< 1 Mpanjaka 1 >

1 Ie amy zao fa bey naho nigain-kantetse t’i Davide mpanjaka; aa ndra t’ie nisafo-damba tsy nahazo hafanàñe.
Mfumu Davide atakalamba sankamva kufunda ngakhale akamufunditsa mabulangeti.
2 Aa le hoe o mpitoro’eo ama’e: Ho paiañe somondrara ki’e i talèko mpanjakay, ie hijohañe añatrefa’ i mpanjakay, hiatrak’ aze, naho hàndre añ’araña’e, hahazoa’ i talèko mpanjakay hafanàñe.
Choncho nduna zake zinamuwuza kuti, “Tiloleni tifune namwali woti azikhala nanu ndi kumakusamalirani. Namwaliyo azigona pafupi nanu kuti mbuye wathu mfumu muzimva kufundira.”
3 Aa le nanitsike i tane Israeley iereo nitsoeke ty ampela soa; le nitendreke t’i Abisage nte-Sonamý vaho na­sese amy mpanjakay.
Kotero anafunafuna mʼdziko lonse la Israeli mtsikana wokongola ndipo anapeza Abisagi wa ku Sunemu, nabwera naye kwa mfumu.
4 Toe nimontramontra i somondraray; naho niatrake i mpanjakay vaho nitoroñ’ aze fe tsy niolora’ i mpanjakay.
Mtsikanayo anali wokongola kwambiri ndipo ankasamalira mfumu ndi kumayitumikira, koma mfumuyo sinakhale naye malo amodzi.
5 Nisenge-vatañe amy zao t’i Adonià ana’ i Kagite, ami’ty hoe: Izaho ty ho mpanjaka. Aa le nihentseñe’e sarete naho mpiningi-tsoavala vaho ondaty limampolo ho mpilay aolo’e.
Nthawi imeneyi Adoniya, mwana wa Hagiti, anayamba kudzitukumula ndipo anati, “Ndidzakhala mfumu ndine.” Choncho anadzikonzera galeta ndi akavalo, pamodzi ndi anthu 50 woti azithamanga patsogolo pake.
6 Mbe lia’e tsy nibosehan-drae’e ami’ ty hoe: Manao akore o anoe’oo? toe ni-ondaty maràm-bintan-dre, nanonjohy i Absalome te nasamake.
(Abambo ake sanalowererepo nʼkamodzi komwe ndipo sanafunsepo kuti, “Nʼchifukwa chiyani ukuchita zimenezi?” Adoniyayo anali wokongola kwambiri ndipo anali wopondana ndi Abisalomu).
7 Nivesoveso am’ Ioabe ana’ i Tseroia naho amy Abiatare mpisoron-dre; le norihe’ iereo t’i Adonià nañolotse aze.
Adoniya anagwirizana ndi Yowabu mwana wa Zeruya ndiponso Abiatara wansembe, ndipo iwowa anamuthandiza.
8 Fe tsy nimpiami’ Adonià t’i Tsadoke mpisoroñe naho i Benaià ana’ Iehoiada naho i Natane mpitoky naho i Simeý naho i Reý vaho o fanalolahi’ i Davideio.
Koma Zadoki wansembe, Benaya mwana wa Yehoyada, mneneri Natani, Simei ndi Rei ndiponso asilikali amphamvu a Davide sanamutsate Adoniya uja.
9 Nandenta añondry naho añombe naho kobatròke marine ty lamilami’ i Tsokelete añ’ila’ i En-drogele eo t’i Adonià; le kinoi’e iaby o longo’eo, o ana’ i mpanjakaio vaho o nte-Iehoda mpitoro’ i mpanjakaio;
Kenaka Adoniya anapereka nsembe za nkhosa ndi ngʼombe ndiponso ana angʼombe onenepa ku Mwala wa Zohereti kufupi ndi Eni Rogeli. Iye anayitana abale ake onse, ana aamuna a mfumu ndiponso akuluakulu onse a ku Yuda,
10 fe tsy kinanji’e t’i Natane mpitoky naho i Benaià, naho o fanalolahio vaho i Selomò rahalahi’e,
koma sanayitane mneneri Natani kapena Benaya kapenanso asilikali amphamvu a Davide ngakhalenso mʼbale wake Solomoni.
