< Jeremia 27 >
1 Niheo am’ Iirmeà ty tsara’ Iehovà ami’ty fifotoram-pifehea’ Iehoiakime ana’ Iosia, mpanjaka’ Iehodà, nanao ty hoe:
Zedekiya mwana wa Yosiya, mfumu ya ku Yuda, atangoyamba kulamulira, Yehova anawuza Yeremiya kuti,
2 Hoe t’Iehovà amako: mañamboara bandy naho joka, le ano ampititia’o eo;
“Tenga zingwe zomangira ndi mitengo ya goli ndipo uzimangirire mʼkhosi mwako.
3 naho ampañitrifo amy mpanjaka’ i Edomey naho amy mpanjaka’ i Moabey, naho amo ana’ i Amoneo, naho amy mpanjaka’ i Tsorey, vaho amy mpanjaka’ i Tsidoney am-pità’ o niraheñe mb’amy Tsidkia mpanjaka’ Iehodà e Ierosalaime mb’etoio;
Tsono utumize uthenga kwa mafumu a Edomu, Mowabu, Amoni, Turo ndi Sidoni kudzera mwa amithenga amene abwera ku Yerusalemu kwa Zedekiya, mfumu ya Yuda.
4 vaho ampitaroño amo talè’eo iereo hinday ty hoe: Hoe t’Iehovà’ i Màroy, i Andrianañahare’ Israeley: Saontsio ty hoe o talè’ areoo:
Uwapatse uthenga wokapereka kwa ambuye awo ndipo uwawuze kuti: Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Mukawuze ambuye anu kuti:
5 Izaho ty namboatse ty tane toy, ondatio naho o biby an-tarehe’ ty tane toio ami’ty haozarako ra’elahy naho an-tañako natorakitsy; vaho hatoloko ami’ty atao mahity a’ masoko.
Ndi mphamvu zanga ndi dzanja langa lamphamvu ndinalenga dziko lapansi ndi anthu ake onse pamodzi ndi nyama zili mʼmenemo, ndipo ndimalipereka kwa aliyense amene ndikufuna.
6 Ie amy zao fa natoloko am-pità’ i Nebokadnetsare mpanjaka’ i Bavele, mpitoroko, o tane iaby retoañe; vaho hatoloko aze ka o hare an-kivokeo hitoroñe aze.
Tsopano ndidzapereka mayiko anu onse kwa mtumiki wanga Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni. Ndamupatsanso nyama zakuthengo zonse kuti zimutumikire.
7 Le hitoroñe aze naho i ana’ey vaho i zafe’ey ze kila’ fifeheañe ampara’ te tondroke ty andro’ i tane’ey; vaho hondevoze’ ty tane maro naho mpanjaka ra’elahy.
Anthu a mitundu yonse adzamutumikira iyeyo, mwana wake ndi chidzukulu chake mpaka nthawi itakwana yoti dziko lake liwonongedwe. Pamenepo mitundu yambiri ndi mafumu amphamvu adzamugonjetsa.
8 Ie amy zay, ze fifeheañe naho fifelehañe mifoneñe tsy hitoroñe i Nebokadnetsare mpanjaka’ i Bavele, vaho tsy hanolotse ty fititia’e ambane’ ty joka’ i mpanjaka’ i Baveley: le ho tiliheko am-pibara naho an-kasalikoañe vaho angorosy i fifeheañey, hoe t’Iehovà, ampara’ te nampangotomomoheko am’pità’e.
“‘Koma ngati anthu a mtundu wina uliwonse kapena ufumu wina uliwonse adzakana kutumikira Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kapena kusenza goli lake, Ine ndidzalanga mtundu umenewo ndi lupanga, ndi njala ndi mliri, akutero Yehova, mpaka nditawapereka mʼmanja mwake kotheratu.
9 Aa inahareo, ko haoñe’ areo o mpitoki’ areoo naho o mpañandro’ areoo naho o mpañinofi’ areoo naho o mpisikili’ areoo vaho o jini’ areo manao ama’ areoo ty hoe: Tsy ho toroñe’ areo i mpanjaka’ i Baveley;
Choncho musamvere aneneri anu, owombeza anu, otanthauza maloto anu, amawula anu kapena amatsenga anu akamakuwuzani kuti, ‘Simudzatumikira mfumu ya ku Babuloni.’
10 amy t’ie mitoky vande, hampisitahañe anahareo lavitse ty tane’ areo; izaho ty handroake anahareo mb’eo, hivetrake añe.
Iwo akukuloserani zabodza kotero kuti adani adzakuchotsani mʼdziko lanu nʼkupita nanu ku dziko lakutali. Ndidzakupirikitsani ndi kukuwonongani kotheratu.
11 Fe ze fifelehañe minday ty fititia’e ambane’ ty joka’ i mpanjaka’ i Baveley, naho mitoroñe aze, le hengako hidoñe amy tane’ey i fifelehañe zay, hoe t’Iehovà; le havae’e vaho himoneñe ao.
Koma ngati mtundu wina uliwonse udzagonjera mfumu ya ku Babuloni ndi kuyitumukira, ndidzawusiya kuti ukhale mʼdziko lake kuti uzilima ndi kukhalamo, akutero Yehova.’”
