< مزامیر 82 >

مزمور آساف خدا در جماعت خدا ایستاده است. درمیان خدایان داوری می‌کند: ۱ 1
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
«تا به کی به بی‌انصافی داوری خواهید کرد و شریران راطرفداری خواهید نمود؟ سلاه. ۲ 2
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
فقیران و یتیمان را دادرسی بکنید. مظلومان و مسکینان را انصاف دهید. ۳ 3
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
مظلومان و فقیران را برهانید و ایشان را ازدست شریران خلاصی دهید. ۴ 4
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
«نمی دانند و نمی فهمند و در تاریکی راه می‌روند و جمیع اساس زمین متزلزل می‌باشد. ۵ 5
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
من گفتم که شما خدایانید و جمیع شما فرزندان حضرت اعلی. ۶ 6
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
لیکن مثل آدمیان خواهید مرد وچون یکی از سروران خواهید افتاد!» ۷ 7
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
‌ای خدا برخیز و جهان را داوری فرما زیراکه تو تمامی امت‌ها را متصرف خواهی شد. ۸ 8
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.

< مزامیر 82 >