< Estera 10 >
1 Nampandoa’ i Akasverose mpanjaka rorotse i taney naho o tokonose an-driakeo.
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 Le ty fitoloñan-kaozara’e naho i hafatrara’ey naho ty talily heneke amy hara’elahi’ i Mordekaiy, ty nampionjona’ i mpanjakay aze, tsy fa sinokitse amy bokem-pamoliliam-panjaka’ i Meday naho i Parasey hao?
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 Amy te nifaharoe’ i Akasverose mpanjakay t’i Mordekay nte-Iehoda, ie nira’elahy amo nte-Iehodao, noron-droahalahi’e maro naho mpipay hañasoa ondati’eo vaho mpitaron-kanintsiñe amo tarira’eo.
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.