< Fitomaniana 3 >
1 Ondaty nahatrea hasotrian-draho amy kobain-kaviñera’ey.
Ine ndine munthu amene ndaona masautso ndi ndodo ya ukali wake.
2 Niaoloa’e naho nampomba’e mb’an-kamoromoroñañe ao fa tsy mb’an-kazavàñe.
Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa mu mdima osati mʼkuwala;
3 Toe nafote’e amako lomoñandro lomoñandro ty fità’e.
zoonadi anandikantha ndi dzanja lake mobwerezabwereza tsiku lonse.
4 Nanoe’e hambo’e o nofokoo naho o holikoo; sindre pinekapeka’e o taolakoo.
Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga, ndipo waphwanya mafupa anga.
5 Nanoa’e hàlañe, nañarikatoha’e afero naho haloviloviañe.
Wandizinga ndi kundizungulira ndi zowawa ndi zolemetsa.
6 Nampitobohe’e an-toetse maieñe ao iraho, hoe lolo-ela.
Wandikhazika mu mdima ngati amene anafa kale.
7 Narindri’e ao tsy hahafionjoñe; nanoe’e mavesatse o silisilikoo.
Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe, wandimanga ndi maunyolo.
8 Aa naho mikoikoike hipay imba, le sikadaña’e alafe ao i halalikoy.
Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo, amakana pemphero langa.
9 Nikalaña’e am-bato vinañe o liakoo, nampikelokelofe’e o oloñolokoo.
Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema; ndipo wakhotetsa tinjira tanga.
10 Hoe amboa romotse mamandroñe ahy, hoe liona añ’etaketak’ ao.
Wandidikirira ngati chimbalangondo, wandibisalira ngati mkango.
11 Natsile’e iaby o fombàkoo, naho nirimidrimite’e ty sandriko; nanoe’e babangoañe.
Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba, ndipo wandisiya wopanda thandizo.
12 Fa nabitso’e ty fale’e, le nohara’e amako ty ana-pale.
Wakoka uta wake ndipo walunjikitsa mivi yake pa ine.
13 Nampitrofahe’e ambaniako ao o ana-tsotsòke boak’ an-trañon’ ana-pale’eo.
Walasa mtima wanga ndi mivi ya mʼphodo mwake.
14 Fa injè’ondatikoo iraho, bekobekoa’ iareo lomoñandro.
Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse; amandinyodola mʼnyimbo zawo tsiku lonse.
15 Finaha’e hafairañe vaho natsafe’e vahon-tsoy.
Wandidyetsa zowawa ndipo wandimwetsa ndulu.
16 Finoifoi’e am-bato o nifekoo; nalembe’e an-davenok’ ao iraho.
Wathyola mano anga ndi miyala; wandiviviniza mʼfumbi;
17 Nampihankàñe’o lavi-panintsiñañe ty haveloko; nihaliñoko ze o hasoa zao.
Wandichotsera mtendere; ndayiwala kuti kupeza bwino nʼchiyani.
18 Le hoe iraho, Fa modo ty haozarako, ty fitamàko am’ Iehovà.
Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka ndi zonse zimene ndimayembekeza kwa Yehova.”
19 Tiahio ty haloviloviako naho ty hasotriako, ty vahon-tsoy naho afero.
Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala, zili ngati zowawa ndi ndulu.
20 Toe tiahi’ ty fiaiko, vaho mibotrek’ amako ao.
Ine ndikuzikumbukira bwino izi, ndipo moyo wanga wathedwa mʼkati mwanga.
21 Ty hoe ty apotam-pitsakoreako, mampitamà ahiko, te
Komabe ndimakumbukira zimenezi, nʼchifukwa chake ndili ndi chiyembekezo.
22 le lia’e tsy mijihetse ty fiferenaiña’ Iehovà tsy mb’ia hilesa o fiferenaiña’eo.
Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu, ndi chifundo chake ndi chosatha.
23 Vao boak’andro; ra’elahy ty figahiña’o.
Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse; kukhulupirika kwanu nʼkwakukulu.
24 Iehovà ty anjarako, hoe ty troko, aa le ie ty fitamàko.
Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse; motero ndimamuyembekezera.”
25 Soa t’Iehovà amo mahaliñe azeo; amy arofo mipay Azey.
Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye, kwa munthu amene amafunafuna Iyeyo;
26 Mahasoa ondatio te mitama, t’ie handiñe am-pianjiñañe ty fandrombaha’ Iehovà.
nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha Yehova modekha.
27 Hasoa am’ondatio ty mivave ty jokan-katora’e.
Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli pamene ali wamngʼono.
28 Angao re hiambesatse am-bangiñe ao, hianjiñe, amy te ie ty nandafik’ aze.
Akhale chete pa yekha, chifukwa Yehova wamusenzetsa golilo.
29 Hatoho’e an-debok’ ao ty falie’e, hera ama’e ty fitamañe.
Abise nkhope yake mʼfumbi mwina chiyembekezo nʼkukhalapobe.
30 Soa re te hatolo’e amy mandrara- tehak’ azey ty fiambina’e; angao ampiliporeñ’ inje.
Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye, ndipo amuchititse manyazi.
31 Fa tsy hañito nainai’e t’i Talè.
Chifukwa Ambuye satayiratu anthu nthawi zonse.
32 Aa ndra t’ie ty mampioremeñe, mbe hiferenaiña’e amy hafatraram-pikokoa’ey.
Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo, chifukwa chikondi chake ndi chosatha.
33 Tsy mora ama’e ty mandafa, ndra ty mandilo o ana’ondatio;
Pakuti sabweretsa masautso mwadala, kapena zowawa kwa ana a anthu.
