< Mpitsara 1 >
1 Ie fa nivilasy t’Iehosoa, le nihalaly am’ Iehovà o ana’ Israeleo ami’ty hoe: Ia ty hionjoñe valoha’e mb’amo nte-Khanàneo ho anay, hialy?
Atamwalira Yoswa Aisraeli anafunsa Yehova kuti, “Ndani mwa ife ayambe nkhondo yomenyana ndi Akanaani?”
2 Le hoe t’Iehovà, Iehodà ty hionjomb’eo fa natoloko am-pità’e i taney.
Yehova anayankha kuti, “Fuko la Yuda ndilo liyambe kupita. Ndawapatsa dzikolo mʼmanja mwawo.”
3 Le hoe t’Iehoda amy Simone rahalahi’e, Mindreza amako mb’amy anjarakoy hialy amo nte-Khanàneo; le hindre ama’o ka iraho mb’amy anjara’oy. Aa le nindre lia ama’e t’i Simone.
Choncho Ayuda anawuza abale awo a fuko la Simeoni kuti, “Bwerani tipitire limodzi mʼdziko limene tapatsidwa kuti tikamenyane ndi Akanaani. Ifenso tidzapita nanu mʼdziko limene anakugawirani.” Ndipo Asimeoni anapita nawo.
4 Nionjom-beo t’Iehoda; naho nasese’ Iehovà am-pità’ iareo o nte-Khanàneo naho o nte-Perizeo, vaho binaibai’ iereo e Bezeke ty lahilahy rai-ale.
Choncho Ayuda ananyamuka, ndipo Yehova anapereka Akanaani ndi Aperezi mʼmanja mwawo. Ndipo anapha anthu 10,000 ku Bezeki.
5 Nizoe’ iareo e Bezek’ ao t’i Adonibezeke, le nialy ama’e, vaho zinama’ iareo t’i nte-Khanàne naho t’i nte-Perize.
Ku Bezekiko anakumana ndi ankhondo a mfumu Adoni-Bezeki ndipo anamenyana nawo, ndipo Ayudawo anagonjetsa Akanaani ndi Aperezi.
6 Fe nipoliotse añe t’i Adonibezeke, le hinorida’ iareo naho tsinepa’iareo vaho fonga kinitsi’ iareo ty tondro-beim-pità’e naho tondrobeim-pandia’e.
Adoni-Bezekiyo anathawa, koma anamuthamangira ndi kumupeza, namugwira. Atamugwira anamudula zala zake zazikulu za ku manja ndi miyendo.
7 Le hoe t’i Adonibezeke, Nitsindrok’ ambanen-datàbako ao ty mpanjaka fitompolo kinitsin-tondrobeim-pitàñe naho tondrobeim-pandia, aa le nafoten’ Añahare amako i nanoekoy. Aa le napo’ iareo e Ierosalaime ao re, vaho ao ty nihomaha’e.
Tsono Adoni-Bezeki anati, “Mafumu 70 omwe anadulidwa zala zazikulu za ku manja ndi miyendo yawo ankatola nyenyeswa pansi pa tebulo langa. Mulungu tsopano wandibwezera zomwe ndinawachita.” Kenaka anapita naye ku Yerusalemu ndipo anafera komweko.
8 Toe fa nialy am’ Ierosalaime o ana’ Iehodao, le fa tinava’ iareo naho linafa’ iareo an-dela-pibara, vaho namiañe afo amy rovay.
Pambuyo pake Ayuda anakathira nkhondo mzinda wa Yerusalemu ndipo anawulanda. Anapha anthu ambiri ndi kutentha mzinda wonse.
9 Ie amy zay, nizotso hialy amo nte-Khanàne mpimoneñe am-bohibohitse ao naho Atimo ao vaho an-tane petrak’ ao o ana’ Iehodao.
