< Amahubo 61 >
1 Kumqondisi wokuhlabela. Kutshaywa iziginci. ElikaDavida. Zwana ukukhala kwami, Oh Nkulunkulu; lalela umkhuleko wami.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Loyimbidwa ndi zipangizo za zingwe. Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu; mvetserani pemphero langa.
2 Ngisemkhawulweni womhlaba ngiyakubiza, ngiyabiza lapho inhliziyo yami isiphela amandla; ngikhokhelela edwaleni eliphakeme kulami.
Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu ndimayitana pomwe mtima wanga ukufowoka; tsogolereni ku thanthwe lalitali kuposa ineyo.
3 Ngoba ube uyisiphephelo sami, inqaba eqinileyo evikela esitheni.
Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga, nsanja yolimba polimbana ndi adani anga.
4 Ngiyalangazelela ukuhlala ethenteni lakho laphakade ngizifihle emthunzini wamaphiko akho.
Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya ndi kupeza chitetezo mu mthunzi wa mapiko anu.
5 Phela usuzizwile izifungo zami, Oh Nkulunkulu; usungiphile ilifa lalabo abalesabayo ibizo lakho.
Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga; mwandipatsa cholowa cha iwo amene amaopa dzina lanu.
6 Yandisa insuku zempilo yenkosi, iminyaka yayo okwezizukulwane ezinengi.
Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu, zaka zake kwa mibado yochuluka.
7 Sengathi ingaba sesihlalweni iphambi kukaNkulunkulu nini lanini; wabele uthando Lwakho lokuthembeka Kwakho kuyivikele.
Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya; ikani chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu kuti zimuteteze.
8 Lapho-ke ngizahlala ngihlabelela indumiso ebizweni Lakho ngigcwalise izifungo zami insuku ngensuku.
Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu ndi kukwaniritsa malumbiro anga tsiku ndi tsiku.