< Acts 17 >

1 Ek din paul aru silas duijon Amphipolis aru Apollonia laga sheher paar kori kene jaise, aru Thessalonica laga sheher te ahi ponchise, ta te Yehudi khan laga ekta mondoli thakise.
Atadutsa ku Amfipoli ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge ya Ayuda.
2 Aru Paul laga adat ekta thaka nisina, tai taikhan logote jaise, aru tin Bisram din tak taikhan logote Isor laga kotha koi thakise.
Paulo, monga mwachizolowezi chake, analowa mʼsunagoge, ndipo anakambirana nawo Mawu a Mulungu kwa masabata atatu,
3 Aru tai Shastro khuli kene taikhan ke bujhai thakise ki Khrista dukh pabo aru mora pora jinda hoi jabo, aru etu eneka hobole dorkar thakise. Aru tai koise, “Etu Jisu kun laga kotha koi kene moi prochar kori ase Tai he Khrista ase.”
kuwafotokozera ndi kuwatsimikizira kuti Khristu anayenera kufa ndi kuuka. Iye anati, “Yesu amene ndikukulalikirani ndiye Khristu.”
4 Ta te kunba Yehudi khan Paul aru Silas laga kotha huni kene tai duijon logote milai loise, aru taikhan logote kunba Yunani khan aru kunba maiki khan bhi mili jaise.
Ena mwa Ayuda anakopeka mtima ndipo anatsatira Paulo ndi Sila, monganso linachitira gulu lalikulu la Agriki woopa Mulungu, pamodzi ndi amayi odziwika ambiri.
5 Kintu biswas nakora Yehudi khan mon julise, aru bajar pora biya manu ke joma kori loise, aru bisi manu lagai kene sheher te hala korise. Aru jitia Jason laga ghor bhangai dise, aru Paul aru Silas ke manu khan dhori kene loi anibole bisarise.
Koma Ayuda ena anachita nsanje; kotero anasonkhanitsa anthu akhalidwe loyipa ochokera pa msika ndipo napanga gulu nayambitsa chipolowe mu mzindawo. Anathamangira ku nyumba ya Yasoni kukafuna Paulo ndi Sila kuti awabweretse pa gulu la anthu.
6 Kintu jitia taikhan duijon ke panai, taikhan Jason aru kunba biswasi bhai khan ke dhori kene sheher laga adhikari khan usorte loi jaise, aru hala kori kene koise, “Etu manu khan jun duniya ke ulta koridi ase, taikhan bhi yate ahikena ase.
Koma atalephera kuwapeza, anakokera Yasoniyo ndi abale ena ku bwalo la akulu a mzindawo akufuwula kuti, “Anthu awa, Paulo ndi Sila, amene akhala akusokoneza dziko lonse lapansi, tsopano afikanso kuno.
7 Jason pora tai laga ghor te manu kunkhan rakhise kunkhan Caesar laga kotha mana nai, aru taikhan koi ase Jisu koi kene dusra raja ase.”
Yasoni ndiye anawalandira mʼnyumba mwake. Onsewa akuchita zotsutsana ndi malamulo a Kaisara pomanena kuti palinso mfumu ina, yotchedwa Yesu.”
8 Aru etu kotha huni kene bisi manu khan aru sheher laga adhikari khan sob chinta hoise.
Atamva zimenezi, gulu la anthu ndi akulu a mzinda anavutika mu mtima.
9 Kintu taikhan Jason aru tai laga saathi khan pora poisa loise, aru dusra biswasi khan ke jabole dise.
Iwo analipiritsa Yasoni ndi anzakewo ndipo anawamasula.
10 Titia biswasi bhai khan etu rati te Paul aru Silas ke Berea sheher te pathai dise. Aru jitia duijon ta te ponchise, tai duijon Yehudi khan laga mondoli te jaise.
Mdima utagwa, abale anatumiza Paulo ndi Sila ku Bereya. Atafika kumeneko anapita ku sunagoge ya Ayuda.
11 Aru Thessalonica te thaka manu khan to dusra jaga laga manu khan pora bhi bhal thakise, kelemane taikhan hodai din Isor laga kotha te ki likha ase etu saikene bhal mon pora grohon kori thakise.
Tsopano anthu a ku Bereya anali akhalidwe labwino kusiyana ndi Atesalonika, pakuti iwo analandira mawu ndi chidwi chachikulu ndipo ankasanthula Malemba tsiku ndi tsiku kuti aone ngati zimene ankanena Paulozo zinali zoona.
12 Etu nimite bisi manu Jisu ke biswas kori loise, aru ta te laga Yunani niyom mani thaka mahila khan aru kunba mota manu khan bhi biswas korise.
