inu munawomba mʼmanja ndi kumalumphalumpha. Munkakondwa mu mtima mwanu pamene munkanyoza dziko la Israeli.
بنابراین، من نیز دست خود را بر ضد شما دراز خواهم کرد و شما را به دست قومهای دیگر خواهم سپرد تا غارتتان کنند. دیگر نمیگذارم به صورت یک قوم باقی بمانید؛ شما را هلاک میکنم تا بدانید که من یهوه هستم.» | 7 |
Nʼchifukwa chake ndidzatambasula dzanja langa kuti ndikulangeni, ndipo ndidzakuperekani kuti mukhale chofunkha cha anthu a mitundu ina. Ndidzakuchotsani pakati pa anthu a mitundu ina ndi kukufafanizani mʼmayiko onse. Ndidzakuwonongani, ndipo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova!’”
خداوند یهوه میفرماید: «چون موآبیها گفتهاند یهودا از هیچ قوم دیگری بهتر نیست، | 8 |
“Ambuye Yehova akuti, ‘Anthu a ku Mowabu ndi a ku Seiri ananena kuti anthu a ku Yuda ali ngati mayiko ena onse.’
پس من نیز حدود شرقی موآب را به روی دشمن میگشایم و شهرهای آن را که مایهٔ فخر و مباهاتش هستند از بین میبرم، یعنی شهرهای بیتیشیموت، بعل معون، و قریه تایم را. قبایل چادرنشینی که در صحرای شرق موآب ساکنند، به داخل عمون و موآب خواهند ریخت. در میان قومها، موآب دیگر یک قوم به حساب نخواهد آمد. | 9 |
Nʼchifukwa chake ndidzagumula mbali ina ya Mowabu, kuyambira ku mizinda yake ya kumalire; mizinda yokongola ya Beti-Yesimoti, Baala-Meoni ndi Kiriataimu.
Ndidzapereka Amowabu pamodzi ndi Aamoni mʼmanja mwa anthu akummawa kotero kuti Aamoni adzayiwalikiratu pakati pa anthu a mitundu ina.
به این طریق موآبیها را مجازات میکنم تا بدانند که من یهوه هستم.» | 11 |
Ndidzawalangadi Amowabuwo. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
خداوند یهوه میفرماید: «چون قوم ادوم از قوم یهودا انتقام گرفت و با این کار مرتکب گناه بزرگی شد، | 12 |
“Ambuye Yehova akuti, ‘Pakuti Edomu analipsira Ayuda, ndiye kuti analakwa kwambiri pochita zimenezi.
پس با دست خود ادوم را ویران میکنم و ساکنانش را با گلهها و رمههایشان از بین میبرم. از تیمان تا ددان همه با شمشیر کشته خواهند شد. | 13 |
Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndidzatambasula dzanja langa kulanga Edomu ndi kupha anthu ake ndiponso nyama zawo. Ndidzawonongeratu Edomu ndipo adzaphedwa ndi lupanga kuchokera ku Temani mpaka ku Dedani.
این کار به دست قومم اسرائیل به انجام خواهد رسید. ایشان انتقام مرا از شما خواهند گرفت و شدت خشم مرا نشان خواهند داد.» این را خداوند یهوه میگوید. | 14 |
Ndidzalanga Edomu ndi dzanja la anthu anga Aisraeli. Adzalanga anthu a ku Edomu molingana ndi mkwiyo ndi ukali wanga. Choncho adzaona kulipsira kwanga akutero Ambuye Yehova.’”
خداوند یهوه میفرماید: «چون فلسطینیها از مردم یهودا انتقام گرفتهاند و از آنها کینهٔ دیرینه به دل داشته، در صدد بودند آنها را نابود سازند، | 15 |
“Ambuye Yehova akuti, ‘Afilisti analanga anthu anga mwankhanza ndi kuwalipsira.
پس من با دست خود فلسطینیها را نابود میکنم؛ بله، تمام کسانی را که در سرزمین فلسطین زندگی میکنند به کلی از بین میبرم. | 16 |
Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndidzatambasula dzanja langa kukantha Afilistiwo. Ndidzafafaniza Akereti ndi kuwononga iwo amene amakhala mʼmbali mwa nyanja.
از آنها به شدت انتقام میگیرم و آنها را سخت مجازات میکنم تا شدت خشم خود را به آنها نشان دهم. بعد از آن، خواهند دانست که من یهوه هستم.» | 17 |
Ndidzawabwezera chilango choopsa ndipo ndidzawalanga mu mkwiyo wanga. Ndikadzawalipsira ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”