11 Aa le nisaontsy amy Betesebà rene’ i Selomò t’i Natane ami’ty hoe, Tsy jinanji’o hao te fa mifehe t’i Adonià ana’ i Hagite, vaho tsy fohi’ i Davide talèntika?
Pamenepo Natani anafunsa Batiseba, amayi ake a Solomoni, kuti, “Kodi simunamve kuti Adoniya, mwana wa Hagiti, walowa ufumu popanda Davide mbuye wathu kudziwa?
12 Antao arè, angao hitolorako hevetse, handrombaha’o ty fiai’o naho ty fiai’ i ana’o Selo­mòy.
Tsopano ine ndikulangizeni inu mmene mungapulumutsire moyo wanu ndi moyo wa mwana wanu Solomoni.
13 Akia mb’amy Davide mpanjaka mb’eo, le ano ty hoe: Tsy nifantà’o amo mpitoro’o ampelao hao, ry talèko mpanjaka, ty hoe: Toe hanonjohy ahy t’i Selomò ana’o hifehe, hiambesatse am-pitobohako eo? aa vaho akore t’i Adonià, ie mifeheo?
Pitani msanga kwa Mfumu Davide ndipo mukanene kuti, ‘Mbuye wanga mfumu, kodi simunalumbire kwa ine mdzakazi wanu kuti, ‘Ndithu mwana wako Solomoni ndiye adzakhale mfumu mʼmalo mwanga, ndipo adzakhala pa mpando wanga waufumu?’ Nanga nʼchifukwa chiyani Adoniya walowa ufumu?’
14 Aa ihe mbe mitaroñe amy mpanjakay, le horihako ao hañonjoñe o saontsi’oo;
Pamene inu muzikayankhula ndi mfumu, ine ndidzalowa ndi kuchitira umboni mawu anuwo.”
15 Aa le niheo mb’ amy mpanjakay añ’efe’e ao t’i Betesebà: toe niloho bey i mpanjakay ie natrafe’ i Abi­sage nte Sonamý i mpanjakay.
Choncho Batiseba anapita nakalowa ku chipinda kukaonana ndi mfumu imene inali itakalamba kwambiri, kumene Abisagi wa ku Sunemu uja ankayisamalira.
16 Nidrodrètse t’i Betesebà naho niambane amy mpanjakay. Le hoe i mpanjakay: Ino o paia’oo?
Batiseba anagwada nalambira mfumu. Mfumu inamufunsa kuti, “Kodi nʼchiyani chimene ukufuna?”
17 Le hoe re tama’e, O ry talèko: Nifanta’o añamy Iehovà Andria­naña­hare’o amy anak’ ampata’o, ty hoe: Toe hanonjohy ahy am-pifeheañe t’i Selo­mò ana’o, vaho ie ty hitobok’ amy fiambesam-pifeheakoy.
Iye anayankha kuti, “Mbuye wanga, inu mwini munalumbira kwa ine mdzakazi wanu mʼdzina la Yehova Mulungu wanu kuti, ‘Solomoni mwana wako ndiye adzakhale mfumu mʼmalo mwa ine, ndipo adzakhala pa mpando wanga waufumu.’
18 Fe inao te mifehe t’i Adonià henanekeo vaho tsy fohi’o ry talèko mpanjaka;
Koma tsopano Adoniya ndiye walowa ufumu, ndipo inu mbuye wanga mfumu, simukuzidziwa zimenezi.
19 mbore fa nandenta añombe naho kobatroke vaho añondry tsifotofoto re le kinoi’e iaby o anam-panjakao, naho i Abiatare mpisoroñe, vaho Ioabe mpifelek’ i valobohòkey; fe tsy kinanji’e t’i Selomò mpitoro’o.