Ayuda ambiri anakhulupirira, monga anachitiranso amayi ndi amuna ambiri odziwika a Chigriki.
13 Kintu jitia Thessalonica laga Yehudi khan Paul pora Berea te Isor laga kotha koi ase koi kene janise, taikhan jai kene manu khan laga monte biya kotha hali dise aru mon biya kori bole dise.
Ayuda a ku Tesalonika atadziwa kuti Paulo akulalikira Mawu a Mulungu ku Bereya, anapitanso kumeneko, ndi kuwutsa mitima ya anthu nayambitsa chisokonezo.
14 Etu homoi te, biswasi bhai khan joldi Paul ke samundar phale pora jabole dise, kintu Silas aru Timothy to Berea te thaki jaise.
Nthawi yomweyo abale anatumiza Paulo ku nyanja koma Sila ndi Timoteyo anatsalira ku Bereya.
15 Aru jun manu Paul ke loi jaise taikhan Athens sheher pora aru dur te taike loi jaise. Aru jitia taikhan Silas aru Timothy duijon ke Paul pora tai usorte te joldi ahibole dibi koi kene khobor paise, taikhan nijor laga ghor te jai jaise.
Anthu amene anamuperekeza Paulo nafika naye ku Atene, ndipo anabwerera ku Bereya atawuzidwa kuti Sila ndi Timoteyo amutsatire msanga.
16 Jitia Paul Athens te Silas aru Timothy ke rukhi thakise, tai etu sheher te murti bhorta thaka dikhi kene tai laga atma pora bisi mon dukh hoise.
Paulo akudikira Timoteyo ndi Sila ku Atene, anavutika mu mtima kwambiri poona kuti mzindawo unali odzaza ndi mafano.
17 Titia tai mondoli te jai kene Yehudi aru hosa Isor ke aradhana kora manu khan logote kotha korise, aru hodai tai jitia bajar te jai ta te bhi manu lok paile etu laga kotha kori thakise.
Tsono anakambirana ndi Ayuda ndi Agriki amene amaopa Mulungu mʼsunagoge, komanso anthu amene amapezeka pa msika tsiku ndi tsiku ndi ena amene amakumana nawo.
18 Titia Epicurean aru Stoic khan laga pondit kunba ahi kene tai logot kotha lagi thakise, aru kunba koise, etu ke najana manu ki kobole mon kori ase? Dusra koise tai dusra jaga laga dhorom manu ase, kelemane tai Jisu laga kotha aru jee utha laga kotha prochar kori ase.
Gulu la Aepikureya ndi Astoiki, anthu anzeru, anayamba kutsutsana naye. Ena a iwo anafunsa kuti, “Kodi wolongololayu akufuna kunena chiyani?” Enanso anati, “Akuoneka ngati akulalikira milungu yachilendo.” Iwo ananena zimenezi chifukwa Paulo amalalikira Uthenga Wabwino wa Yesu ndi kuuka kwa akufa.
19 Taikhan Paul ke Aropagus laga usorte loi jaise aru koise, “Tumi ki koi ase aru sikhai ase etu amikhan bhi janibole paribo?
Kenaka iwo anamutenga nafika naye ku bwalo la Areopagi kumene anamufunsa kuti, “Kodi tingadziweko chiphunzitso chatsopano chimene ukuchifotokozachi?
20 Kelemane amikhan laga kan pora kitia bhi nahuna kotha huni bole pai ase. Etu nimite, amikhan bhi janibole mon ase etu kotha laga ki motlob ase.”
Iwe ukubweretsa zinthu zina zachilendo mʼmakutu mwathu, ndipo ife tikufuna tidziwe tanthauzo lake.”
21 -Etiya sob Athens laga manu aru dusra desh pora ahi kene thaka manu khan dusra eku kaam nakori kene kiba notun kotha hunile etu laga kotha koi kene bohi thake.
Atene onse ndi alendo amene amakhala kumeneko samachita kanthu kena koma kufotokoza ndi kumvera fundo zatsopano.
22 Titia Paul Areopagus majote khara hoi kene koise, “Tumi Athens laga manu khan, moi dikhi ase tumikhan sob kaam te bhal ase.
Paulo anayimirira mʼbwalo la Areopagi nati: “Inu anthu a ku Atene! Ine ndikuona kuti mʼnjira zonse ndinu opembedza kwambiri.
23 Jitia moi tumikhan laga puja kori thaka saman khan saikene paar kori thakise, tumikhan pathor pora bona bedi te eneka likhi kene rakha dikhise, “Ekjon najana Isor nimite.” Etu karone junke apnikhan najani kene puja kori thaki ase, etu laga kotha tumikhan ke moi kobo.
