< Amanani 15 >
1 INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
Yehova anawuza Mose kuti,
2 Tshono ebantwaneni bakoIsrayeli uthi kubo: Lapho lifika elizweni lokuhlala kwenu, engilinika lona,
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukupatsanilo,
3 lisenza umnikelo owenzelwe iNkosi ngomlilo, umnikelo wokutshiswa kumbe umhlatshelo, owokugcwalisa isithembiso, loba emnikelweni wesihle, loba emikhosini yenu emisiweyo, ukwenza uqhatshi olumnandi eNkosini, okuvela enkomeni kumbe ezimvini,
ndipo mukamadzapereka kwa Yehova, nsembe yotentha pa moto ya ngʼombe kapena nkhosa monga fungo lokoma kwa Yehova, kaya ndi nsembe yopsereza kapena nsembe zina, nsembe yapadera chifukwa cha lumbiro kapena nsembe yoperekedwa mwaufulu kapenanso yoperekedwa pa chikondwerero,
4 lowo-ke onikelayo umnikelo wakhe eNkosini uzasondeza umnikelo wokudla, ube ngokwetshumi lempuphu ecolekileyo ixubene lengxenye yesine yehini yamafutha;
munthu amene akubweretsa zopereka zake, azikapereka kwa Yehova chopereka chachakudya cholemera kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta wokwana lita imodzi.
5 lewayini libe ngumnikelo wokunathwayo, ingxenye yesine yehini, uzakulungisa lomnikelo wokutshiswa loba umhlatshelo, owewundlu elilodwa.
Pamodzi ndi mwana wankhosa aliyense wa nsembe yopsereza kapena nsembe ina, muzikakonzanso lita imodzi la vinyo ngati chopereka cha chakumwa.’”
6 Kumbe owenqama lizalungisa umnikelo wokudla, ube zingxenye ezimbili etshumini zempuphu ecolekileyo ixubene lamafutha, ingxenye yesithathu yehini;
“Pamodzi ndi nkhosa yayimuna, muzikakonzanso chopereka cha chakudya cholemera makilogalamu awiri a ufa wosalala, wosakaniza ndi mafuta okwanira lita imodzi ndi theka,
7 lewayini libe ngumnikelo wokunathwayo, ingxenye yesithathu yehini, uzalinikela libe liphunga elimnandi eNkosini.
ndi vinyo wokwanira lita imodzi ndi theka ngati chopereka cha chakumwa. Muzikapereka monga nsembe yopereka fungo lokoma kwa Yehova.
8 Njalo nxa lilungisa ithole eliduna lenkomo libe ngumnikelo wokutshiswa kumbe umhlatshelo, owokugcwalisa isithembiso, kumbe iminikelo yokuthula eNkosini,
“‘Pamene mukukonza mwana wangʼombe wamwamuna kuti akhale nsembe yopsereza kapena nsembe ina iliyonse: ya lumbiro lapadera kapena nsembe yachiyanjano kwa Yehova,
9 uzanikelela-ke ithole lenkomo umnikelo wokudla, ube zingxenye ezintathu etshumini lempuphu ecolekileyo ixubene lamafutha, ingxenye yehini.
pamodzi ndi mwana wangʼombe wamwamunayo muzibweretsa nsembe yachakudya yolemera makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta okwana malita awiri.
10 Linikele iwayini libe ngumnikelo wokunathwayo, ingxenye yehini, kube ngumnikelo owenziwe ngomlilo olephunga elimnandi eNkosini.
Komanso muzibweretsa vinyo wokwanira malita awiri monga chopereka chachakumwa. Imeneyi idzakhala chopereka chotentha pa moto kuti likhale fungo lokoma kwa Yehova.
11 Kuzakwenziwa njalo ngaleyonkunzi, loba ngaleyonqama, loba ngewundlu, kumbe ngezinyane.
Ngʼombe yayimuna iliyonse kapena nkhosa yayimuna iliyonse, mwana wankhosa aliyense kapena mbuzi yayingʼono, zizikonzedwa motere.
12 Njengenani elizalilungisa, lizakwenza njalo kuleyo laleyo, ngokwenani lazo.
Ngakhale zingachuluke chotani, chitani izi kwa iliyonse ya nyamazo.
13 Wonke owokuzalwa elizweni uzazenza njalo lezizinto, ekunikeleni umnikelo owenziwe ngomlilo woqhatshi olumnandi eNkosini.
“‘Mbadwa iliyonse ya mu Israeli izichita zimenezi pamene ibweretsa nsembe yotentha pa moto kuti ikhale fungo lokoma kwa Yehova.
14 Uba-ke owemzini ohlala njengowezizwe lani, kumbe loba ngubani ophakathi kwenu ezizukulwaneni zenu, njalo enikela umnikelo owenziwe ngomlilo woqhatshi olumnandi eNkosini, njengoba lisenza uzakwenza njalo.
