< UHoseya 5 >

1 Zwanini lokhu, bapristi, lilalele, ndlu kaIsrayeli, libeke indlebe, lani ndlu yenkosi. Ngoba isahlulelo singakini, ngoba selibe ngumjibila eMizipa, lembule elendlalwe phezu kweThabhori.
“Ansembe inu, imvani izi! Inu Aisraeli, tcherani khutu! Inu nyumba yaufumu, mvetserani! Chiweruzo ichi ndi chotsutsa inu: Inu munali ngati msampha ku Mizipa, munali ngati ukonde woyalidwa pa phiri la Tabori.
2 Labahlamuki batshonisa ukuhlaba, kodwa ngizakuba ngumlayi wabo bonke.
Owukira azama mʼmoyo wakupha, Ine ndidzawalanga onsewo.
3 Mina ngiyamazi uEfrayimi, loIsrayeli kafihlakalanga kimi; ngoba khathesi ufebile, wena Efrayimi, uIsrayeli uzingcolisile.
Ndimadziwa zonse za Efereimu; Aisraeli ndi osabisika kwa Ine. Efereimu wayamba tsopano kuchita zachiwerewere; Israeli wadziyipitsa.
4 Kabaqondisi izenzo zabo ukuze baphendukele kuNkulunkulu wabo, ngoba umoya wokuwula uphakathi kwabo, leNkosi kabayazi.
“Ntchito zawo siziwalola kubwerera kwa Mulungu wawo. Mʼmitima mwawo muli mzimu wachiwerewere; Iwo sadziwa Yehova.
5 Lokuzigqaja kukaIsrayeli kuyafakaza ebusweni bakhe; ngakho uIsrayeli loEfrayimi bazakhubeka esiphambekweni sabo, loJuda uzakhubeka kanye labo.
Kudzikuza kwa Israeli kwakhala umboni womutsutsa; Aisraeli, ngakhale Aefereimu, anagwa mʼmachimo awo; Yudanso anagwa nawo pamodzi.
6 Bazahamba lezimvu zabo lenkomo zabo ukuyadinga iNkosi, kodwa kabayikuyithola; imonyukile kubo.
Pamene adzapita ndi nkhosa zawo ndi ngʼombe zawo kukapereka nsembe kwa Yehova, iwo sadzamupeza; Iye wawachokera.
7 Benze ngenkohliso ngakuyo iNkosi, ngoba bazele abantwana bezizweni. Khathesi inyanga ethwasayo izabaqeda lezabelo zabo.
Iwo ndi osakhulupirika kwa Yehova; amabereka ana amʼchigololo ndipo chikondwerero chawo cha mwezi watsopano chidzawawononga pamodzi ndi minda yawo.
8 Vuthelani uphondo lwenqama eGibeya, uphondo eRama, lihlabe umkhosi eBeti-Aveni lithi: Emva kwakho, wena Bhenjamini.
“Womba lipenga mu Gibeya, liza mbetete mu Rama. Fuwulani mfuwu wankhondo mu Beti-Aveni; iwe Benjamini tsogolera.
9 UEfrayimi uzakuba yincithakalo ngosuku lokujeziswa; phakathi kwezizwe zakoIsrayeli ngikwazisile okuliqiniso.
Efereimu adzasanduka bwinja pa tsiku la chilango. Ine ndikulengeza zomwe zidzachitikadi pakati pa mafuko a Israeli.
10 Iziphathamandla zakoJuda sezinjengalabo abatshedisa umngcele; ngizathululela phezu kwabo ulaka lwami njengamanzi.
Atsogoleri a Yuda ali ngati anthu amene amasuntha miyala ya mʼmalire. Ndidzawakhutulira ukali wanga ngati madzi a chigumula.
11 UEfrayimi ucindezelwe wachotshozwa ngesahlulelo, ngoba wavuma ukuhamba elandela umlayo.
Efereimu waponderezedwa, akulangidwa chifukwa chotsatira mafano.
12 Ngakho ngizakuba njengenundu koEfrayimi, lanjengokubola endlini yakoJuda.
Ine ndili ngati njenjete kwa Efereimu, ngati chinthu chowola kwa anthu a ku Yuda.
13 Kwathi uEfrayimi ebona umkhuhlane wakhe, loJuda isilonda sakhe, uEfrayimi waya eAsiriya, wathumela ilizwi enkosini yeJarebhi; kodwa yona kayiyikuba lakho ukulelapha, kayiyikupholisa isilonda senu.
“Efereimu ataona nthenda yake, ndi Yuda ataona zilonda zake, pamenepo Efereimu anatembenukira kwa Asiriya, ndipo anawatumizira mfumu yayikulu kudzawathandiza. Koma mfumuyo singathe kukuchizani, singathe kuchiritsa mabala anu.
14 Ngoba ngizakuba njengesilwane koEfrayimi, lanjengebhongo lesilwane endlini yakoJuda. Mina, uqobo lwami, ngizadabudabula, besengihamba, ngisuse, kungabi lomophuli.
Pakuti Ine ndidzakhala ngati mkango kwa Efereimu. Ngati mkango wamphamvu kwa Yuda. Ndidzawakhadzula nʼkuchokapo; ndidzawatenga ndipo palibe amene adzawalanditse.
15 Ngizahamba ngibuyele endaweni yami, baze bavume icala labo, badinge ubuso bami; ekucindezelweni kwabo bazangidinga ngovivi.
Ndipo ndidzabwerera ku malo anga mpaka anthu anga atavomereza kulakwa kwawo. Ndipo iwo adzafunafuna nkhope yanga; mʼmasautso awo adzandifunitsitsa Ine.”

< UHoseya 5 >