Ndipo wapereka nsembe ngʼombe zambiri, ana angʼombe onenepa ndi nkhosa ndi mbuzi ndipo wayitana ana anu onse, wansembe Abiatara ndiponso Yowabu mkulu wa ankhondo, koma sanayitane kapolo wanu Solomoni.
20 Ie amy zao hene ama’o, ry talèko mpanjaka ty fihaino’ Israele, ty hitaroña’o te ia ty hiambesatse amy fiambesan-talèko mpanjakay hanonjohy aze.
Mbuye wanga mfumu, maso a Aisraeli onse ali pa inu, kuti adziwe kuchokera kwa inu amene adzakhala pa mpando waufumu wa mbuye wanga mʼmalo mwanu.
21 Naho tsy izay, hifetsake te, ie mirotse an-droae’e ao ty talèko mpanjaka, le hatao mpandilatse iraho naho i Selomò anako.
Mukapanda kutero, mbuye wanga, mukadzangotisiya nʼkulondola kumene kunapita makolo anu, ine pamodzi ndi mwana wangayu Solomoni adzatiyesa owukira.”
22 Ie mbe nisaon­tsy amy mpanjakay, le nimoak’ ao t’i Natane mpitoky
Pamene Batiseba amayankhula ndi mfumu, mneneri Natani analowa.
23 vaho nitohine’e ami’ty hoe i mpanjakay, Ingo t’i Natane mpitoky. Aa ie tafa-zilik’ amy mpanjakay, le nibokobokok’ aolo’ i mpanjakay, nihohok’ an-tane ty lahara’e.
Ndipo anthu anawuza mfumu kuti, “Kwabwera mneneri Natani.” Kotero iye anafika pamaso pa mfumu ndipo anawerama nagunditsa nkhope yake pansi.
24 Le hoe t’i Natane, Ry talèko mpanjaka, Nitaroñe ty hoe hao irehe te i Adonià ty hifehe manonjohy azo, le ie ty hiambesatse amy fiambesa’oy?
Natani anafunsa kuti, “Mbuye wanga mfumu, kodi mwalengeza kuti Adoniya adzakhala mfumu mʼmalo mwanu, ndi kuti adzakhala pa mpando wanu waufumu?
25 Amy t’ie nizotso mb’eo anindroany nandenta añombe naho kobatroke naho añondry maro vaho nambarà’e iaby o anam-panjakao naho o mpifelek’ i valobohòkeio naho i Abiatare mpisoroñe; ie mikama naho mitohok’ añ’atrefa’e eo, manao ty hoe, Lava havelo ry Adonià mpanjaka.
Lero lomwe lino wakapereka nsembe ngʼombe zambiri, ana angʼombe onenepa ndiponso nkhosa ndi mbuzi. Iye wayitana ana anu onse, atsogoleri a nkhondo, ndiponso wansembe Abiatara. Panopa onsewa akudya ndi kumwa naye ndipo akunena kuti, ‘Akhale ndi moyo wautali mfumu Adoniya!’
26 Fe izaho, izaho mpitoro’o, naho i Tsadoke mpisoroñe, naho i Benaià ana’ Iehoiadà, vaho i Se­lomò mpitoro’o—tsy nambara’e.
Koma ine kapolo wanu, wansembe Zadoki ndi Benaya mwana wa Yehoyada, ndiponso kapolo wanu Solomoni sanatiyitane.
27 Nanoen-talèko mpanjaka hao izao, ie tsy natoro’o amo mpitoro’oo ty hanonjohy azo hiambesatse am-piambesan-talèko mpanjaka?
Kodi zimenezi mbuye wanga mfumu mwazichita ndinu, osawawuza atumiki anu kuti adziwe amene adzakhale pa mpando waufumu mʼmalo mwanu?”
28 Aa hoe ty natoi’ i Davide mpanjaka, Kanjio homb’ amako mb’ etoa t’i Betesebà. Le niheo mb’ añatrefa’ i mpanjakay mb’eo re, nijohañe aolo’ i mpanjakay.
