< Jobs 19 >
1 Da tok Job til orde og sa:
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 Hvor lenge vil I bedrøve min sjel og knuse mig med ord?
“Kodi mudzakhala mukundizunza mpaka liti, ndi kundilasa ndi mawu anuwo?
3 Det er nu tiende gang I håner mig og ikke skammer eder ved å krenke mig.
Inuyo mwandinyoza kwambiri; mwanditsutsa mopanda manyazi.
4 Har jeg virkelig faret vill, da blir min villfarelse min egen sak.
Ngati ndi zoona kuti ine ndasochera, cholakwachotu nʼchanga.
5 Vil I virkelig ophøie eder over mig og vise mig at min vanære har rammet mig med rette?
Ngati ndithudi mukudziyika nokha pamwamba panga, ndi kugwiritsa ntchito kunyozedwa kwanga polimbana nane,
6 Så vit da at Gud har gjort mig urett og satt sitt garn omkring mig!
pamenepa dziwani kuti Mulungu wandilakwira ndipo wandizinga ukonde wake.
7 Se, jeg roper: Vold! - men jeg får intet svar; jeg skriker om hjelp, men det er ingen rett å få.
“Ngakhale ndifuwule kuti, ‘Akundizunza!’ Palibe wondiyankha; ngakhale ndipemphe thandizo, palibe wondichitira zolungama.
8 Min vei har han stengt, så jeg ikke kommer frem, og over mine stier legger han mørke.
Mulungu wanditsekera njira yanga kotero sindingathe kudutsa; waphimba njira zanga ndi mdima.
9 Min ære har han avklædd mig og tatt bort kronen fra mitt hode.
Iye wandilanda ulemu wanga ndipo wandivula chipewa chaufumu pamutu panga.
10 Han bryter mig ned på alle kanter, så jeg går til grunne, og han rykker op mitt håp som et tre.
Wandiphwanyaphwanya mbali zonse ndipo ndatheratu; Iye wazula chiyembekezo changa ngati mtengo.
11 Han lar sin vrede brenne mot mig og akter mig som sin fiende.
Wandikwiyira ndipo akundiyesa mmodzi mwa adani ake.
12 Hans hærflokker kommer alle sammen og rydder sig vei mot mig, og de leirer sig rundt om mitt telt.
Ankhondo ake akubwera kwa ine mwamphamvu, akonzekera zodzalimbana nane ndipo azungulira nyumba yanga.
13 Mine brødre har han drevet langt bort fra mig, og mine kjenninger er blitt aldeles fremmede for mig.
“Mulungu wandisiyanitsa ndi abale anga; wasandutsa odziwana nane kukhala achilendo kwa ine.
14 Mine nærmeste holder sig borte, og mine kjente har glemt mig.
Abale anga andithawa; abwenzi anga andiyiwala.
15 Mine husfolk og mine tjenestepiker akter mig for en fremmed; jeg er en utlending i deres øine.
Anthu odzacheza ku nyumba kwanga ndiponso antchito anga aakazi andisandutsa mlendo; ndasanduka mlendo mʼmaso mwawo.
16 Kaller jeg på min tjener, så svarer han ikke; med egen munn må jeg bønnfalle ham.
Ndikayitana wa ntchito wanga, iye sandiyankha, ngakhale ndikapempha ndi pakamwa panga sandichitira kanthu.
17 Min ånde er motbydelig for min hustru, og min vonde lukt for min mors sønner.
Mpweya wanga umamunyansa mkazi wanga; ndine chinthu chonyansa kwa abale anga a mimba imodzi.
18 Endog barn forakter mig; vil jeg reise mig, så taler de mot mig.
Inde, ngakhale ana amandinyoza; akandiona amandinyodola.
19 Alle mine nærmeste venner avskyr mig, og de jeg elsket, har vendt sig mot mig.
Anzanga onse apamtima amanyansidwa nane; iwo amene ndinkawakonda andiwukira.
20 Mine ben trenger ut gjennem min hud og mitt kjøtt, og bare tannhinnen er ennu urørt på mig.
Ndangotsala khungu ndi mafupa okhaokha; ndapulumuka lokumbakumba.
21 Forbarm eder, forbarm eder over mig, I mine venner! For Guds hånd har rørt ved mig.
“Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni, pakuti dzanja la Mulungu landikantha.
22 Hvorfor forfølger I mig likesom Gud og blir ikke mette av mitt kjøtt?
Chifukwa chiyani mukundilondola ngati Mulungu? Kodi simunatope nalo thupi langa?
23 Men gid mine ord måtte bli opskrevet! Gid de måtte bli optegnet i en bok,
“Aa, achikhala mawu anga analembedwa, achikhala analembedwa mʼbuku,
24 ja, med jerngriffel og bly for evig bli hugget inn i sten!
akanalembedwa pa mwala ndi chitsulo, akanalembedwa pa thanthwe kuti sangathe kufufutidwa!
25 Men jeg - jeg vet min gjenløser lever, og som den siste skal han stå frem på støvet.
Koma ndikudziwa kuti mpulumutsi wanga ali ndi moyo, ndipo pa nthawi yomaliza adzabwera kudzanditeteza.
26 Og efterat denne min hud er blitt ødelagt, skal jeg ut fra mitt kjød skue Gud,
Ndipo khungu langa litatha nʼkuwonongeka, mʼthupi langa lomweli ndidzamuona Mulungu.
27 han som jeg skal skue, mig til gode, han som mine øine skal se og ikke nogen fremmed - mine nyrer tæres bort i mitt liv.
Ine ndemwe ndidzamuona Iye ndi maso angawa, ineyo, osati wina ayi. Ndithu mtima wanga ukufunitsitsadi!
28 Når I sier: Hvor vi skal forfølge ham! - I har jo funnet skylden hos mig -
“Koma inu mukuti, ‘Haa! Tingamuzunze bwanji, popeza kuti zonsezi zaoneka chifukwa cha iye yemweyo?’
29 så frykt for sverdet! For vrede er en synd som er hjemfalt til sverd. Dette sier jeg forat I skal tenke på at det kommer en dom.
Inu muyenera kuopa lupanga; pakuti mkwiyo wake umalangadi ndi lupanga; zikadzatero muzadziwa kuti chiweruzo chilipo ndithu.”