< Amahubo 128 >
1 Ubusisiwe wonke oyesabayo iNkosi, ohamba endleleni zayo.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake.
2 Ngoba uzakudla umsebenzi wezandla zakho; uzathokoza, njalo kuzakuba kuhle kuwe.
Udzadya chipatso cha ntchito yako; madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3 Umkakho uzakuba njengevini elithelayo emaceleni endlu yakho, abantwana bakho bazakuba njengamahlumela omhlwathi bezingelezele itafula lakho.
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka mʼkati mwa nyumba yako; ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi kuzungulira tebulo lako.
4 Ngoba khangela, ngokunjalo izabusiswa indoda eyesabayo iNkosi.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
5 INkosi izakubusisa iseZiyoni, njalo ubone okuhle kweJerusalema insuku zonke zempilo yakho,
Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni masiku onse a moyo wako; uwone zokoma za Yerusalemu,
6 yebo, uzabona abantwana babantwana bakho. Ukuthula kakube phezu kukaIsrayeli!
ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako. Mtendere ukhale ndi Israeli.