< Salamo 45 >

1 Andipore’ ty troko i talily soay: Hoe iraho: I mpanjakay ro fitoloñako; fisokim-panokitse mahimbañe ty lelako.
Kwa mtsogoleri wamayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe a “Maluwa a Kakombo.” Salimo la ana a Kora. Nyimbo ya pa ukwati. Mtima wanga watakasika ndi nkhani yokoma pamene ndikulakatula mawu anga kwa mfumu; lilime langa ndi cholembera cha wolemba waluso.
2 Tsomerentsereñe ta o ana’ondatio n’Iheo; idoañam-pañisohañe o fivimbi’oo, aa le nitahien’Añahare kitro añ’afe’e.
Inu ndinu abwino kwambiri kuposa anthu onse ndipo milomo yanu inadzozedwa ndi chikondi cha Mulungu chosasinthika, popeza Mulungu wakudalitsani kwamuyaya.
3 Adiaño an-toha’o ty fibara’o, ry Fanalolahy, ty enge’o naho volonahe’o.
Mangirirani lupanga lanu mʼchiwuno mwanu, inu munthu wamphamvu; mudziveke nokha ndi ulemerero ndi ukulu wanu.
4 Mionjona am-pandreketañe am-bolonahe’o, hañonjonañe ty hatò naho ty halèn-arofo, vaho ty havantañañe; le hañoke azo an-­draha mampañeveñe ty fità’o havana.
Mu ukulu wanu mupite mutakwera mwachigonjetso mʼmalo mwa choonadi, kudzichepetsa ndi chilungamo; dzanja lanu lamanja lionetsere ntchito zanu zoopsa.
5 Masioñe ty ana-pale’o añ’arofon-drafelahi’ i mpanjakay ao—mihotrakotrak’ ambane’o ondatio;
Mivi yanu yakuthwa ilase mitima ya adani a mfumu, mitundu ya anthu igwe pansi pa mapazi anu.
6 Nainai’e donia, ry Andrianañahare, ty fiambesa’o; kobain-kavantañañe ty kobaim-pifehea’o.
Mpando wanu waufumu, Inu Mulungu, udzakhala ku nthawi za nthawi; ndodo yaufumu yachilungamo idzakhala ndodo yaufumu ya ufumu wanu.
7 Fitea’o ty havañonañe, falai’o ty hatsivokarañe; aa le nañory azo t’i Andrianañahare, Andrianañahare’o, an-tsolim-pirebehañe ambone’ o rañe’oo.
Inu mumakonda chilungamo ndi kudana ndi zoyipa; choncho Mulungu, Mulungu wanu, wakukhazikani pamwamba pa anzanu pokudzozani ndi mafuta a chimwemwe.
8 Ze hene saro’o ro tsotse naho emboke vaho mañidè! marovany boak’ amo anjomba nitemereñe nifem-bibio ro ifalea’o.
Mikanjo yanu yonse ndi yonunkhira ndi mure ndi aloe ndi kasiya; kuchokera ku nyumba zaufumu zokongoletsedwa ndi mnyanga wanjovu nyimbo za zoyimbira zazingwe zimakusangalatsani.
9 Anak’ampelam-panjaka ro amo noro’oo; mijohañe am-pitàn-kavana’o eo ty tañanjomba’o am-bolamena ki’ i Ofire.
Ana aakazi a mafumu ali pakati pa akazi anu olemekezeka; ku dzanja lanu lamanja kuli mkwatibwi waufumu ali mu golide wa ku Ofiri.
10 Mitsendreña ry anak’ampela, Inao! atokilaño ty sofi’o, andikofo o rofoko’oo, naho ty anjomban-drae’o.
Tamvera, iwe mwana wa mkazi ganizira ndipo tchera khutu; iwala anthu ako ndi nyumba ya abambo ako.
11 Mahasinda i mpanjakay ty hamontramontra’o; iambaneo kanao talè’o.
Mfumu yathedwa nzeru chifukwa cha kukongola kwako; mulemekeze pakuti iyeyo ndiye mbuye wako.
12 Hibanabana ama’e ty anak’ ampela’ i Tsore, Hipay fañisoahañ’ ama’e o mpañaleale am’ondatio.
Mwana wa mkazi wa ku Turo adzabwera ndi mphatso, amuna a chuma adzafunafuna kukoma mtima kwako.
13 Fanjàka añ’anjomba ao ty anak’ampela’ i mpanjakay, vinahotse am-­bolamena o saro’eo.
Wokongola kwambiri ndi mwana wa mfumu ali mʼchipinda mwake, chovala chake ndi cholukidwa ndi thonje ndi golide.
14 Ho roroteñe mb’amy mpanjakay mb’eo an-tsaroñe soa vinahotse, hasese ama’o rekets’ o somondrara mpiama’e mpañotroñe azeo.
Atavala zovala zamaluwamaluwa akupita naye kwa mfumu; anamwali okhala naye akumutsatira ndipo abweretsedwa kwa inu.
15 Amañ’ehake naho an-drebeke ro aneseañe iareo; ie ampiziliheñe añ’anjomba’ i mpanjakay.
Iwo akuwaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo; akulowa mʼnyumba yaufumu.
16 Handimbe’an-droae’o o ana-dahi’oo; horiza’o ho mpiaolo’ i tane iabiy iereo.
Ana ako aamuna adzatenga malo a makolo ako; udzachititsa kuti akhale ana a mfumu mʼdziko lonse.
17 Hampitiahieko ze hene tariratse ty tahina’o, hañandriañe azo nainai’e donia ondatio.
Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse; choncho mitundu yonse idzakutamanda ku nthawi za nthawi.

< Salamo 45 >