< UDutheronomi 8 >

1 “Nanzelelani njalo lilandele yonke imilayo engilinika yona lamuhla, ukuze liphile njalo lande khona lizangena lithumbe ilizwe uThixo alinika okhokho benu ethembisa ngesifungo.
Samalani potsata lamulo lililonse limene ndikukupatsani lero, kuti mukhale ndi moyo ndi kuchulukana kuti mulande ndi kulowa mʼdziko limene Yehova analumbira kuti adzapereka kwa makolo anu.
2 Likhumbule ukuthi uThixo uNkulunkulu wenu walikhokhela njani lidabula inkangala okweminyaka engamatshumi amane, elichumisa lokulilinga ukuthi abone okwakusezinhliziyweni zenu, ukuthi kambe lizayigcina imiyalo yakhe na loba hayi.
Kumbukirani mmene Yehova Mulungu wanu anakutsogolerani njira yonse mʼchipululu kwa zaka makumi anayi, kukutsitsani ndi kukuyesani kuti adziwe chimene chinali mu mtima mwanu ngati mungathe kusunga malamulo ake kapena ayi.
3 UThixo walichumisa, walenza lalamba kanti njalo walipha ukudla okuyimana, ukudla lokho laboyihlo abangazange bakwazi, kuyikulifundisa ukuthi umuntu kaphili ngesinkwa kuphela zwi kodwa ngalo lonke ilizwi eliphuma emlonyeni kaThixo.
Iye anakutsitsani nakumvetsani njala kenaka nʼkukudyetsani mana amene anali osadziwika kwa inu kapena makolo anu, kuti akuphunzitseni kuti munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha koma ndi mawu aliwonse ochokera mʼkamwa mwa Yehova.
4 Izigqoko zenu aziguganga njalo lezinyawo zenu azivuvukanga kuleyo minyaka engamatshumi amane.
Mʼzaka makumi anayi zimenezi, zovala zanu sizinangʼambike ndipo mapazi anu sanatupe.
5 Gcinani lokhu ezinhliziyweni zenu lazi ukuthi njengendoda ikhuza indodana yayo, ngokufananayo uThixo uNkulunkulu wenu uyalikhuza.
Tsono dziwani mu mtima mwanu kuti monga abambo amalanga mwana wawo, momwemonso Yehova Mulungu wanu amakulangani.
6 Gcinani imilayo kaThixo uNkulunkulu wenu lihambe endleleni yakhe njalo limkhonze.
Samalirani malamulo a Yehova Mulungu wanu, kuyenda mʼnjira yake ndi kumuopa Iye.
7 Ngakho uThixo uNkulunkulu wenu ulisa elizweni elihle, ilizwe elilezifula leziziba zamanzi, intombo zamanzi ezimpompoza ezigodini lasemaqaqeni;
Pakuti Yehova Mulungu wanu akukulowetsani mʼdziko labwino, dziko lokhala ndi mitsinje ndi mathawale a madzi, akasupe oyenderera mu zigwa ndi mʼmapiri,
8 elizweni lengqoloyi lebhali, amavini lemikhiwa, amaphomegranathi, amafutha ama-oliva lenyosi;
dziko lokhala ndi tirigu ndi barele, mpesa ndi mitengo ya mkuyu, makangadza, mafuta a olivi ndi uchi;
9 elizweni lapha okungasayi kusweleka khona isinkwa njalo aliyikuswela lutho; elizweni lapho amatshe akhona ayinsimbi kanti njalo lingemba ikhopha emaqaqeni.
dziko limene buledi sadzasowa ndipo simudzasowa chilichonse; dziko limene miyala yake ndi chitsulo ndipo ku mapiri ake mukhoza kukumbako mkuwa.
10 Lizakuthi selidlile lasutha, lidumise uThixo uNkulunkulu wenu ngelizwe elihle alinike lona.
Mukadya ndi kukhuta, yamikani Yehova Mulungu wanu chifukwa cha dziko labwino limene wakupatsani.
