< Jeremia 24 >

1 Nitoroa’ Iehovà, te ingo ty haroñe roe pea sakoañe napok’ aolo’ i anjomba’ Iehovày eo; ie fa nasese’ i Nebokadnetsare mpanjaka’ i Bavele boak’ Ierosalaime ao mb’ am-pandrohizañe añe t’Ie­konià ana’ Iehoiakime mpanjaka’ Iehodà naho o ana-dona’ Iehodào, rekets’ o mpandranji’eo naho o mpanefe’eo, vaho nendese’e mb’e Bavele mb’eo.
Nebukadinezara, mfumu ya ku Babuloni anatenga ukapolo Yekoniya mwana wa Yehoyakimu mfumu ya ku Yuda pamodzi ndi nduna zake, anthu aluso ndi akatswiri a ku Yuda ndi kupita nawo ku Babuloni. Pambuyo pake Yehova anandionetsa madengu awiri a nkhuyu atayikidwa pa khomo pa Nyumba ya Yehova.
2 An-karoñe raik’ ao ty sakoañe fanjaka, manahake o sakoañe matoeo, fe sakoañe vata’e raty, tsy mete kamaeñe, o amy hàroñe ila’eio.
Mʼdengu limodzi munali nkhuyu zabwino kwambiri, ngati nkhuyu zoyambirira kucha. Mʼdengu linalo munali nkhuyu zoyipa kwambiri zosati nʼkudya.
3 Le hoe t’Iehovà amako: Ino o isa’o eoo, Iirmeà? Aa hoe iraho, Sakoañe; ty sakoañe soa, toe fanjaka; naho ty raty, vata’e lo tsy ho kamaeñe ami’ty haratia’e.
Yehova anandifunsa kuti, “Yeremiya, kodi ukuona chiyani?” Ndinayankha kuti, “Ndikuona nkhuyu zabwino kwambiri ndi nkhuyu zoyipa zosati nʼkudya.”
4 Le niheo amako ty tsara’ Iehovà nanao ty hoe:
Tsono Yehova anandiwuza kuti,
5 Hoe t’Iehovà, Andria­na­ñahare’ Israele, hambañe amy sakoañe soa reroy ty fisareako o ana’ Iehodà nampiakareko an-toetse toy mb’an-tane’ o nte-Kasdioo ho ami’ty hasoa.
“Ine Yehova, Mulungu wa Israeli ndikuti, ‘Anthu a ku Yuda amene ndinawachotsa ku malo ano nʼkupita nawo ku ukapolo ku dziko la Ababuloni ndikuwafanizira ndi nkhuyu zabwinozi.
6 Fa hapetako am’ iereo an-kasoa o masokoo, naho hampoliko mb’an-tane atoy, vaho haràfiko fa tsy haro­tsako; hamboleko fa tsy hombotako.
Ndidzaonetsesa kuti ndiwachitire zabwino ndipo ndidzabwera nawonso ku dziko lino. Ndidzawamanga osati kuwapasula; ndidzawadzala osati kuwazula.
7 Hitolo­rako arofo hahafohiñe ahy, te Izaho Iehovà; le ho ondatiko iereo, vaho ho Andrianañahare’ iareo iraho; amy t’ie himpoly amako an-kaliforañ’ arofo.
Ndidzawapatsa mtima woti andidziwe kuti ndine Yehova. Adzakhala anthu anga ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, chifukwa adzabwerera kwa Ine ndi mtima wawo wonse.
8 Le ty amo sakoañe raty tsy mete kamaeñeo; hoe t’Iehovà: Toe haitoako t’i Tsidkià, mpanjaka’ Iehodà, naho o roandria’eo naho ty sehanga’ Ierosa­laime, o napok’ an-tane atoio vaho o mpañialo an-tane Mitsraimeo.
“‘Koma monga nkhuyu zoyipa zija, zomwe ndi zoyipa kwambiri zosati nʼkudya,’ Yehova akuti, ‘ndi mmene ndidzalangire Zedekiya mfumu ya ku Yuda, nduna zake pamodzi ndi otsala a mu Yerusalemu, kaya adzakhala ali mʼdziko muno kapena mʼdziko la Igupto.
9 Hanoeko fangebahebahañe amo fifehea’ ty tane toy iabio ho an-kaloloañe; ho inje naho oha-drehake, fikizahañe naho fatse, amy ze hene toetse handroahako iareo.
Ndidzawasandutsa chinthu chonyansa kwa maufumu onse a dziko lapansi, chinthu chonyozeka ndi chopandapake, chinthu chochitidwa chipongwe ndi chotembereredwa kulikonse kumene ndidzawabalalitsira.
10 Vaho hahitriko am’ iereo ty fibara naho ty kerè naho ty angorosy ampara’ t’ie mongotse amy tane natoloko iareo naho an-droae’ iareoy.
Ndidzawatumizira nkhondo, njala ndi mliri mpaka atawonongedwa mʼdziko limene ndinawapatsa iwo ndi makolo awo.’”

< Jeremia 24 >