< 2 Samoela 7 >

1 Ie amy zao, fa nimoneñe añ’ an­jom­ba’e ao i mpanjakay vaho hene nampitofae’ Iehovà ze rafe­lahi’e mb’ etia mb’etia,
Mfumu itakhazikika mʼnyumba yake yaufumu, Yehova atayipatsa mpumulo kwa adani ake onse woyizungulira,
2 le hoe i mpanjakay amy Natane, mpitoky: Eo hey! Mimoneñe añ’ anjomba mendoraven-draho, fe mimoneñe an-damba miradorado ao ty vatam-pañinan’ Añahare.
mfumuyo inawuza mneneri Natani kuti, “Ine pano ndikukhala mʼnyumba yomanga ndi mitengo ya mkungudza, pomwe Bokosi la Mulungu lili mu tenti.”
3 Le hoe t’i Natane amy mpanjakay: Akia, ano ze hene añ’ arofo’o; fa ama’o t’Iehovà.
Natani anayankha mfumu kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu chifukwa Yehova ali nanu.”
4 Fe amy haleñey avao, niheo amy Natane ty tsara’ Iehovà nanao ty hoe:
Usiku umenewo mawu a Yehova anafika kwa Natani ndipo anati,
5 Akia, saontsio t’i Davide mpitoroko: Hoe ty nafè’ Iehovà: Ihe hao ty hamboatse anjomba himoneñako?
“Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti: kodi ndiwe amene udzandimangira Ine nyumba yokhalamo?
6 Izaho tsy nimoneñe an-traño sikal’ amy nampiavotako boake Mitsraime añe o ana’ Israeleoy, pak’ androany, fa i kiboho­tsey naho i kivohoy ty nombako.
Ine sindinakhalepo mʼnyumba kuyambira tsiku limene ndinatulutsa Aisraeli mʼdziko la Igupto mpaka lero lino. Ndakhala ndikuyenda uku ndi uku ndipo mokhala mwanga munali mu tenti.
7 Aa vaho fa nametse tsara raike hao iraho am-pifokoa’ Israele ndra aman’ iaia amo hene tane nombako mindre amo ana’ Israeleo, o nandiliako hamahañe ondatiko Is­rae­leoo, ty hoe: Manao akore te tsy nandranjia’o anjomba mendoraven-draho?
Konse ndakhala ndikuyenda ndi Aisraeli onse, kodi ndinanenapo kwa wina aliyense atsogoleri awo, amene ndinamulamula kuweta anthu anga Aisraeli kuti, nʼchifukwa chiyani simunandimangire nyumba ya mitengo ya mkungudza?’”
8 Aa le zao ty ho saontsie’o amy mpitoroko Davidey: Hoe t’Iehovà’ i Màroy: Rinambeko am-piandrazañe ao irehe, am-pañorihañe añondry, ho mpifelek’ ondatiko Israeleo.
“Ndipo tsopano umuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti: Ine ndinakutenga ku busa ukuweta nkhosa kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Aisraeli.
9 Fa nindre ama’o iraho ndra aia’ aia ty nañaveloa’o, naho zinamako aolo’o ey o rafelahi’o iabio; mbore hitolorako tahinañe ra’elahy, manahake o jabajaba an-tane atoio.
Ineyo ndinali nawe kulikonse kumene unkapita, ndipo ndachotsa adani ako onse pamaso pako. Tsopano ndidzakuza dzina lako kuti likhale mʼgulu la mayina a anthu otchuka kwambiri pa dziko lapansi.
