< Salamo 16 >
1 Tambozoro iraho, ry Andrianañahare, toe ama’o ty fitsolohako.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Ty hoe ty tinaroko am’ Iehovà: Ihe ro Talèko, izaho tsy aman-kasoa naho tsy ama’o.
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 O noro’e an-tane atoio: ie ro talango’e, toe mampinembanembañe ahiko.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 Hampitomboeñe ty hasotria’ ze mihitrike mb’an-tsamposampo’e añe; tsy hailiko ty engan-dranon-dio’iareo, le tsy ho rambesen-tsoñiko o añara’ iareoo.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 Iehovà ro anjara-lovako naho ty fitoviko. Tohañe’o ty navike ho ahiko.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 An-toetse fanjaka ty nipoha’ o taly ho ahikoo; Eka, soa i lovakoy.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Andriañeko t’Iehovà mpamere ahiko, ie haleñe, anare’ ty troko.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Najadoko aoloko nainai’e t’Iehovà. Ie ty an-tañako havana eo, tsy higavingaviñe.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Aa le tsy mahay avao ty troko, vaho mirebeke ty havokarako; mierañerañe ka ty sandriko,
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 amy te tsy hapo’o an-tsikeokeok’ ao ty fiaiko, vaho tsy hado’o hahaoni-pihomahañe i Masi’oy. (Sheol )
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
11 Ampaharofoana’o ahiko ty lalan-kaveloñe; lifotse hafaleañe ty añatrefa’o; haravoravoañe nainai’e ro am-pitàn-kavana’o.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.