Kenaka Ayuda anapita kukamenyana ndi Akanaani omwe amakhala ku dziko la ku mapiri, dziko la Negevi kummwera ndiponso mu zigwa.
10 Naname o nte-Khanàne nimoneñe e Kebroneo t’Iehoda (toe natao Kiriate’arba ty Kebrone taolo), le vinono’ iareo t’i Sesay, naho i Akimane vaho i Talmaý.
Anakalimbananso ndi Akanaani amene ankakhala ku Hebroni (mzinda womwe kale unkatchedwa Kiriyati-Araba). Kumeneko anagonjetsa Sesai, Ahimani ndi Talimai.
11 Boak’ao re nañoridañe o mpimone’ i Debireo (toe natao Kiriate-sefere ty Debire taolo).
Kuchokera kumeneko, iwo anakathira nkhondo anthu amene ankakhala ku Debri (mzindawu poyamba unkatchedwa Kiriati Seferi).
12 Le hoe t’i Kalebe, Ze mandafa i Kiriate-sefere vaho mandrambe aze, ty hitolorako i Aksae anak’ ampelako ho vali’e.
Tsono Kalebe anati, “Munthu amene angathire nkhondo mzinda wa Kiriati Seferi ndi kuwulanda, ndidzamupatsa mwana wanga Akisa kuti akhale mkazi wake.”
13 I Otniele, ana’i Kenaze zai’ i Kalebe ty nandrambe aze; vaho natolo’e ama’e t’i Aksae anak’ampela’e ho tañanjomba’e.
Otanieli mwana wa Kenazi, mngʼono wake wa Kalebe, ndiye anawulanda. Choncho Kalebe anamupatsa mwana wake Akisa kuti akhale mkazi wake.
14 Ie amy zao, naho nimb’ama’e, le nosihe’e hihalaly tane aman-drae’e hambolea’e. Aa ie nizotso amy borìke’ey, le hoe ty asa’ i Kalebe ama’e, Ino o paia’oo?
Tsiku lina atafika Akisayo, Otanieli anamuwumiriza mkazi wakeyo kuti apemphe munda kwa Kalebe abambo ake. Pamene Akisa anatsika pa bulu wake, Kalebe anamufunsa kuti, “Kodi ukufuna ndikuchitire chiyani?”
15 Le hoe re tama’e: Fitsezo rano iraho fa tane maike ty natolo’o ahy; ehe toloro rano manganahana ka. Aa le natolo’ i Kalebe aze o manganahana amboneo naho o manganahana ambaneo.
Iye anayankha kuti, “Mundikomere mtima. Popeza mwandipatsa ku Negevi, kumalo kumene kulibe madzi, mundipatsenso akasupe amadzi.” Choncho Kalebe anamupatsa akasupe a kumtunda ndi a kumunsi.
16 Nionjoñe boak’ an-drovan-tsatrañe ao o ana’ i Keny, rafoza’ i Mosèo, mindre amo ana’ Iehodao, mb’ am-patram-bei’ Iehoda mb’eo, atimo’ i Arade ey vaho nindre nimoneñe am’ ondatio.
Tsono zidzukulu za Hobabu, Mkeni uja, mpongozi wa Mose, zinachoka ku Yeriko mzinda wa migwalangwa pamodzi ndi anthu a fuko la Yuda mpaka ku chipululu chimene chili kummwera kwa Aradi ndi kukakhala ndi Aamaleki.
17 Le nindre aman-joke’e Simone t’Iehoda, le linafa’ iareo o nte-Khanàne nimoneñe e Tsefate ao le vata’e narotsa’e. Natao Kormà ty añara’ i rovay.
Kenaka anthu a fuko la Yuda anapita pamodzi ndi abale awo a fuko la Simeoni ndi kukagonjetsa Akanaani amene amakhala ku Zefati, ndipo mzindawo anawuwononga kwambiri. Choncho mzindawo anawutcha Horima.
