< Amahubo 125 >

1 Labo abathembela eNkosini banjengentaba iZiyonienganyikinyekiyo, emi kuze kube phakade.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2 Njengezintaba ziyiphahlile iJerusalema, ngokunjalo iNkosi iyabaphahla abantu bayo kusukela kulesisikhathi kuze kube nininini.
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3 Ngoba intonga yobukhosi yobubi kayiyikuhlala phezu kwesabelo sabalungileyo, ukuze abalungileyo bangeluleli izandla zabo kokubi.
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
4 Nkosi, yenza okuhle kubo abalungileyo lakubo abaqotho enhliziyweni zabo.
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
5 Kodwa labo abaphambukela ezindleleni zabo ezitshekileyo iNkosi izabenza bahambe labenzi bobubi. Ukuthula phezu kukaIsrayeli!
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.

< Amahubo 125 >