< Ihaia 55 >
1 E! e nga tangata katoa e matewai ana, haere mai ki nga wai! me te tangata kahore ana moni; haere mai, hokona, kainga! Haere mai, hokona he waina, he waiu; kaua he moni, kaua he utu.
“Bwerani, inu nonse amene muli ndi ludzu, bwerani madzi alipo; ndipo inu amene mulibe ndalama bwerani, mudzagule chakudya kuti mudye! Bwerani mudzagule vinyo ndi mkaka osalipira ndalama, osalipira chilichonse.
2 He aha ra i hokona ai e koutou te moni mo nga mea ehara i te taro, to koutou uaua mo nga mea e kore ai koutou e makona? ata whakarongo mai ki ahau, a kainga te mea pai; kia ora hoki o koutou wairua i nga mea momona.
Chifukwa chiyani ndalama zanu mukuwonongera zinthu zimene samadya, ndipo mukuwononga malipiro anu pa zinthu zimene sizikhutitsa? Tamverani, mvetsetsani zimene ndikunena kuti mudye zimene zili zabwino; ndipo mudzisangalatse.
3 Tahuri mai o koutou taringa, haere mai ki ahau; whakarongo mai, a ka ora o koutou wairua, a maku e whakarite ki a koutou he kawenata mau tonu, ara nga atawhainga pono i a Rawiri.
Tcherani makutu ndipo mubwere kwa Ine; mvereni Ine, kuti mukhale ndi moyo. Ndidzachita nanu pangano losatha, chikondi changa chija chosasinthika ndi chodalirika ndinalonjeza Davide.
4 Nana, kua waiho ia e ahau hei kaiwhakaatu ki nga iwi, hei rangatira, hei kaiwhakahau mo nga tauiwi.
Taonani, ine ndamusankha kuti akhale mboni yanga kwa mitundu ya anthu, kuti akhale mtsogoleri ndi wolamulira mitundu ya anthu.
5 Nana, ka karanga koe i te iwi kihai i mohiotia e koe; ka rere mai ano ki a koe nga iwi kahore i mohio ki a koe; mo Ihowa hoki, mo tou Atua, mo te Mea Tapu o Iharaira; nana hoki koe i whakanui.
Ndithu inu mudzayitanitsa mitundu ya anthu imene simuyidziwa, ndipo mitundu ya anthu imene sikudziwani idzabwera ndi liwiro kwa inu. Izi zidzatero chifukwa Yehova Mulungu wanu, Woyerayo wa Israeli, wakuvekani ulemerero.”
6 Rapua a Ihowa, kei kitea ana ia: karangatia atu, kei tata ana mai ia.
Funafunani Yehova pamene Iye akupezeka. Mupemphere kwa Iye pamene ali pafupi.
7 Kia whakarere te tangata kino i tona ara, te tangata mahi he i ona whakaaro; kia hoki ki a Ihowa, a ka aroha ia ki a ia; ki to tatou Atua hoki, he nui rawa hoki tana mahi tohu.
Woyipa asiye makhalidwe ake oyipa, ndipo wosalungama asinthe maganizo ake oyipa. Abwerere kwa Yehova, ndipo adzamuchitira chifundo, ndi kwa Mulungu wathu, pakuti adzamukhululukira koposa.
8 Ehara hoki oku whakaaro i o koutou whakaaro, o koutou hurarahi i oku huarahi, e ai ta Ihowa.
“Pakuti maganizo anga siwofanana ndi maganizo anu, ngakhale njira zanu si njira zanga,” akutero Yehova.
9 Ta te mea e ikeike ake ana te rangi i te whenua, waihoki ko oku huarahi e ikeike ake ana i o koutou huarahi, ko oku whakaaro i o koutou whakaaro.
“Monga momwe mlengalenga muli kutali ndi dziko lapansi, momwemonso zochita zanga nʼzolekana kutali ndi zochita zanu, ndipo maganizo anga ndi osiyana kutali ndi maganizo anu.
10 Ka rite hoki ki te ua raua ko te hukarere e rere iho ana i te rangi, a e kore e hoki ki reira; engari e whakamakuku ana i te whenua, e mea ana kia whai hua, kia pihi ake, kia homai ano he purapura ma te kaiwhakato, he taro ma te tangata e kai an a:
Monga mvula ndi chisanu chowundana zimatsika kuchokera kumwamba, ndipo sizibwerera komweko koma zimathirira dziko lapansi. Ndipo zimameretsa ndi kukulitsa zomera kenaka nʼkupatsa mlimi mbewu ndi chakudya.
11 Ka pena ano taku kupu e puta ana i toku mangai: e kore e hoki kau, mai ki ahau; engari ka meatia taku i pai ai, ka taea hoki taku i unga atu ai.
Ndi mmenenso amachitira mawu ochokera mʼkamwa mwanga. Sadzabwerera kwa Ine kopanda phindu lake, koma adzachita zonse zimene ndifuna, ndipo adzakwaniritsa cholinga chimene ndinawatumira.
12 Ta te mea ka haere atu koutou me te hari ano, ka arahina i runga i te rangimarie; ka pakaru mai te waiata a nga maunga, a nga pukepuke, i to koutou aroaro, a ka papaki ringa nga rakau katoa o te whenua.
Inu mudzatuluka mu mzindawo mwachimwemwe ndipo adzakutsogolerani mwamtendere; mapiri ndi zitunda zidzakuyimbirani nyimbo, ndipo mitengo yonse yamʼthengo idzakuwombereni mʼmanja.
13 He tataramoa i mua, ka puta ake he kauri; he tumatakuru i mua, ka puta ake he ramarama: a ka waiho hei ingoa ki a Ihowa, hei tohu mo a mua tonu atu, e kore e motuhia.
Mʼmalo mʼmene tsopano muli mitengo ya minga mudzamera mitengo ya payini, ndipo kumene kuli mkandankhuku kudzamera mchisu. Zimenezi zidzakhala chikumbutso cha Yehova, ngati chizindikiro chamuyaya, chimene sichidzafafanizika konse.”