< 1 Imilando 14 >
1 Ngalesosikhathi uHiramu inkosi yaseThire wathumela izithunywa kuDavida, ndawonye lezigodo zomsedari, ababazi bamatshe kanye lababazi ukuthi bayemakhela isigodlo.
Hiramu mfumu ya ku Turo inatumiza amithenga kwa Davide pamodzi ndi mitengo ya mkungudza ndiponso amisiri a miyala ndi amisiri a matabwa kuti adzamumangire nyumba yaufumu.
2 UDavida wahle wakwazi ukuthi uThixo usembekile ukuba abe yinkosi ka-Israyeli lokuthi umbuso wakhe uphakanyisiwe kakhulu ngenxa yabantu bakhe bako-Israyeli.
Choncho Davide anazindikira kuti Yehova wamukhazikitsa kukhala mfumu ya Israeli ndipo wakuza kwambiri ufumu wake chifukwa cha anthu ake, Aisraeli.
3 EJerusalema uDavida wathatha abanye abafazi wazala amanye amadodana lamadodakazi.
Davide anakwatira akazi ena ambiri ku Yerusalemu ndipo anabereka ana aamuna ndi aakazi ambiri.
4 Nanka amabizo abantwana abazalelwa khona: uShamuwa, uShobabi, uNathani, uSolomoni,
Mayina a ana amene anaberekera ku Yerusalemu anali awa: Samua, Sobabu, Natani, Solomoni,
5 u-Ibhari, u-Elishuwa, u-Eliphelethi,
Ibihari, Elisua, Elipeleti,
6 uNoga, uNefegi, uJafiya,
Noga, Nefegi, Yafiya,
7 u-Elishama, uBheyeliyada kanye lo-Elifelethi.
Elisama, Beeliada ndi Elifeleti.
8 AmaFilistiya athi esizwa ukuthi uDavida usegcotshwe ukuba yinkosi yalo lonke elako-Israyeli, aphuma wonke ehlome ephelele esiyamzingela, kodwa uDavida wakuzwa lokho wahle waphuma yena ukuyawahlangabeza.
Afilisti atamva kuti Davide wadzozedwa kukhala mfumu ya dziko lonse la Israeli, iwo anapita mwamphamvu kukamusakasaka. Koma Davide atamva zimenezi anapita kukakumana nawo.
9 AmaFilistiya ayesefikile njalo ukuyahlasela eSigodini saseRefayi;
Ndipo Afilisti anabwera ndi kulanda zinthu mʼChigwa cha Refaimu.
10 ngakho uDavida wabuza kuNkulunkulu wathi: “Ngihambe ngiyewahlasela amaFilistiya na? Uzawanikela kimi na?” UThixo wamphendula wathi, “Hamba, ngizawanikela kuwe.”
Davide anafunsa Mulungu kuti, “Kodi ndipite kukathira nkhondo Afilisti? Kodi mukawapereka mʼmanja mwanga?” Yehova anamuyankha kuti, “Pita, Ine ndidzawapereka mʼmanja mwako.”
11 Ngakho uDavida lamabutho akhe aya eBhali Pherazimi lapho awehlula khona. Wathi: “Njengamanzi efohla, uNkulunkulu ufohlele ezitheni zami ngesandla sami.” Ngakho leyondawo yasibizwa ngokuthi yiBhali Pherazimi.
Choncho Davide ndi anthu ake anapita ku Baala-Perazimu ndi kugonjetsa Afilistiwo. Iye anati, “Monga amasefukira madzi, Mulungu waphwanya adani anga ine ndikuona.” Motero anawatcha malowa Baala Perazimu.
12 AmaFilistiya ayebaleke atshiya onkulunkulu bawo khonale, uDavida wathi kabatshiswe ngomlilo.
Afilisti anasiya milungu yawo kumeneko ndipo Davide analamulira kuti itenthedwe ndi moto.
13 AmaFilistiya aphinda njalo ukuhlasela isigodi,
Nthawi inanso Afilisti anadzalanda katundu mu Chigwamo.
14 ngakho uDavida wabuza kuNkulunkulu njalo, uNkulunkulu wamphendula wathi, “Ungasuki uqonde phambili kodwa bazingeleze ubusubahlasela uvelela ezihlahleni zebhalisamu.
Choncho Davide anafunsa Mulungu ndipo Mulunguyo anayankha kuti, “Usapite molunjika, koma uzungulire kumbuyo kwawo. Ukawathire nkhondo patsogolo pa mitengo ya mkandankhuku.
15 Kuzakuthi lapho usizwa izisinde zabahambayo ezihlahleni zebhalisamu, uphume uhlasele, ngoba lokho kuzabe kusitsho ukuthi uNkulunkulu usehambe phambi kwakho ukuyanqoba amabutho amaFilistiya.”
Mukakangomva phokoso pa msonga za mitengo ya mkandankhuku, mukapite kukamenyana nawo, chifukwa izi zikasonyeza kuti Mulungu ali patsogolo panu kukantha ankhondo a Afilisti.”
16 Ngakho uDavida wenza njengokulaywa kwakhe nguNkulunkulu, njalo bawacakazela phansi amaFilistiya umango wonke kusukela eGibhiyoni kusiya eGezeri.
Kotero Davide anachita zimene Mulungu anamulamulira ndipo anakantha ankhondo a Afilisti njira yonse kuchokera ku Gibiyoni mpaka ku Gezeri.
17 Yikho udumo lukaDavida lwanda lwafinyelela kuwo wonke amazwe, uThixo wenza izizwe zonke zimesabe.
Choncho mbiri ya Davide inafalikira dziko lonse, ndipo Yehova anachititsa kuti mayiko ena azimuopa.