Pakuti pamene ndimayenda ndi kuona zinthu zimene mumazipembedza, ndapezanso guwa lansembe lolembedwapo kuti, kwa mulungu wosadziwika. Tsopano chimene mumachipembedza osachidziwa ndi chimene ndikuchilalikira.
24 Isor jun he prithibi aru ta te thaka sob bonai dise, Tai sorgo aru prithibi laga Isor ase, manu pora bonai diya laga mondoli te nathake.
“Mulungu amene analenga dziko lapansi ndiponso zonse zili mʼmenemo ndiye Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi ndipo sakhala mʼnyumba zachipembedzo zomangidwa ndi manja.
25 Aru Tai manu laga hath laga sewa nalage, aru manu pora eku nibisare, kelemane Tai he sobke jibon aru saas diye aru manu ki lage Tai etu sob diye.
Ndipo satumikiridwa ndi manja a anthu ngati kuti Iye amasowa kanthu, chifukwa Iye ndiye amapereka moyo ndi mpweya kwa anthu onse ndi zina zonse.
26 Aru Tai ekjon manu pora he ekta desh aru jiman manu etiya thaki ase etu sobke bonai dise, ki homoi te kineka dibole lage aru kun manu laga jat kote thaki bole lage etu sob Tai pora bonai kene rakhidise,
Kuchoka kwa munthu mmodzi Iye analenga mtundu uliwonse wa anthu, kuti akakhale pa dziko lonse lapansi; ndipo Iye anakonzeratu nthawi yawo ndiponso malo enieni kumene adzakhale.
27 Eneka korile manu khan Taike bisaribo aru taikhan Isor phale mon dibo aru Tai usorte ahibo. Kintu Tai amikhan pora kitia bhi dur thaka nai.
Mulungu anachita izi kuti anthu amufunefune, ndikuti pomufunafunapo amupeze ngakhale kuti Iye sali kutali ndi aliyense wa ife.
28 Kelemane amikhan Tai logote jinda ase aru amikhan laga ki ase etu sob to Tai laga he ase, jineka apuni khan laga majote kitab likha ekjon pora koise, ‘Amikhan sob Tai laga bacha khan he ase.’
‘Pakuti timakhala mwa Iye, kuyenda mwa Iye ndi kukhala moyo mwa Iye.’ Monga olemba ndakatulo anu ena akuti, ‘Ife ndi zidzukulu zake.’
29 Etu karone, amikhan Isor laga bacha ase, amikhan eneka bhabona kori bole nalage ki tai laga sobhab to suna, chandi, aru pathor nisena ase- eitu khan jinis to manu laga bhabona pora bonai.
“Tsono popeza ndife ana a Mulungu, tisaganize kuti umulungu wake ndi wofanana ndi ndalama zagolide, zasiliva, mwala, kapenanso fanizo lopangidwa mwaluso la nzeru za anthu.
30 Etu nimite Isor poila te manu laga paap dhyan nakori kene chari dise, kintu etiya Tai sob manu ke paap pora mon ghura bole hukum dise.
Nthawi imene anthu sankadziwa, Mulungu anawalekerera koma tsopano akulamulira kuti anthu onse, kulikonse atembenuke mtima.
31 Kelemane, ek dinte rakhi kene ase, juntu dinte, Tai pora basi luwa ekjon pora etu duniya ke dhormikta pora bisar koribo. Isor he Jisu ke mora pora jinda kori kene Tai hosa Isor ase koi kene dikhai dise.”
Pakuti Iye wayika tsiku limene adzaweruze dziko lapansi mwa chilungamo kudzera mwa Munthu amene anamusankha. Iye watsimikizira anthu onse zimenezi pomuukitsa.”
32 Aru jitia Athens laga manu khan mori kene jinda huwa kotha hunise, kunba ta te thaka khan Paul ke hinsa korise; kintu kunba koise, “Amikhan etu kotha apuni pora aru hunibo.”
Atamva za kuuka kwa akufa, ena a iwo anaseka, koma enanso anati, “Ife tikufuna tidzamvenso zimenezi tsiku lina.”
33 Etu pichete Paul taikhan laga majot pora ulai jaise.
Ndipo Paulo anatuluka mʼBwalolo.
34 Kintu kunba tai logote mili jaise aru tai ki kotha koise etu biswas korise, etu majote Dionysius jun Areopagus laga ekjon manu, aru Damaris koi kene ekjon mahila, aru dusra manu khan bhi taikhan logote thakise.
Anthu ena ochepa anamutsatira Paulo ndipo anakhulupirira. Pakati pawo panali Dionisiyo mmodzi wa bwalo la Areopagi ndi mayi wina wotchedwa Damalisi ndi enanso.

< Acts 17 >