18 Rinambe’ Iehoda ka t’i Azà rekets’ i tane’ey naho i Askelone rekets’ i tane’ey, vaho i Ekrone rekets’ i tane’ey.
Anthu a fuko la Yuda analandanso mzinda wa Gaza ndi dziko lonse lozungulira, mzinda wa Asikeloni pamodzi ndi dziko lake lonse lozungulira, ndi mzinda wa Ekroni pamodzi ndi dziko lonse lozungulira.
19 Nindre am’ Iehoda t’Iehovà, nandroake o am-bohibohitseo, fe tsy nahafaniotse o an-tane petrakeo ty amo saretem-bi’ iareoo.
Yehova anathandiza anthu a fuko la Yuda. Iwo analanda dziko la kumapiri, koma sanathe kuwachotsa anthu ku zigwa, chifukwa anali ndi magaleta azitsulo.
20 Le natolo’e amy Kalebe ty Kebrone ty amy saontsi’ i Mosèy; vaho rinoa’e boak’ao i ana-dahi’ i Anake telo rey.
Monga analonjezera Mose, Kalebe anapatsidwa Hebroni. Kalebe anapirikitsa mafuko atatu a Anaki mu mzindamo.
21 Tsy nahafandroake o nte-Iebosý nimoneñe e Ierosalaimeo t’i Beniamine; le mitrao-pimoneñe amo ana’ i Beniamineo pake henane o nte Iebosìo.
Koma fuko la Benjamini linalephera kuwachotsa Ayebusi, amene amakhala mu Yerusalemu. Choncho Ayebusiwo akukhalabe ndi fuko la Benjamini mu Yerusalemu mpaka lero.
22 Aa naho i anjomba’ Iosefey, naname i Betele ka iereo vaho nolora’ Iehovà.
A banja la Yosefe nawonso anathira nkhondo mzinda wa Beteli, ndipo Yehova anali nawo.
23 Nirahe’ i anjomba’ Iosefey ty hisarisary i Betele, i nitokaveñe ty hoe Loze taoloy.
Anatumiza anthu kuti akazonde Beteli. Mzindawo kale unkatchedwa Luzi.
24 Nahaoniñe ondaty niakatse i rovay i mpisary rey, le hoe iereo tama’e, Atorò anay ty lalam-pimoahañe amo rovao, le hitretreza’ay.
Anthu okazondawo anaona munthu akutuluka mu mzindamo ndipo anamuwuza kuti, “Tisonyeze njira yolowera mu mzindamu, ndipo ife tidzakuchitira chifundo.”
25 Aa ie natoro’e ty fizilihañe amy rovay, le linafa’ iareo am-pibara i rovay, fe napo’ iareo hañavelo mb’eo indatiy reketse ty hasavereña’e iaby.
Choncho iye anawaonetsa njirayo, ndipo iwo anapha anthu onse mu mzindamo ndi lupanga koma munthu uja pamodzi ndi banja lake sanawaphe.
26 Nomb’ an-tane’ o nte Kiteo indatiy le namboatse rova vaho natao’e Loze ty añara’e, le mbe ie henaneo.
Ndipo iye anapita ku dziko la Ahiti, kumene anamangako mzinda nawutcha dzina lake Luzi. Mpaka lero lino mzindawo dzina lake ndi lomwelo.
27 Fe tsy nahafaniotse o mpimone i Betseane naho o tanà’eo ndra i Tànake naho o tanà’eo, ndra o mpimone’ i Dore naho o tanà’eo, ndra o mpimone’ Ibleame naho o tanà’eo, ndra i Megido naho o tanà’eo t’i Menasè; amy te nifahatse amy taney o nte-Khanàne nimoneñ’ aoo.
Koma a fuko la Manase sanachotse nzika za mzinda wa Beti-Seani pamodzi ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapena nzika za mzinda wa Taanaki ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapenanso nzika za mzinda wa Dori ndi mʼmidzi yake yozungulira. Iwo sanapirikitse nzika za mzinda wa Ibuleamu ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapena mzinda wa Megido ndi mʼmidzi yake yozungulira. Choncho Akanaani anapitirirabe kukhala mʼdzikomo.
