< Amahubo 26 >

1 Ngahlulela, Nkosi, ngoba mina ngihambe ngobuqotho bami, njalo ngithembele eNkosini, angiyikutshelela.
Salimo la Davide. Weruzeni Inu Yehova pakuti ndakhala moyo wosalakwa. Ndadalira Yehova popanda kugwedezeka.
2 Ngihlola, Nkosi, ungilinge, uhlole izinso zami lenhliziyo yami.
Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni, santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;
3 Ngoba uthandolomusa wakho luphambi kwamehlo ami, njalo ngihambe eqinisweni lakho.
pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse, ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.
4 Kangihlalanga labantu benkohliso, kangihambelani labazenzisayo.
Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo, kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.
5 Ngiyizondile inhlangano yabenzi bobubi, kangihlali lababi.
Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.
6 Ngizageza izandla zami ngokungelacala, ngizingelezele ilathi lakho, Nkosi.
Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova,
7 Ukuze ngizwakalise ngelizwi lokubonga, lokuze ngilandise zonke izenzo zakho ezimangalisayo.
kulengeza mofuwula za matamando anu ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa.
8 Nkosi, ngiyayithanda inhlalo yendlu yakho, lendawo yokuhlala yenkazimulo yakho.
Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo, malo amene ulemerero wanu umapezekako.
9 Ungabuthi umphefumulo wami kanye lezoni, kumbe impilo yami kanye labantu abomele igazi.
Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa, moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo,
10 Ozandla zabo zilobubi, lesandla sabo sokunene sigcwele izivalamlomo.
amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa, dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu.
11 Kodwa mina ngizahamba ngobuqotho bami; ngihlenga, ube lomusa kimi.
Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa; mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova.
12 Unyawo lwami lumi endaweni elingeneyo; ngizayidumisa iNkosi emabandleni.
Ndayima pa malo wopanda zovuta ndipo ndidzatamanda Yehova mu msonkhano waukulu.

< Amahubo 26 >