Ku mibado yanu yonse ya mʼtsogolo, pamene mlendo kapena wina aliyense wokhala pakati panu apereka chopereka chotentha pa moto kuti chikhale fungo lokoma kwa Yehova, azichita mofanana ndi momwe inu mumachitira.
15 Kuzakuba lesimiso sinye kini abebandla lakowemzini ohlala njengowezizwe, isimiso esilaphakade ezizukulwaneni zenu; njengani uzakuba njalo owemzini phambi kweNkosi.
Gulu lonse likhale ndi malamulo ofanana a inu kapena mlendo wokhala pakati panu. Limeneli ndi lamulo lamuyaya kwa mibado imene ikubwera. Inuyo ndi mlendo mudzakhala wofanana pamaso pa Yehova.
16 Kuzakuba lomthetho munye lesimiso sinye kini lakowemzini ohlala lani njengowezizwe.
Mudzakhale ndi malamulo ndi miyambo yofanana, inuyo ndi mlendo wokhala pakati panu.’”
17 INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
Yehova anawuza Mose kuti,
18 Tshono ebantwaneni bakoIsrayeli uthi kubo: Ekungeneni kwenu elizweni engilisa kulo,
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo unene kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukutengeraniko
19 kuzakuthi nxa lisidla okokudla kwelizwe, linikele umnikelo wokuphakanyiswa eNkosini.
ndipo mukakadya chakudya cha mʼdzikolo, mukapereke gawo lina kwa Yehova monga chopereka.
20 Ngokokuqala kwenhlama yenu lizanikela iqebelengwana, kube ngumnikelo wokuphakanyiswa; njengomnikelo wokuphakanyiswa webala lokubhulela, ngokunjalo lizawuphakamisa.
Pa buledi wanu woyamba, mukapereke mmodzi monga nsembe, ngati chopereka chochokera ku malo wopunthira tirigu.
21 Ngokokuqala kwenhlama yenu lizanika eNkosini umnikelo wokuphakanyiswa ezizukulwaneni zenu.
Pa mibado yanu yonse muzidzapereka chopereka ichi kwa Yehova kuchokera ku zakudya zanu zoyamba za mʼnthaka.
22 Uba-ke liduha, lingenzanga yonke imilayo le iNkosi eyikhulume kuMozisi,
“‘Ndipo ngati muchimwa mosadziwa posasunga ena mwa malamulo awa amene Yehova wapereka kwa Mose,
23 konke iNkosi elilaye khona ngesandla sikaMozisi kusukela ngosuku iNkosi eyalaya ngalo kusiya phambili ezizukulwaneni zenu,
lina lililonse mwa malamulo a Yehova amene wapereka kwa inu kudzera mwa Mose, kuyambira tsiku limene Yehova anawapereka mpaka mibado ya mʼtsogolo,
24 kuzakuthi-ke uba kwenziwe ngokungazi, kungekho emehlweni enhlangano, inhlangano yonke izanikela ijongosi elilodwa ithole lenkomo, libe ngumnikelo wokutshiswa, kube luqhatshi olumnandi eNkosini, lomnikelo walo wokudla, lomnikelo walo wokunathwayo njengomthetho, lezinyane lembuzi elilodwa, libe ngumnikelo wesono.
ndipo ngati zimenezi zachitika osati mwadala ndipo gulu lonse silinadziwe, zikatero gulu lonselo lipereke mwana wangʼombe wamwamuna monga nsembe yopsereza kuti likhale fungo lokoma kwa Yehova pamodzinso ndi chopereka chachakudya ndi chopereka cha chakumwa ndi mbuzi yayimuna ngati nsembe yopepesera machimo potsata zimene zinalamulidwa.
25 Umpristi uzakwenzela-ke inhlangano yonke yabantwana bakoIsrayeli inhlawulo yokuthula, bakuthethelelwe, ngoba kuyikungazi, futhi bona bazaletha umnikelo wabo, umnikelo owenzelwe iNkosi ngomlilo, lomnikelo wabo wesono phambi kweNkosi, ngenxa yesiphambeko sokungazi kwabo.
Wansembe apereke nsembe yopepesera machimo a gulu lonse la Aisraeli, ndipo adzakhululukidwa, pakuti linali tchimo lochita mosadziwa. Ndipo chifukwa cha tchimo lawolo, abweretse kwa Yehova nsembe yotentha pa moto ndi nsembe yopepesera machimo.
26 Lenhlangano yonke yabantwana bakoIsrayeli izakuthethelelwa, lowemzini ohlala njengowezizwe phakathi kwabo, ngoba kubo bonke abantu kwakusekungazini.
Gulu lonse la Aisraeli ndi alendo okhala pakati pawo adzakhululukidwa chifukwa anthu onsewo anachimwa mosadziwa.
