< 1 Imilando 7 >

1 Lemadodaneni kaIsakari: OThola, loPhuwa, uJashubi, loShimroni; bebane.
Ana a Isakara anali awa: Tola, Puwa, Yasubu ndi Simironi ndipo onse analipo anayi.
2 Njalo amadodana kaThola: OUzi, loRefaya, loJeriyeli, loJahimayi, loIbisamu, loShemuweli, izinhloko zendlu yaboyise, abakoThola, amaqhawe alamandla ezizukulwaneni zabo; inani labo ensukwini zikaDavida laliyizinkulungwane ezingamatshumi amabili lambili lamakhulu ayisithupha.
Ana a Tola ndi awa: Uzi, Refaya, Yerieli, Yahimai, Ibisamu ndi Samueli. Awa anali atsogoleri a mabanja awo. Pa nthawi ya ulamuliro wa Davide zidzukulu za Tola zomwe zinali anthu odziwa kumenya nkhondo zinalipo 22,600.
3 Lamadodana kaUzi: UIzrahiya. Lamadodana kaIzrahiya: OMikayeli, loObhadiya, loJoweli, uIshiya, bebahlanu; beyizinhloko bonke.
Mwana wa Uzi anali Izirahiya. Ana a Izirahiya anali: Mikayeli, Obadiya, Yoweli ndi Isiya. Onse asanu anali atsogoleri a mabanja.
4 Kanye labo-ke, ngensendo zabo, ngendlu yaboyise, kwakukhona amaviyo ebutho lempi, izinkulungwane ezingamatshumi amathathu lesithupha, ngoba babelabafazi labantwana abanengi.
Monga mwa chiwerengero cha mabanja awo, panali anthu 36,000 odziwa kumenya nkhondo, pakuti iwo anali ndi akazi ndi ana ambiri.
5 Labafowabo, phakathi kwensendo zonke zakoIsakari, amaqhawe alamandla, izinkulungwane ezingamatshumi ayisificaminwembili lesikhombisa, bebhalwe bonke ngezizukulwana.
Abale awo onse a mʼbanja la Isakara amene anali odziwa kumenya nkhondo analipo 87,000, olembedwa potsata mibado yawo.
6 Amadodana kaBhenjamini: OBhela, loBekeri loJediyayeli, bebathathu.
Ana atatu a Benjamini anali awa: Bela, Bekeri ndi Yediaeli.
7 Lamadodana kaBhela: OEziboni, loUzi, loUziyeli, loJerimothi, loIri, bebahlanu; izinhloko zendlu zaboyise, amaqhawe alamandla; bebhalwe ngezizukulwana, babeyizinkulungwane ezingamatshumi amabili lambili lamatshumi amathathu lane.
Ana a Bela anali awa: Eziboni, Uzi, Uzieli, Yerimoti ndi Iri. Iwowa anali atsogoleri a mabanja awo ndipo onse pamodzi analipo asanu. Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali anthu 22,034 odziwa kumenya nkhondo.
8 Njalo amadodana kaBekeri: OZemira, loJowashi, loEliyezeri, loEliyohenayi, loOmri, loJeremothi, loAbhiya, loAnathothi, loAlemethi; bonke laba babengamadodana kaBekeri.
Ana a Bekeri anali awa: Zemira, Yowasi, Eliezara, Eliyoenai, Omiri, Yeremoti, Abiya, Anatoti ndi Alemeti. Onsewa anali ana a Bekeri.
9 Bebhalwe ngensendo ngezizukulwana zabo, izinhloko zezindlu zaboyise, amaqhawe alamandla, babezinkulungwane ezingamatshumi amabili lamakhulu amabili.
Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali atsogoleri a mabanja ndi anthu 20,200 odziwa kumenya nkhondo.
10 Njalo amadodana kaJediyayeli: UBilihani. Lamadodana kaBilihani: OJewushi, loBhenjamini, loEhudi, loKenahana, loZethani, loTarshishi, loAhishahari.
Mwana wa Yediaeli anali Bilihani. Ana a Bilihani anali awa: Yeusi, Benjamini, Ehudi, Kenaana, Zetani, Tarisisi ndi Ahisahara.