11 Linanzelele ukuthi alilibali uThixo uNkulunkulu wenu, lingehluleki ukugcina imilayo yakhe, imithetho kanye lezimiso engilinika zona lamuhla.
Samalani kuopa kuti mungayiwale Yehova Mulungu wanu posasunga malamulo, zikhazikitso ndi malangizo ake amene ndikukupatsani lero,
12 Kungenzeka ukuthi lithi selidlile lasutha, selakhe izindlu ezinhle lahlala lazinza,
kuopa kuti mukadya ndi kukhuta, mukamanga nyumba zabwino ndi kukhalamo,
13 njalo imihlambi yezifuyo zenu leyezimvu zenu isiqhelile yanda kuze kuthi lesiliva legolide lenu selilinengi kanye lakho konke okwenu sekukunengi kuphindwe kanenginengi,
ndi pamene ngʼombe zanu ndi nkhosa zanu zaswana, ndi siliva ndi golide wanu wachuluka ndiponso kuti zonse zimene muli nazo zachuluka,
14 liziqhenye ezinhliziyweni zenu, libe selikhohlwa uThixo uNkulunkulu wenu, yena owalikhupha eGibhithe, walikhupha elizweni lobugqili.
mtima wanu udzayamba kunyada ndi kuyiwala Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto, kukuchotsani ku dziko la ukapolo.
15 UThixo walikhokhela enkangala enkulu eyesabekayo, eyomileyo engelamanzi, elobuthi benyoka lenkume. Walinika amanzi aphuma edwaleni.
Iye anakutsogolerani kudutsa mʼchipululu chachikulu ndi chochititsa mantha, dziko lija la ludzu ndi lopanda madzi, lokhala ndi njoka zaululu ndi zinkhanira. Iye anatulutsa madzi kuchokera mʼthanthwe lowuma.
16 Walinika imana ukuba lidle enkangala, into abangazange bayazi oyihlo, ukulichumisa njalo lokulilinga ukuze kuthi ekucineni kulihambele kuhle.
Iye anakupatsani mana kuti mudye mʼchipululu, zinthu zoti ngakhale makolo anu sanazidziwe, kuti akuchepetseni ndi kukuyesani ndipo kuti pa mapeto pake zikuyendereni bwino.
17 Mhlawumbe lingathi, ‘Ngokuzimisela kwami langamandla ezandla zami sengizidalele inotho.’
Mu mtima mwanu mukhoza kuganiza kuti, “Mphamvu zanga ndi kulimbika kwa dzanja langa ndi zimene zandilemeretsa chonchi.”
18 Kodwa khumbulani uThixo uNkulunkulu wenu ngoba kunguye olipha amandla okunotha, lokho kuyikho ukugcwaliseka kwesivumelwano sakhe, sona afunga kubokhokho benu, okulokhu kunjalo lalamuhla.
Koma kumbukirani Yehova Mulungu chifukwa ndi amene amakupatsani mphamvu zopezera chuma chimenechi kuti atsimikize pangano limene analumbira kwa makolo anu, monga liliri lero lino.
19 Nxa lizake likhohlwe uThixo uNkulunkulu wenu beselilandela abanye onkulunkulu libakhonze libakhothamele, ngiyalifungela lamuhla ukuthi lizabhujiswa ngempela.
Ine ndine mboni yokutsutsani lero lino, kuti mukayiwala Yehova Mulungu wanu ndi kutsata milungu ina nʼkumayigwadira, mudzawonongeka ndithu.
20 Njengezizwe uThixo azibhubhisa phambi kwenu lani lizabhujiswa nguThixo uNkulunkulu wenu.”
Monga mitundu ina ya anthu imene Yehova anayiwononga pamaso panu, inunso mudzawonongedwa chifukwa chosamvera Yehova Mulungu wanu.

< UDutheronomi 8 >