< 1 Imilando 3 >

1 Njalo la ayengamadodana kaDavida awazalelwa eHebroni: Izibulo nguAmnoni kuAhinowama umJizereyelikazi; eyesibili nguDaniyeli kuAbigayili umKharmelikazi;
Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa: Woyamba anali Amnoni, amayi ake anali Ahinoamu wa ku Yezireeli; wachiwiri anali Danieli, amayi ake anali Abigayeli wa ku Karimeli;
2 eyesithathu nguAbisalomu indodana kaMahaka indodakazi kaTalimayi inkosi yeGeshuri; eyesine nguAdonija indodana kaHagithi;
wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri; wachinayi anali Adoniya amayi ake anali Hagiti;
3 eyesihlanu nguShefathiya kuAbithali; eyesithupha nguIthereyamu kuEgila umkakhe.
wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali; wachisanu ndi chimodzi anali Itireamu, amayi ake anali Egila.
4 Abayisithupha bazalelwa yena eHebroni, lapho abusa khona iminyaka eyisikhombisa lezinyanga eziyisithupha; leJerusalema wabusa iminyaka engamatshumi amathathu lantathu.
Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi. Davide analamuliranso mu Yerusalemu kwa zaka 33,
5 Lalaba bazalelwa yena eJerusalema: OShimeya loShobabi loNathani loSolomoni, bobane, kuBathishuwa indodakazi kaAmiyeli;
ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa: Samua, Sobabu, Natani ndi Solomoni. Ana anayi awa anali a Batisuwa mwana wa Amieli.
6 loIbihari loElishama loElifelethi
Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,
7 loNoga loNefegi loJafiya
Noga, Nefegi, Yafiya,
8 loElishama loEliyada loElifelethi, abayisificamunwemunye.
Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.
9 Bonke babengamadodana kaDavida, ngaphandle kwamadodana abafazi abancane, loTamari udadewabo.
Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.
10 Lendodana kaSolomoni yayinguRehobhowamu, uAbhiya indodana yakhe, uAsa indodana yakhe, uJehoshafathi indodana yakhe,
Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu, Rehabiamu anabereka Abiya, Abiya anabereka Asa, Asa anabereka Yehosafati,
11 uJoramu indodana yakhe, uAhaziya indodana yakhe, uJowashi indodana yakhe,
Yehosafati anabereka Yehoramu, Yehoramu anabereka Ahaziya, Ahaziya anabereka Yowasi,
12 uAmaziya indodana yakhe, uAzariya indodana yakhe, uJothamu indodana yakhe,
Yowasi anabereka Amaziya, Amaziya anabereka Azariya, Azariya anabereka Yotamu,
13 uAhazi indodana yakhe, uHezekhiya indodana yakhe, uManase indodana yakhe,
Yotamu anabereka Ahazi, Ahazi anabereka Hezekiya, Hezekiya anabereka Manase,
14 uAmoni indodana yakhe, uJosiya indodana yakhe.
Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.
15 Njalo amadodana kaJosiya: Izibulo uJohanani, eyesibili uJehoyakhimi, eyesithathu uZedekhiya, eyesine uShaluma.
Ana a Yosiya anali awa: Yohanani mwana wake woyamba, Yehoyakimu mwana wake wachiwiri, Zedekiya mwana wake wachitatu, Salumu mwana wake wachinayi.
16 Lamadodana kaJehoyakhimi: UJekoniya indodana yakhe, uZedekhiya indodana yakhe.
Ana a Yehoyakimu: Yekoniya ndi Zedekiya mwana wake.
17 Njalo amadodana kaJekoniya: UAsiri, uSheyalitiyeli indodana yakhe,
Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi: mwana wake Silatieli,
18 loMalikiramu, loPhedaya, loShenazari, uJekamiya, uHoshama, loNedabiya.
Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.
19 Njalo amadodana kaPhedaya: OZerubhabheli loShimeyi. Lamadodana kaZerubhabheli: OMeshulamu, loHananiya, loShelomithi udadewabo;
Ana a Pedaya anali awa: Zerubabeli ndi Simei. Ana a Zerubabeli anali awa: Mesulamu ndi Hananiya. Mlongo wawo anali Selomiti.
20 loHashuba, loOheli, loBerekiya, loHasadiya, uJushabi-Hesedi, amahlanu.
Panalinso ana ena asanu awa: Hasubu, Oheli, Berekiya, Hasabiya ndi Yusabu-Hesedi.
21 Lamadodana kaHananiya: OPelatiya loJeshaya; amadodana kaRefaya, amadodana kaArinani, amadodana kaObhadiya, amadodana kaShekaniya.
Zidzukulu za Hananiya zinali izi: Pelatiya ndi Yesaiya, ndiponso ana a Refaya, ana a Arinani, ana a Obadiya ndi ana a Sekaniya.
22 Lamadodana kaShekaniya: UShemaya. Lamadodana kaShemaya: OHathushi loIgali loBariya loNeyariya loShafati, ayisithupha.
Zidzukulu za Sekaniya zinali izi: Semaya ndi ana ake: Hatusi, Igala, Bariya, Neariya ndi Safati. Onse anali asanu ndi mmodzi.
23 Njalo amadodana kaNeyariya: OEliyohenayi loHizikiya loAzirikamu, amathathu.
Ana a Neariya anali awa: Eliyoenai, Hezekiya ndi Azirikamu. Onse anali atatu.
24 Njalo amadodana kaEliyohenayi: OHodaviya loEliyashibi loPelaya loAkubi loJohanani loDelaya loAnani, ayisikhombisa.
Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu, Yohanani, Delaya ndi Anani, onse anali asanu ndi awiri.

< 1 Imilando 3 >