11 Bonke laba babengamadodana kaJediyayeli, ngezinhloko zaboyise, amaqhawe alamandla; babeyizinkulungwane ezilitshumi lesikhombisa lamakhulu amabili, angaphuma ebuthweni ukuya empini.
Ana onsewa a Yediaeli anali atsogoleri a mabanja. Analipo anthu 17,200 amene anali okonzeka kupita ku nkhondo.
12 LoShupimi loHupimi babengamadodana kaIri, loHushimi amadodana kaAheri.
Asupi ndi Ahupi anali zidzukulu za Iri, ndipo Ahusimu anali zidzukulu za Aheri.
13 Amadodana kaNafithali: OJahaziyeli, loGuni, loJezeri, loShaluma, amadodana kaBiliha.
Ana a Nafutali anali awa: Yahazieli, Guni, Yezeri ndi Salumu, zidzukulu za Biliha.
14 Amadodana kaManase: UAsiriyeli umkakhe amzalayo. (Umfazi wakhe omncinyane umAramukazi wazala uMakiri uyise kaGileyadi.
Ana a Manase anali awa: Asirieli ndi mwana amene anabereka kwa mzikazi wake wa ku Aramu. Mzikazi yemweyo anaberekanso Makiri abambo ake a Giliyadi.
15 UMakiri wathatha udadewabo kaHupimi loShupimi, waba ngumkakhe, obizo lakhe nguMahaka.) Lebizo leyesibili lalinguZelofehadi; njalo uZelofehadi wayelamadodakazi.
Makiri anatenga mkazi wa banja la Ahupi ndi Asupi. Mlongo wake anali Maaka. Mwana wake wina anali Zelofehadi, amene anabereka ana aakazi okhaokha.
16 UMahaka umkaMakiri wasezala indodana, wayitha ibizo wathi nguPereshi; lebizo lomfowabo lalinguShereshi, lamadodana akhe ayengoUlamu loRakema.
Maaka mkazi wa Makiri anabereka mwana wamwamuna ndipo anamutcha Perezi. Mʼbale wake anamutcha Seresi, ndipo ana ake anali Ulamu ndi Rakemu.
17 Njalo amadodana kaUlamu: UBedani. La ayengamadodana kaGileyadi indodana kaMakiri indodana kaManase.
Mwana wa Ulamu anali Bedani. Awa anali ana a Giliyadi mwana wa Makiri, mwana wa Manase.
18 Udadewabo uHamolekethi wasezala oIshodi loAbiyezeri loMahla.
Mlongo wake Hamoleketi anabereka Isihodi, Abiezeri ndi Mahila.
19 Lamadodana kaShemida ayengoAhiyani loShekema loLikhi loAniyamu.
Ana a Semida anali: Ahiyani, Sekemu, Likihi ndi Aniyamu.
20 Njalo amadodana kaEfrayimi: OShuthela, loBeredi indodana yakhe, loTahathi indodana yakhe, loEleyada indodana yakhe, loTahathi indodana yakhe,
Ana a Efereimu anali awa: Sutela, Beredi, Tahati, Eliada, Tahati,
21 loZabadi indodana yakhe, loShuthela indodana yakhe, loEzeri loEleyadi, amadoda eGathi azalelwa kulelolizwe abababulalayo, ngoba behlela ukuthatha izifuyo zabo.
Zabadi, Sutela. Ezeri ndi Eladi anaphedwa ndi anthu a ku Gati, pamene anabwera kudzalanda zoweta zawo.
22 UEfrayimi uyise walila insuku ezinengi; abafowabo basebesiza ukuzamduduza.
Efereimu, abambo awo, anawalira masiku ambiri, ndipo abale ake anabwera kudzamutonthoza.
23 Wasengena kumkakhe; wathatha isisu, wazala indodana; waseyitha ibizo wathi nguBeriya, ngoba wayesebubini endlini yakhe.
Kenaka anagona ndi mkazi wake, ndipo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Anamutcha dzina lake Beriya, chifukwa tsoka linagwera banja lake.
24 Lendodakazi yakhe yayinguShera, owakha iBethi-Horoni engaphansi lengaphezulu, leUzeni-Shera.
Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera.