12 Aa le hene vinolako amy Tsedkià mpanjaka’ Iehodà i tsaray, ami’ty hoe, Ampiambaneo ami’ty jokam-panjaka’ i Bavele ty fititia’ areo, vaho itoroño naho ondati’eo, le miveloma.
Uthenga womwewu ndinawuzanso Hezekiya mfumu ya Yuda. Ndinati, “Gonjerani mfumu ya ku Babuloni. Itumikireni iyoyo pamodzi ndi anthu ake ndipo mudzakhala ndi moyo.
13 Ino ty hikoromaha’o, ihe naho ondati’oo, ami’ty fibara, ty hasalikoañe, vaho ty angorosy, amy nitsarae’ Iehovà amy ze fifeheañe tsy mete hitoroñe ty mpanjaka’ i Bavele?
Nanga inu ndi anthu anu, muferenji ndi lupanga, ndi njala, ndi mliri, zimene Yehova waopsezera mtundu wina uliwonse umene sudzatumikira mfumu ya ku Babuloni?
14 Aa le ko haoñe’ areo o enta’ i mpitoky misaontsy ama’ areoio ty hoe: Tsy hitoroñe ty mpanjaka’ i Bavele nahareo. Ie mpitoky mandañitse ama’ areo.
Musamvere mawu a aneneri akamakuwuzani kuti, ‘Simudzatumikira mfumu ya ku Babuloni,’ chifukwa zimene akukuloseranizo nʼzabodza.
15 Amy te tsy niraheko, hoe t’Iehovà, ie mitoky vìlañe ami’ty añarako, soa te ho roaheko añe vaho hikorokomake, inahareo rekets’ o mpitoky mitoky ama’ areoo.
Sindinawatume ngakhale iwo akulosera mʼdzina langa. Nʼchifukwa chake, ndidzakupirikitsani ndipo mudzawonongeka kotheratu, inu pamodzi ndi aneneri amene akunenera zabodza kwa inu.”
16 Nivolañeko ka o mpisoroñeo, naho ondaty iaby retoa ty hoe: Hoe t’Iehovà: Ko mañaoñe ty saontsi’ o mpitoki’ areo ie mitoky ty hoe: Ingo, fa hampolieñe boak’e Bavele añe aniany o fingan’ anjomba’ Iehovàio, f’ie mitoky vande.
Kenaka ndinawuza ansembe pamodzi ndi anthu ena onse kuti, “Yehova akuti: Musamvere aneneri amene akumanena kuti, ‘Posachedwapa ziwiya za mʼNyumba ya Yehova zibwera kuchokera ku Babuloni.’ Iwowo akunenera zabodza kwa inu.
17 Ko ijanjiñañe; toroño ty mpanjaka’ i Bavele, le miveloma, fa akore te hampangoakoaheñe ty rova toy?
Musawamvere. Tumikirani mfumu ya ku Babuloni, ndipo mudzakhala ndi moyo. Mzindawu usandukirenji bwinja?
18 Aa naho toe mpitoky iereo, naho am’ iereo ao ty tsara’ Iehovà, le ehe t’ie hihalaly am’ Iehovà’ i Màroy henaneo, te tsy hasese e Bavele añe o fanake sisa amy anjomba’ Iehovày naho amy anjomba’ i mpanjaka’ Iehodày vaho e Ierosalaimeo.
Ngati iwo ndi aneneri ndipo ali ndi mawu a Yehova, apempheretu kwa Yehova Wamphamvuzonse kuti ziwiya zimene zatsala mʼNyumba ya Yehova ndi mʼnyumba ya mfumu ya Yuda ndiponso mu Yerusalemu zisatengedwe kupita ku Babuloni.
19 Fa hoe t’Iehovà’ i Màroy ty amo fahañeo naho i riakey naho o fototseo naho ze harao’e ila’e mbe an-drova atoa;
Pakuti Yehova akunena za zipilala, za mbiya ya madzi, maphaka ndi ziwiya zina zimene zatsala mu Yerusalemu.
20 o tsy nendese’ i Nebokadnetsare mpanjaka’ i Baveleo, ie nasese’e boak’ Iersosalaime ao pake Bavele añe an-drohy t’Iekonia ana’ Iehoiakime, mpanjaka’ Iehodà naho o roandria’ Iehodà naho Ierosalaimeo;
Izi ndi zimene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni sanatenge pamene anatenga ukapolo Yekoniya mwana wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda kupita ku Babuloni kuchokera ku Yerusalemu, pamodzi ndi anthu olemekezeka a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu.
21 eka, hoe t’Iehovà’ i Màroy, o fanake sisa añ’ anjomba’ Iehovà ao naho añ’ anjomba’ i mpanjaka’ Iehodà Ierosalaimeo;
Inde, Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akunena za zinthu zimene zinatsala mʼNyumba ya Yehova ndi mʼnyumba ya mfumu ya Yuda ndi mu Yerusalemu kuti,
22 toe hendeseñe mb’e Bavele mb’eo, le hidoñe añe ampara’ ty andro hitilihako iereo, hoe t’Iehovà, izay vaho hakareko boak’ ao le hampoliko mb’an-toetse atoy.
‘Zidzatengedwa kupita ku Babuloni ndipo zidzakhala kumeneko mpaka tsiku limene ndidzawakumbukirenso,’ akutero Yehova. ‘Pamenepo ndidzazitenganso ndi kuzibwezanso ku malo ano.’”