< ULevi 12 >

1 INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
2 Tshono ebantwaneni bakoIsrayeli uthi: Uba owesifazana ekhululeka, abelethe owesilisa, uzakuba ngongcolileyo insuku eziyisikhombisa, njengensuku zokwehlukaniswa kwakhe esemfuleni uzakuba ngongcolileyo.
“Awuze Aisraeli kuti, ‘Mkazi akakhala woyembekezera, nabala mwana wa mwamuna, mkaziyo adzakhala wodetsedwa kwa masiku asanu ndi awiri, ngati pa masiku ake akusamba.
3 Langosuku lwesificaminwembili inyama yejwabu lakhe laphambili izasokwa.
Pa tsiku lachisanu ndi chitatu, mwanayo achite mdulidwe.
4 Khona ezahlala okwensuku ezingamatshumi amathathu lantathu egazini lokuhlanjululwa kwakhe, angathinti lutho olungcwele, angangeni endlini engcwele, zize ziphelele insuku zokuhlanjululwa kwakhe.
Mkaziyo adikire masiku ena 33 kuti ayeretsedwe ku matenda ake. Asakhudze kanthu kalikonse koyera kapena kulowa mʼmalo wopatulika mpaka masiku a kuyeretsedwa kwake atatha.
5 Kodwa angabeletha owesifazana, uzakuba ngongcolileyo amaviki amabili, njengokwehlukaniswa kwakhe; uzahlala insuku ezingamatshumi ayisithupha lesithupha egazini lokuhlanjululwa kwakhe.
Ngati abala mwana wamkazi, adzakhala wodetsedwa kwa masabata awiri, monga zikhalira pa nthawi yake yosamba. Ndipo mkaziyo adikire masiku ena 66, kuti ayeretsedwe ku matenda akewo.
6 Lapho sezigcwalisekile insuku zokuhlanjululwa kwakhe, ngendodana loba ngendodakazi, uzaletha iwundlu elilomnyaka owodwa, libe ngumnikelo wokutshiswa, lephuphu lenkwilimba kumbe ijuba kube ngumnikelo wesono, emnyango wethente lenhlangano, kumpristi,
“‘Masiku ake wodziyeretsa akatha, kaya ndi a mwana wamwamuna kapena a mwana wamkazi, abwere kwa wansembe ndi mwana wankhosa wa chaka chimodzi pa khomo la tenti ya msonkhano kuti ikhale nsembe yopsereza. Abwerenso ndi chiwunda cha nkhunda kapena njiwa kuti ikhale nsembe yopepesera machimo.
7 ozakunikela eNkosini, amenzele inhlawulo yokuthula; khona ezahlambuluka ekopheni kwegazi lakhe. Lo ngumlayo walowo obeletha owesilisa loba owesifazana.
Wansembeyo apereke zimenezi pamaso pa Yehova pochita mwambo wopepesera mkaziyo. Ndipo mkaziyo adzakhala woyeretsedwa ku msambo wake. “‘Amenewa ndiwo malamulo a mkazi amene wabala mwana wamwamuna kapena wamkazi.
8 Kodwa uba isandla sakhe singatholi okwanela imvu, uzathatha amajuba amabili loba amaphuphu amabili enkwilimba, okunye kube ngumnikelo wokutshiswa lokunye kube ngumnikelo wesono, lompristi amenzele inhlawulo yokuthula, aze ahlambuluke.
Ngati mkaziyo sangathe kupeza mwana wankhosa, abwere ndi njiwa ziwiri kapena mawunda ankhunda awiri: imodzi ikhale ya nsembe yopsereza ndipo inayo ikhale ya nsembe yopepesera machimo. Tsono wansembe achite mwambo wopepesera wa mkaziyo ndipo adzayeretsedwa.’”

< ULevi 12 >