< Salmenes 100 >

1 En salme til lovprisning. Rop med fryd for Herren, all jorden!
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Tjen Herren med glede, kom frem for hans åsyn med jubel!
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3 Kjenn at Herren er Gud! Han har skapt oss, og ikke vi selv, til sitt folk og til den hjord han før.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4 Gå inn i hans porter med pris, i hans forgårder med lov, pris ham, lov hans navn!
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5 For Herren er god; hans miskunnhet varer til evig tid, og hans trofasthet fra slekt til slekt.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

< Salmenes 100 >