< Waiata 48 >

1 He waiata, he himene ma nga tama a Koraha. He nui a Ihowa, kia nui hoki te whakamoemiti ki a ia i te pa o to tatou Atua, i te maunga o tona tapu.
Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
2 Ataahua ana te tairanga o Maunga Hiona, ko ta te ao katoa e koa ai: kei te taha ki te raki te pa o te Kingi nui.
Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
3 E matauria ana te Atua i roto i ona whare papai hei piringa.
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
4 Na, huihui tahi mai ana nga kingi haere tahi atu ana ratou.
Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
5 I kite ratou, miharo iho: raruraru ana, hohoro tonu atu.
iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
6 Pa ana te wehi ki a ratou i reira, te mamae, ano he wahine e whanau ana.
Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
7 E wahia ana e koe nga kaipuke o Tarahihi ki te marangai.
Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
8 Rite tonu ki ta matou i rongo ai, ta matou i kite ai i roto i te pa o Ihowa o nga mano, i te pa o to tatou Atua: ma te Atua e whakapumau ake ake. (Hera)
Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
9 I whakaaroaro matou ki tou atawhai, e te Atua, i waenganui o tou temepara.
Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
10 E te Atua, rite tahi ki tou ingoa te whakamoemiti mou, tae noa atu ki nga pito o te whenua: ki tonu tou matau i te tika.
Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
11 Kia hari a Maunga Hiona, kia koa nga tamahine a Hura i au whakaritenga.
Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
12 Taiawhiotia a Hiona, haere, a kopiko noa mai: taua ona pourewa.
Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
13 Maharatia ona pekerangi, tirohia ona whare papai; hei korerotanga ma koutou ki enei ake whakatupuranga.
Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
14 Ko tenei Atua hoki te Atua mo tatou ake ake: ko ia hei kaiarahi i a tatou a mate noa.
Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.

< Waiata 48 >