28 Ie añe naho naozatse t’Israele le nampandoa’e haba o nte-Khanàneo fa tsy fonga niroaheñe.
Aisraeli atakhala amphamvu, anawagwiritsa Akanaaniwo ntchito yakalavulagaga, koma sanawapirikitse.
29 Tsy nahafaniotse o nte-Khanàne nimoneñe e Gezereo ka t’i Efraime, fe nitrao-pimoneñe am’ iereo e Gezere ao o nte-Khanàneo.
Nawonso Aefereimu sanathamangitse Akanaani amene amakhala mu Gezeri, choncho Akanaaniwo ankakhalabe pakati pawo ku Gezeriko.
30 Tsy niroahe’ i Zebolone ka o mpimone’ i Kitroneo, ndra o mpimone’ i Nahaloleo, le nitrao-pimoneñe am’ iereo o nte-Khanàneo vaho nampandoàñe haba.
Azebuloni sanathamangitse Akanaani amene amakhala mu Kitironi kapena a ku Nahaloli. Iwo ankakhala pakati pawo ndipo ankawagwiritsa ntchito yakalavulagaga.
31 Tsy niroahe’ i Asere ka o mpimone’ i Akòo ndra o mpimone’ i Tsidoneo, ndra o Aklabeo, ndra i Kelbà, ndra i Afike, ndra i Rekobe;
A fuko la Aseri nawo sanathamangitse amene amakhala mu Ako, Sidoni, Ahilabu, Akizibu, Heliba, Afiki, ndi Rehobu.
32 te mone nitrao-pimoneñe amo nte-Khanàne mpimoneñe amy taneio t’i Asere; fa tsy nilefe’e ty naniotse iareo.
Choncho anthu a fuko la Aseri anakhala pakati pa Akanaani amene ankakhala mʼdzikomo popeza sanawapirikitse.
33 Tsy niroahe’ i Naftalý ka o mpimone’ i Bete’semeseo, ndra o mpimone’ i Bet’anateo; te mone nitrao-pimoneñe amo nte-Khanàne mpimoneñe amy taneio; aa le nampandoa’e haba o mpimone’ i Bete-semese naho Bet’anateo.
Nalonso fuko la Nafutali silinathamangitse anthu amene ankakhala ku Beti Semesi kapena ku Beti Anati. Koma Anafutaliwo ankakhala pakati pa Akanaaniwo mʼdzikomo. Koma anthu amene ankakhala ku Beti Semesi ndi ku Beti Anati anawasandutsa kukhala ogwira ntchito yathangata.
34 Nazi’ o nte-Amoreo mb’ am-bohibohitse ao o ana’ i Daneo, le tsy nenga’ iareo hizotso mb’am-bavatane mb’eo.
Aamori anapirikitsira anthu a fuko la Dani ku dziko la ku mapiri popeza sanawalole kuti atsikire ku chigwa.
35 Nimanea’ o nte-Amoreo ty himoneñe am-bohi-Karese e Ai’ialone naho e Saalbime ao; fe nahagioke ty fità’ Iosefe vaho nanoe’e mpandoa haba.
Aamori anatsimikiza mtima zokhalabe ku phiri la Hara-Heresi, ku Ayaloni, ndiponso ku Saalibimu. Koma a fuko la Yosefe anakula mphamvu ndipo anagwiritsa Aamoriwo ntchito yakalavulagaga.
36 Nifototse amy fitroara’ i Akrabimey ty efe-tane’ o nte-Amoreo, boak’ amy vatoy mañambone.
Malire a Aamori anayambira ku chikweza cha Akirabimu nʼkulowera ku Sela napitirira kumapita chakumapiri ndithu.