< स्तोत्रसंहिता 121 >

1 मी आपली दृष्टी पर्वताकडे लावतो. मला मदत कोठून येईल?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 परमेश्वर जो आकाशाचा व पृथ्वीचा निर्माण करणारा त्याकडून माझी मदत येते.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 तो तुझा पाय घसरू देत नाही; जो तुझे संरक्षण करतो तो कधीही स्वस्थ झोपत नाही.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 पाहा, इस्राएलाचा रक्षणकर्ता कधीच झोपत नाही किंवा तो डुलकीही घेत नाही.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 परमेश्वर तुझा रक्षणकर्ता आहे; परमेश्वर तुझ्या उजव्या हाताला सावली आहे.
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 दिवसा तुला सूर्य किंवा रात्री चंद्र तुला नुकसान करणार नाही.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 परमेश्वर सर्व वाईटापासून तुझे रक्षण करील; तो तुझ्या जिवाचे रक्षण करील.
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 परमेश्वर तुला; जे सर्व काही तू करशील, त्यामध्ये आता आणि सदासर्वकाळ रक्षण करील.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< स्तोत्रसंहिता 121 >