10 Le hanendreako toetse ondatiko Israeleo, le hajadoko iereo, songa himoneñe an-toe’e, tsy ho tsoboreñe ka; vaho tsy hanolo-tsotry am’iareo ka o anan-katsivokarañeo, manahake te taolo,
Ndipo ndidzawapatsa malo anthu anga Aisraeli ndipo ndidzawadzala pamalo awoawo kuti asadzavutitsidwenso. Anthu oyipa sadzawazunzanso monga ankachitira poyamba paja,
11 sikal’ amy andro nililieko mpizaka hifehe ondatiko Israeleio. Le hampitofàko amo rafelahi’o iabio irehe. Tovo izay, Mitaroñe ama’o t’Iehovà t’ie hanoa’ Iehovà anjomba.
monga akhala akuchitira kuchokera nthawi imene ndinasankha atsogoleri a anthu anga Aisraeli. Ine ndidzakupatsaninso mpumulo kwa adani anu onse. “‘Yehova akulengeza kwa iwe kuti Iye mwini adzakhazikitsa banja lako:
12 Ie heneke o an­dro’oo, naho hirotse aman-droae’o ao, le horizako ty tiri’o hanonjohy azo, ty hiboak’ an-tsandri’o, le hajadoko i fifeleha’ey.
Masiku ako akadzatha ndipo ukadzakapuma ndi makolo ako, Ine ndidzawutsa mphukira yako imene idzalowa mʼmalo mwako, imene idzachokera mʼthupi mwako, ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wake.
13 Ie ty handranjy anjomba ho amy añarakoy, le horizako ho nainai’e i fifeleha’ey.
Iye ndiye amene adzamangire nyumba Dzina langa, ndipo Ine ndidzakhazikitsa ufumu wake kwamuyaya.
14 Ho rae ama’e iraho, le ho anake amako re; aa ie mandilatse le ho lafaeko an-kobai’ ondatio, naho am-pamofoha’ o ana’ ondatio;
Ine ndidzakhala abambo ake, ndipo iye adzakhala mwana wanga. Akadzachita choyipa, Ineyo ndidzamulanga ndi ndodo ndi zikwapu za anthu.
15 fe tsy hasintak’ ama’e ty fitretrezako, manahake ty nampisintahako aze amy Saole, i naviko aolo’o.
Koma sindidzasiya kumukonda, monga ndinachitira ndi Sauli, amene ndinamuchotsa iwe usanakhale mfumu.
16 Hioreñe ho fatratse nainai’e añatrefa’o ty fifehea’o vaho hajadoñe ho kitro añ’afe’e ty fiambesa’o.
Nyumba yako ndi ufumu wako zidzakhala zamuyaya pamaso panga. Mpando wako waufumu udzakhazikika kwamuyaya!’”
17 Nita­roñe’ i Natane amy Davide i tsara zay naho i hene aroñaroñey.
Natani anafotokozera Davide mawu onse avumbulutso limene analandira.
18 Aa le nizilik’ ao t’i Davide mpanjaka niambesatse añatrefa’ Iehovà, nanao ty hoe; Ia v’iraho ry Talè Iehovà vaho ino i trañokoy te nendese’o pak’eo?
Choncho Davide analowa mu tenti nakhala pamaso pa Yehova, ndipo anati: “Inu Yehova Wamphamvuzonse, ine ndine yani, ndipo banja langa nʼchiyani kuti mundifikitse pamene ndafikapa?”
19 f’ie mbe loho kede am-pihaino’o, ry Talè Iehovà, kanao nitsarae’o i akibam-pitoro’oy t’ie ho haehae añe ka; ie toe fañoha ondaty, ry Talè Iehovà?
Ndipo kukhala ngati izi ndi zosakwanira pamaso panu, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, mwayankhula zatsogolo la banja la mtumiki wanu. Kodi umu ndi mmene mumachitira ndi munthu, Inu Ambuye Wamphamvuzonse?
20 Aa ino ka ty hivolaña’ i Davide? amy te Ihe ro maharofoanañe o mpitoro’oo ry TalèIehovà.
Kodi Davide anenenso chiyani kwa Inu? Pakuti Inu Ambuye Wamphamvuzonse mukumudziwa mtumiki wanu.
21 O tsara’oo naho o arofo’oo ty nanoa’o o raha ra’elahy iaby zao, naho nampibentara’o amo mpitoro’oo.
Chifukwa cha mawu anu komanso mwa chifuniro chanu, mwachita chinthu chachikulu ichi ndipo mwachiwulula kwa mtumiki wanu.