34 Ie ampidemoheñe am-pandia, ze mpirohi’ ty tane toy;
Kuphwanya ndi phazi a mʼndende onse a mʼdziko,
35 ie tsy omen-to ondatio añatrefa’ i Andindimoneñey,
kukaniza munthu ufulu wake pamaso pa Wammwambamwamba,
36 ie ampikeloheñe ty enta’ ondatio— tsy arofoana’ i Talè hao?
kumana munthu chiweruzo cholungama— kodi Ambuye saona zonsezi?
37 Ia ty nitaroñe naho nahafetsake zao, naho tsy i Talè ty nametse?
Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika ngati Ambuye sanavomereze?
38 Tsy boak’am-palie’ i Abo Tiañey hao ty hankàñe naho ty soa?
Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka mʼkamwa mwa Wammwambamwamba?
39 Akore ty itoreova’ondaty veloñeo, o lahilahio ty amo tahi’eo?
Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula akalangidwa chifukwa cha machimo ake?
40 Antao hañotsohotso hitsoke o lalan-tikañeo, vaho himpoly mb’am’ Iehovà mb’eo.
Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu, ndipo tiyeni tibwerere kwa Yehova.
41 Antao hañonjoñ’ arofo am-pitàñe mb’aman’Añahare an-digiligy añe.
Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu kwa Mulungu kumwamba ndipo tinene kuti:
42 Toe nandilatse zahay naho niola; toly ndra tsy napo’o.
“Ife tachimwa ndi kuwukira ndipo inu simunakhululuke.
43 Nikolopok’ an-kaviñeran-drehe te nañoridañe anay; tsy niferenaiña’o t’ie nanjamañe.
“Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo mwatitha mopanda chifundo.
44 Nisaron-drahon-dRehe, tsy himoahan-kalaly.
Mwadzikuta mu mtambo kotero mapemphero athu sakukufikani.
45 Nanoe’o romoromo’e naho forompotse zahay añivo’ o kilakila’ndatio.
Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala pakati pa mitundu ya anthu.
46 Songa midañadaña falie ama’ay o malaiñ’anaio.
“Adani anthu atitsekulira pakamwa.
47 Fa nifetsak’ ama’ay ty hebakebake naho i koboñey, ty famongorañe naho fandrotsahañe.
Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje, tapasuka ndi kuwonongedwa.”
48 Mitsiritsioke rano o masokoo, amy fandrotsahañe i anak’ampela’ ondatikoy.
Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe chifukwa anthu anga akuwonongedwa.
49 Midoandoañe mañambane o masokoo, vaho tsy mijihetse, tsy mitroatse,
Misozi idzatsika kosalekeza, ndipo sidzasiya,
50 Ampara’ te mivazoho mañambane t’Iehovà, mitalake boak’ an-dikerañe añe.
mpaka Yehova ayangʼane pansi kuchokera kumwamba ndi kuona.
51 Mampihontoke ty troko o masokoo ty amo hene anak’ampelan-drovakoo.
Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi chifukwa cha akazi onse a mu mzinda.
52 Fa nikehe ahy hoe kibo, tsy amam-poto’e o malaiñ’ahio.
Akundisaka ngati mbalame, amene anali adani anga, popanda chifukwa.
53 Naitoa’ iareo an-koboñe ao ty fiaiko, vaho nandretsa-bato amako.
Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje ndi kundiponya miyala;
54 Nandipotse ty lohako o ranoo vaho nanoeko ty hoe: Opo iraho!
madzi anamiza mutu wanga ndipo ndinkaganiza kuti imfa yayandikira.
55 Kinanjiko ty tahina’o ry Iehovà, boak’ an-koboñe loho lalek’ ao.
Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova, kuchokera mʼdzenje lozama.
56 Jinanji’o ty feoko; ko aeta’o amy ravembia’oy i fitoreokoy hahafikofohako.
Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere kulira kwanga kopempha thandizo.”
57 Nitotok’ ahy irehe amy andro nikanjiako azoy; le hoe irehe: Ko hemban-drehe.
Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani, ndipo munati, “Usaope.”
58 Ry Talè, nañalañalañe’o o entan’ aikoo; fa jineba’o ty fiaiko.
Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga; munapulumutsa moyo wanga.
59 Ry Iehovà, fa nivazoho’o ty nasarañ’ ahy; ehe izakao.
Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira. Mundiweruzire ndinu!
60 Fa nioni’o ty fitrotrofiaha’ iareo naho ty fikitroha’ iareo amako.
Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo, chiwembu chawo chonse pa ine.
61 Fa jinanji’o ty inje’ iareo, ry Iehovà, naho o fikililia’ iareo ahy iabio,
Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo, chiwembu chawo chonse pa ine,
62 Ty fivimbi’ o nitroatse amakoo, ty fikinià’ iareo ahy lomoñandro,
manongʼonongʼo a adani anga ondiwukira ine tsiku lonse.
63 Vazohò iereo te miambesatse, naho t’ie miongake; izaho bekobekoa’ iareo.
Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira, akundinyoza mu nyimbo zawo.
64 Mbe hondroha’o, ry Iehovà, ty amo satam-pità’ iareoo.
Inu Yehova, muwabwezere chowayenera, chifukwa cha zimene manja awo achita.
65 Kolopofo ty arofo’ iareo, ametsaho fatse!
Phimbani mitima yawo, ndipo matemberero anu akhale pa iwo!
66 Horidaño an-kaviñerañe vaho mongoro ambanen-dikera’ Iehovà eo.
Muwalondole mwaukali ndipo muwawonongeretu pa dziko lapansi.