27 Uba-ke umuntu oyedwa esona ngokungazi, uzasondeza isibhuzikazi esilomnyaka owodwa, sibe ngumnikelo wesono.
“‘Koma ngati munthu mmodzi achimwa mosadziwa, ayenera kubweretsa mbuzi yayikazi ya chaka chimodzi kuti ikhale nsembe yopepesera machimo.
28 Lompristi uzawenzela lowomphefumulo owone ngokungazi inhlawulo yokuthula, lapho one ngokungazi phambi kweNkosi, ukumenzela inhlawulo yokuthula; uzakuthethelelwa-ke.
Wansembe apereke nsembe yopepesera machimowo pamaso pa Yehova chifukwa cha munthu yemwe anachimwa mosadziwayo. Nsembe yopepesera tchimo lakelo ikaperekedwa, munthuyo adzakhululukidwa.
29 Lizakuba lomlayo munye kwalowo owona ngokungazi, owokuzalwa elizweni phakathi kwabantwana bakoIsrayeli, lowemzini ohlala njengowezizwe phakathi kwabo.
Lamulo lomweli ligwiritsidwe ntchito kwa aliyense wochimwa mosadziwa, kaya ndi mbadwa ya mu Israeli kapena mlendo.
30 Kodwa umuntu okwenza ngabomo, engowokuzalwa elizweni loba engowemzini, ethuka iNkosi; njalo lowomuntu uzaqunywa asuke phakathi kwabantu bakibo.
“‘Koma aliyense amene achimwa mwadala, kaya ndi mbadwa kapena mlendo, nachitira chipongwe Yehova, ameneyo achotsedwe ndithu pakati pa anthu ake.
31 Ngoba edelele ilizwi leNkosi, wephula umlayo wayo, lowomuntu uzaqunywa lokuqunywa; ububi bakhe buzakuba phezu kwakhe.
Popeza wanyoza mawu a Yehova ndi kuphwanya malamulo ake. Munthu ameneyo achotsedwe ndithu, kuchimwa kwake kudzakhala pa iyeyo.’”
32 Kwathi abantwana bakoIsrayeli besenkangala, bafica umuntu etheza inkuni ngosuku lwesabatha.
Aisraeli ali mʼchipululu, munthu wina anapezeka akutola nkhuni tsiku la Sabata.
33 Labo abamficayo etheza inkuni bamletha kuMozisi lakuAroni lakunhlangano yonke.
Amene anamupeza akutola nkhunizo anabwera naye kwa Mose ndi Aaroni ndi kwa gulu lonse
34 Bamfaka esitokisini, ngoba kwakungakatshiwo ukuthi kuzakwenziwani kuye.
ndipo anamutsekera mʼndende chifukwa sankadziwa choti achite naye.
35 INkosi yasisithi kuMozisi: Lowomuntu kabulawe lokubulawa; inhlangano yonke izamkhanda ngamatshe ngaphandle kwenkamba.
Pamenepo Yehova anawuza Mose kuti, “Munthu ameneyu ayenera kuphedwa. Gulu lonse liyenera kumugenda ndi miyala kunja kwa msasa.”
36 Lenhlangano yonke yamkhuphela ngaphandle kwenkamba, yamkhanda ngamatshe waze wafa, njengokulaya kweNkosi kuMozisi.
Choncho gululo linamutengera kunja kwa msasa ndi kumupha pomugenda ndi miyala, monga momwe Yehova analamulira Mose.
37 INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
Yehova anawuza Mose kuti,
38 Khuluma ebantwaneni bakoIsrayeli, ubatshele ukuthi bazenzele izintshaka emagumbini ezembatho zabo, ezizukulwaneni zabo, lokuthi bafake entshakeni yomphetho intambo eluhlaza okwesibhakabhaka.
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Pa mibado yanu yonse muzisokerera mphonje pa ngodya za zovala zanu ndipo pa ngodya ya mphonje iliyonse azisokererapo chingwe chobiriwira.
39 Njalo kuzakuba kini yintshaka ukuze likukhangele, likhumbule yonke imilayo yeNkosi, liyenze, lingadingi lilandele inhliziyo yenu lilandele amehlo enu, eliphinga ngokukulandela.
Mudzakhala ndi mphonje zimenezi kuti mukaziona muzikakumbukira malamulo onse a Yehova ndi kuwamvera kuti musamatsatenso zilakolako za mʼmitima mwanu ndi za maso anu.
40 Ukuze likhumbule lenze yonke imilayo yami, libe ngcwele kuNkulunkulu wenu.
Motero mudzakumbukira kumvera malamulo anga ndipo mudzakhala opatulikira a Mulungu wanu.
41 NgiyiNkosi uNkulunkulu wenu eyalikhupha elizweni leGibhithe ukuba nguNkulunkulu wenu; ngiyiNkosi uNkulunkulu wenu.
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mʼdziko la Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’”