25 Njalo uRefa wayeyindodana yakhe, loReshefi, loTela indodana yakhe, loTahani indodana yakhe,
Mwana wina wa Efereimu anali Refa amene zidzukulu zake zinali Resefu, Tela, Tahani,
26 uLadani indodana yakhe, uAmihudi indodana yakhe, uElishama indodana yakhe,
Ladani, Amihudi, Elisama,
27 uNoni indodana yakhe, uJoshuwa indodana yakhe.
Nuni ndi Yoswa.
28 Lemfuyo yawo lendawo zawo zokuhlala kwakuyiBhetheli lemizana yayo, langempumalanga iNaharani, langentshonalanga iGezeri lemizana yayo, leShekema lemizana yayo, kwaze kwaba seAya lemizana yayo.
Malo amene ankakhala anali Beteli ndi midzi yozungulira, cha kummawa kunali Naarani, Gezeri ndi midzi yake ya kumadzulo ndi Sekemu ndi midzi yake mpaka ku Aya ndi midzi yake.
29 Lasemingceleni yabantwana bakoManase, iBeti-Sheyani lemizana yayo, iThahanakhi lemizana yayo, iMegido lemizana yayo, iDori lemizana yayo. Kule kwahlala abantwana bakoJosefa indodana kaIsrayeli.
Mʼmbali mwa malire a Manase munali Beti-Seani, Taanaki, Megido ndi Dori, pamodzi ndi midzi yake. Zidzukulu za Yosefe mwana wa Israeli zimakhala mʼmizinda imeneyi.
30 Abantwana bakaAsheri: OImina, loIshiva, loIshivi, loBeriya, loSera udadewabo.
Ana a Aseri anali awa: Imuna, Isiva, Isivi ndi Beriya. Mlongo wawo anali Sera.
31 Njalo amadodana kaBeriya: OHeberi, loMalikiyeli onguyise kaBirizayithi.
Ana a Beriya anali awa: Heberi ndi Malikieli amene anabereka Birizaiti.
32 UHeberi wasezala oJafilethi loShomeri loHothamu loShuwa udadewabo.
Heberi anabereka Yafuleti, Someri, Hotamu ndi Suwa, mlongo wawo.
33 Lamadodana kaJafilethi: OPasaki loBimihali loAshivathi; la ngamadodana kaJafilethi.
Ana a Yafuleti anali awa: Pasaki, Bimuhali ndi Asivati. Awa anali ana a Yafuleti.
34 Lamadodana kaShemeri: OAhi, loRohiga, uJehuba, loAramu.
Ana a Someri anali awa: Ahi, Rohiga, Yehuba ndi Aramu.
35 Njalo amadodana kaHelemu umfowabo: OZofa loImina loSheleshi loAmali.
Ana a mʼbale wake Helemu anali awa: Zofa, Imuna, Selesi ndi Amali.
36 Njalo amadodana kaZofa: OSuwa, loHarineferi, loShuwali, loBeri, loImra,
Ana a Zofa anali awa: Suwa, Harineferi, Suwali, Beri, Imula,
37 uBezeri, loHodi, loShama, loShilisha, loIthirani, loBehera.
Bezeri, Hodi, Sama, Silisa, Itirani ndi Bera.
38 Njalo amadodana kaJetheri: OJefune loPisipa loAra.
Ana a Yeteri anali awa: Yefune, Pisipa ndi Ara.
39 Njalo amadodana kaUla: OAra loHaniyeli loRiziya.
Ana a Ula anali awa: Ara, Hanieli ndi Riziya.
40 Bonke laba babengabantwana bakaAsheri, izinhloko zendlu yaboyise, abakhethiweyo, amaqhawe alamandla, izinhloko zeziphathamandla. Basebebhalwa ngezizukulwana ebuthweni empini; inani labo lalingamadoda azinkulungwane ezingamatshumi amabili lesithupha.
Onsewa anali zidzukulu za Aseri, atsogoleri a mabanja, anthu omveka, ankhondo olimba mtima, ndi akuluakulu pakati pa atsogoleri anzawo. Chiwerengero cha anthu odziwa kumenya nkhondo chomwe chinalembedwa chinali 26,000.

< 1 Imilando 7 >