< Amahubo 93 >

1 INkosi iyabusa; yembethe ubukhosi; iNkosi yembethe amandla; izibhincisile. Umhlaba lawo uqinisiwe, kawuyikunyikinywa.
Yehova akulamulira, wavala ulemerero; Yehova wavala ulemerero ndipo wadzimangirira mphamvu, dziko lonse lakhazikika kolimba; silingasunthidwe.
2 Isihlalo sakho sobukhosi samiswa kwasendulo; usukela ephakadeni.
Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale; Inu ndinu wamuyaya.
3 Imifula iphakamisile, Nkosi, imifula iphakamise ukuholoba kwayo, imifula iphakamisile amagagasi ayo agubhazelayo.
Nyanja zakweza Inu Yehova, nyanja zakweza mawu ake; nyanja zakweza mafunde ake ochita mkokomo.
4 INkosi ephakemeyo ilamandla kulokuduma kwamanzi amanengi, kulamagagasi olwandle agubhazayo alamandla.
Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri, ndi wamphamvu kupambana mafunde a nyanja, Yehova mmwamba ndi wamphamvu.
5 Izifakazelo zakho ziqinisekile kakhulu; ubungcwele buyifanele indlu yakho, Nkosi, kuze kube ebudeni bezinsuku.
Malamulo anu Yehova ndi osasinthika; chiyero chimakongoletsa nyumba yanu mpaka muyaya.

< Amahubo 93 >