22 Aa le onjonen-dRehe ry Rañandria Iehovà, fa tsy amam-pihambañe, vaho tsy eo t’i Andrianañahare hatovoñ’ Azo, ty amy ze he’e jinanjin-dravembia’ay.
Inu ndinu wamkulu, Yehova Wamphamvuzonse! Palibe wina wofanana nanu, ndipo palibe Mulungu wina koma Inu nokha, monga tamvera ndi makutu athu.
23 Aa ia ka ty fifeheañe ambone’ ty tane toy mañirin­kiriñe ondati’o Israeleo, ie navoten’ Andrinañahare hijebañe aze hondati’e, hanoa’e tahinañe, hitoloña’e raha fanjaka naho tsitantane ho an-tane’o añatrefa’ ondaty jineba’o amo fifeheañeo naho amo ‘ndrahare’eo ho azo boak’ an-tane Mitsraimeo?
Ndipo ndi ndani wofanana ndi anthu anu Aisraeli, mtundu wokhawo pa dziko lapansi umene Mulungu wake anapita kukawuwombola monga anthu akeake ndi kukadzitchukitsa yekha pochita zinthu zodabwitsa zazikulu, pothamangitsa mitundu ina ndi milungu yawo pamaso pa anthu ake, amene Inu munawawombola ku Igupto?
24 naho najado’o ho azo ondati’o Israeleo ho foko’o nainai’e, ry Iehovà vaho te Ihe ro Andrianañahare’ iareo.
Inu mwawapanga anthu anu Aisraeli kukhala anuanu kwamuyaya, ndipo Inu, Inu Yehova ndinu Mulungu wawo.
25 Ie amy zao, ry Iehovà Andrianañahare, ajadoño ho nainai’e i nitsarae’o o mpitoro’oo naho i anjom­ba’eiy; aa le ano i linaño’oy.
“Ndipo tsopano Yehova Mulungu, sungani kwamuyaya lonjezo limene mwachita ndi mtumiki wanu ndi banja lake. Chitani monga mwalonjezera,
26 Honjoneñe nainai’e ty tahina’o, soa te ho saon­tsieñe ty hoe: Iehovà’ i Màroy ro Andrianañahare’ Israele; vaho hioreñe nainai’e añatrefa’o ty anjomba’ o mpitoro’o Davideo.
kotero dzina lanu lidzakhala lotchuka mpaka muyaya. Ndipo anthu adzanena kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse ndi Mulungu wa Israeli!’ Ndipo banja la mtumiki wanu Davide lidzakhazikika pamaso panu.
27 Fa nabenta’o amo mpitoro’oo, ry Iehovà’ i Màroy, Andrianañahare’ Israeleo ami’ty hoe: Handranjiako anjomba; aa le nahasibek’ an-troke ty mpitoro’o hitaroñe o halaly zao.
“Inu Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, mwaululira mtumiki wanu ponena kuti, ‘Ine ndidzakumangira iwe nyumba!’ Nʼchifukwa chake ine mtumiki wanu ndalimba mtima kupemphera motere.
28 Toe Ihe ry Talè Iehovà, Ihe avao ro Andrianañahare, naho o tsara’oo ro to vaho nampitamae’o amo mpitoro’oo o raha soa zao;
Inu Ambuye Wamphamvuzonse, ndinu Mulungu! Mawu anu ndi odalirika, ndipo mwalonjeza zinthu zabwinozi kwa mtumiki wanu.
29 ie henaneo, ehe te ho no’o ty hitahy ty akibam-pitoro’o hitoloña’e nainai’e añatrefa’o, ty amy nitsara’oy ry Talè Iehovà; le lonik’ abey te ho soa-tahy nainai’e ty akibam-pitoro’o am-pitahia’o.
Ndipo tsopano chikukomereni kudalitsa banja la mtumiki wanu, kuti likhale mpaka muyaya pamaso panu. Pakuti Inu, Yehova Wamphamvuzonse, mwayankhula, ndipo ndi mʼdalitso wanu banja la mtumiki wanu lidzakhala lodalitsika mpaka muyaya.”

< 2 Samoela 7 >