Pamenepo mfumu Davide anati, “Muyitaneni Batiseba.” Kotero Batiseba analowa ndipo anayimirira pamaso pa mfumu.
29 Le nifanta ty hoe i mpanjakay: Kanao veloñe t’Iehovà nijebañe ty fiaiko amy ze haoreañe iaby,
Tsono mfumu inalumbira kuti, “Pali Yehova wamoyo, amene anandipulumutsa ine ku mavuto onse,
30 tsy kalafo te nifantàko ama’o añam’ Iehovà, Andrianañahare’ Israele, ty hoe: Hifehe handimbe ahy t’i Selomò ana’o, le ie ty handimbe ahy hiambesatse amy fitobohakoy. Toe hanoeko anito.
ndithu ine lero ndichita zonse zimene ndinalumbira kwa Yehova Mulungu wa Israeli kuti, mwana wako Solomoni adzakhala mfumu mʼmalo mwanga ndipo adzakhala pa mpando wanga waufumu.”
31 Nidròdreke mb’an-tane ty lahara’ i Bete-sebà, niambane amy mpanjakay, nanao ty hoe: Lonik’ abey te ho veloñe nainai’e ty talèko Davide mpanjaka.
Pamenepo Batiseba anawerama, nagunditsa mutu wake pansi nalambira mfumu, ndipo anati, “Mbuye wanga Mfumu Davide mukhale ndi moyo wautali!”
32 Le hoe t’i Davide mpanjaka, Kanjio homb’ amako mb’etoa t’i Tsadoke mpisoroñe, naho i Natane mpitoky, vaho i Benaià ana’ Iehoiadà. Aa le nomb’ añatrefa’ i mpanjakay mb’eo iereo.
Mfumu Davide anati, “Ndiyitanireni wansembe Zadoki, mneneri Natani ndi Benaya mwana wa Yehoyada.” Atafika pamaso pa mfumu,
33 Le hoe i mpanjakay am’ iereo: Endeso ama’ areo o mpitoro’ i talè’ areoio, le ampiningiro amy borikekoy t’i Selomò, le aseseo hizotso mb’e Gihone mb’eo;
mfumuyo inati kwa iwo, “Tengani atumiki anga ndipo mukweze mwana wanga Solomoni pa bulu wanga ndipo mupite naye ku Gihoni. Mukalize lipenga ndi kufuwula kuti, ‘Akhale ndi moyo wautali mfumu Solomoni!’
34 le hañory aze ho mpanjaka’ Israele t’i Tsa­doke mpisoroñe naho i Natane mpitoky; le popòho i antsivay, vaho ano ty hoe: Mahavelo t’i Selomò mpanjaka.
Kumeneko Zadoki wansembe ndi mneneri Natani akamudzoze kuti akhale mfumu ya Israeli. Kenaka mukalize lipenga ndi kumanena kuti ‘Akhale ndi moyo wautali Mfumu Solomoni.’
35 Le mionjona mb’ etoa am-pañorihañ’ aze, le homb’eo re hiambesatse amy fitobohakoy, amy te ie ty handimbe ahy ho mpanjaka; ie ty jinoboko hifehe Israele naho Iehodà.
Ndipo pobwera muzikamutsata pambuyo. Iyeyo akabwere kuno ndi kudzakhala pa mpando wanga waufumu ndi kudzalamulira mʼmalo mwanga. Ndamusankha kukhala wolamulira Israeli ndi Yuda.”
36 Aa le hoe ty natoi’ i Benaià ana’ Iehoiada amy mpanjakay: Amena! Lonike t’ie ty hanoe’ Iehovà Andrianañaharen-talèko mpanjaka.
Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu kuti, “Ameni! Yehova Mulungu wa mbuye wanga mfumu akhazikitse kuti zichitike motero.
37 Hambañ’ amy nindreza’ Iehovà amy talèko mpanjakaiy ty hindreza’e amy Selomò, naho honjone’e ambone’ ty fiambesa’ i talèko Davide mpanjakay i fiambesa’ey.
Monga momwe Yehova wakhalira ndi inu mbuye wanga mfumu, momwemonso akhale ndi Solomoni ndi kukhazikitsa ufumu wake kuti ukhale waukulu kuposa ufumu wa mbuye wanga Mfumu Davide!”
38 Aa le nizotso mb’eo t’i Tsadoke mpisoroñe naho i Natane mpitoky naho i Benaià ana’ Iehoiada naho o nte-Kereteo naho o nte Peleteo le natongoa’ iereo amy borìke’ i Davide mpanjakay t’i Selomò vaho nasese’ iereo mb’e Gihone mb’eo.
Kotero Zadoki wansembe, mneneri Natani, Benaya mwana wa Yehoyada, Akereti ndiponso Apeleti, anthu oteteza mfumu, anapita kukamukweza Solomoni pa bulu wa Mfumu Davide ndi kupita naye ku Gihoni.
39 Le nakare’ i Tsadoke i tsifa ama’menake boak’ amy Kivohoiy naho noriza’e t’i Selo­mò vaho nipopoeñe i antsivay; le hene nirihoñe ty hoe ondatio, Mahavelo ry Selomò mpanjaka.
Wansembe Zadoki anatenga nyanga ya mafuta yochokera ku malo opatulika ndi kumudzoza Solomoni. Kenaka analiza lipenga ndipo anthu onse anafuwula kuti, “Akhale ndi moyo wautali Mfumu Solomoni!”
40 Nionjomb’eo am-pañorihañe aze ondaty iabio; nitio-tsoly vaho nirebeke an-kafaleam-bey, kanao nahariatse i taney ty fikontsiaña’ ondatio.
Ndipo anthu onsewo anapita namutsatira pambuyo akuyimba zitoliro ndi kukondwerera kwambiri, kotero nthaka inagwedezeka chifukwa cha phokoso lawo.
41 Jinanji’ i Adonià naho o nambarà’eo, ie vaho nianjam-pikama. Le hoe t’Ioabe naho nahajanjiñe ty feo’ i antsivay: Ino o fipoñafan-drañoraño an-drovao?
Adoniya pamodzi ndi anthu onse oyitanidwa amene anali naye anamva zimenezi pamene ankamaliza madyerero awo. Atamva kulira kwa malipenga, Yowabu anafunsa kuti, “Kodi phokoso lonselo mu mzindamo likutanthauza chiyani?”
42 Ie mbe nisaontsy, ingo, pok’eo t’Ionatane ana’ i Abiatare mpisoroñe: le hoe t’i Adonià: Miziliha, ry lahy manjofake, mpinday entan-tsoa.
Iye akuyankhula, Yonatani mwana wa wansembe Abiatara anafika. Adoniya anati, “Lowa. Munthu wabwino ngati iwe ayenera kubweretsa nkhani yabwino.”
43 Le hoe ty natoi’ Ionatane amy Adonià, Toe i Selomò ty nanoe’ i Davide mpanjaka talèn-tika, mpanjaka;
Yonatani anayankha Adoniya kuti, “Ayi ndithu, zinthu sizili bwino! Mbuye wathu Mfumu Davide walonga Solomoni ufumu.
44 naho nirahe’ i mpanjakay hindre ama’e t’i Tsadoke mpisoroñe naho i Natane mpitoky naho i Benaià ana’ Iehoiadà naho o nte-Kereteo naho o nte-Peleteo, le nampiningire’ iereo amy borì’ i mpanjakaiy;
Mfumu yatuma Zadoki wansembe, mneneri Natani, Benaya mwana wa Yehoyada, Akereti ndi Apeleti ku Gihoni ndipo iwo amukweza pa bulu wa mfumu,
45 vaho noriza’ i Tsadoke mpisoroñe naho i Natane mpitoky ho mpanjaka e Gihone ao re; mivoamboañe boak’ ao an-drebeke iereo kanao mañeno-tsatsake o rovao. Izay o korakoràke janji’ areoo.
ndipo Zadoki wansembe ndi mneneri Natani adzoza Solomoni ku Gihoni kuti akhale mfumu. Ndipo kuchokera kumeneko akhala akululutira, kotero kuti mu mzinda monse muli phokoso lokhalokha. Ndiyetu phokoso limene mukulimvalo.
46 Eka! fa miambesatse amy fiambesam-pifeheañey t’i Selomò.
Ndipo Solomoni wakhala kale pa mpando wake waufumu.
47 Nimb’eo ka o mpitoro’ i mpanjakaio hitata i Davide mpanjaka talèn-tika ami’ty hoe: Honjone’ i Andrianañahare’o ambone’ ty tahina’o ty tahina’ i Selomò vaho hampitoabore’e ambone’ i fiambesa’oy ty fiambesa’e; le niondrek’ am-pandrea’e eo i mpanjakay.
Kuwonjezera pamenepo, nduna za mfumu zabwera kale kudzayamika mbuye wathu Mfumu Davide, pomanena kuti, ‘Mulungu wanu atchukitse dzina la Solomoni kuposa dzina lanu ndipo ufumu wake ukule kupambana ufumu wanu!’ Ndipo mfumu inawerama niyamba kupembedza pa bedi lake,
48 Tinovo’ i mpanjakay ty ti-hoe, Andriañeñe t’Iehovà, Andrianañahare’ Israele, nanolotse ty hiambesatse amy fitobohakoy anindroany, hahatreava’ o masokoo.
inati, ‘Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli, amene wasankha wolowa mʼmalo mwanga ine ndikanali ndi moyo lero lino.’”
49 Fonga nangebahebak’ amy zao o nambarà’ i Adoniào, le niongake, songa ninankañe mb’ an-dala’e mb’eo.
Anthu onse amene Adoniya anawayitana ananjenjemera ndi mantha, ndipo anayimirira, kenaka anamwazikana.
50 Nirevendreveñe amy zao t’i Adonià ty amy Selomò, le niavotse mb’eo nivontititse amo tsifa’ i kitreliio.
Koma Adoniya, poopa Solomoni, anapita ku Nyumba ya Mulungu nakagwira msonga za guwa lansembe.
51 Aa le nisaontsieñe amy Selomò ty hoe: Inao! mañeveñe amy Selomò mpanjaka t’i Adonià, kanao tambozore’e o tsifan-kitrelio, le hoe ty asa’e, Ehe te hifanta amako anito t’i Selomò mpanjaka tsy hanjevoñe i mpitoro’ey am-pibara.
Tsono Solomoni anawuzidwa kuti, “Adoniya akukuopani inu Mfumu Solomoni ndipo wagwira msonga za guwa lansembe. Iye akuti, ‘Mfumu Solomoni alumbire kuti sadzapha kapolo wake ndi lupanga.’”
52 Le hoe t’i Selomò, Naho miboake hondaty vañon-dre, leo raik’ amo maroi’eo tsy hipok’ an-tane; f’ie tendrehan-kaloloañe le hihomake.
Solomoni anayankha kuti, “Ngati iyeyo aonetse kuti ndi munthu wakhalidwe labwino, ngakhale tsitsi la mʼmutu mwake silidzathothoka ndi kugwera pansi, koma akapezeka kuti ali ndi khalidwe loyipa, adzafa ndithu.”
53 Aa le nañirake t’i Selo­mò mpanjaka, vaho nazotso’ iareo amy kitreliy. Nimb’eo re niambane amy Selo­mò mpanjaka; le hoe ty Se­lomò ama’e: Akia mb’ añ’akiba’o añe.
Pamenepo Mfumu Solomoni inatuma anthu ndipo anakamutenga paguwa paja. Adoniya anabwera ndi kudzalambira Mfumu Solomoni, ndipo Solomoni anati, “Pita ku nyumba yako.”

< 1 Mpanjaka 1 >