< 1 Mpanjaka 5 >

1 Nirahe’ i Kirame, mpanjaka’ i Tsore mb’amy Selomò mb’eo o mpitoro’eo, ie nahajanjiñe t’ie norizañe ho mpanjaka handimbe an-drae’e; amy te nainai’e nimpirañetse amy Davide t’i Kirame.
Hiramu mfumu ya ku Turo atamva kuti Solomoni wadzozedwa kukhala mfumu mʼmalo mwa abambo ake Davide, anatumiza akazembe ake kwa Solomoni, chifukwa mfumu Hiramu inali pa ubale wabwino ndi Davide nthawi zonse.
2 Aa le nampihitrife’ i Selomò amy Kirame, ty hoe:
Solomoni anabweza mawu awa kwa Hiramu:
3 Fohi’o te tsy nahafamboatse anjomba ho a i tahina’ Iehovà Andrianañahare’ey t’i Davide raeko, ty amo hotakotake niariseho azeo ampara’ t’ie napo’ Iehovà ambane’ o lelam-pandia’eo.
“Inu mukudziwa kuti chifukwa cha nkhondo zimene zinkachokera ku mbali zonse kulimbana ndi abambo anga, iwo sanathe kumangira Nyumba Yehova Mulungu wawo, mpaka Yehova atawayika adani awo pansi pa ulamuliro wawo.
4 Fe tinolo’ Iehovà Andrianañahareko fitofàñe ty miariary ahy iaby henanekeo, amy t’ie tsy aman-drafelahy ndra raha mizo.
Koma tsopano Yehova Mulungu wanga wandipatsa mtendere mbali zonse za dziko ndipo ndilibe mdani kapena chovuta chilichonse.
5 Ingo, hoe ty volako, Handranjiako anjomba ty tahina’ Iehovà Andrianañahareko, ty amy tsinara’ Iehovà an-draeko Davidey, ty hoe: Ty ana’o hampiambesarako am-piambesa’o ty hamboatse anjom­ba ho ami’ty añarako.
Choncho ine ndikufuna kumangira nyumba Yehova Mulungu wanga, monga momwe Iye anawuzira abambo anga Davide kuti, ‘Mwana wako amene ndidzamukhazike pa mpando waufumu mʼmalo mwako ndiye adzandimangire Nyumba.’
6 Aa le lilio ty hamiràñe mendo­raveñe e Lebanone ao, le hindre amo mpi­toro’oo o mpitorokoo vaho hatoloko ama’o ho a o mpi­toro’oo ty tambe toñone’o ho a iareo, ie fohi’o te tsy ama’ay ty mahafira hatae manahake o nte-Tsidoneo.
“Choncho lamulani kuti andidulire mikungudza ya ku Lebanoni. Anthu anga adzagwira ntchito imeneyo pamodzi ndi anthu anuwo, ndipo ine ndidzalipira anthu anuwo malipiro amene inu mungakhazikitse. Inu mukudziwa kuti ife tilibe anthu aluso locheka matabwa monga Asidoni.”
7 Ie jinanji’ i Kirame i saontsi’ i Selo­mòy le vata’e nirebeke vaho nanao ty hoe: Andriañeñe t’Iehovà henane zao, Ie nanolotse i Davide anake mahihitse hifeleke ondaty jabajaba retoañe.
Hiramu anakondwa kwambiri atamva uthenga wa Solomoni ndipo anati, “Lero Yehova atamandike chifukwa wapatsa Davide mwana wanzeru kuti alamulire mtundu waukuluwu.”
8 Aa le nahitri’ i Kirame amy Selomò ty hoe: Fa tsinanoko i nañitrifa’o ahiy le hene hanoeko o satrien’ arofo’oo amo mendoraveñe naho haradrantoo.
Tsono Hiramu anabweza mawu awa kwa Solomoni: “Ndalandira uthenga umene mwanditumizira ndipo ine ndidzachita zonse zimene mukufuna pokupatsani mitengo ya mkungudza ndi payini.
9 Hazotso’ o mpitorokoo boake Lebanone pak’ an-driak’ añe izay; le hamboareko t’ie hihafo amy riakey handenà’ iereo mb’amy toetse hatoro’o ahio, naho hakatrak’ añe, vaho ho rambese’o; le ihe ty hañeneke i fañiriakoy te hamahana’o mahakama ty akibako.
Anthu anga adzatsika nayo kuchokera ku Lebanoni mpaka ku nyanja, ndipo adzayiyandamitsa pa nyanja mpaka ku malo amene munene. Kumeneko ndidzayimasula ndipo mudzayitenga. Ndipo inu mudzakwaniritsa chokhumba changa pondipatsa chakudya cha banja langa laufumu.”
10 Aa le natolo’ i Kirame amy Selo­mò ze fonga mendoraveñe naho hara­dranto ni­paia’e.
Motero Hiramu anapereka kwa Solomoni mitengo yonse ya mkungudza ndi payini imene ankayifuna,
11 Natolo’ i Selo­mò amy Kirame ka ty vare-bolè ro’ale kore hama­­hana’e o añ’an­­jomba’eo, naho menake finofoke roapolo kore; izay ty natolo’ i Selo­mò amy Kirame taoñ’ an-taoñe.
ndipo Solomoni anamupatsa Hiramu mitanga ya tirigu 20,000 ngati chakudya cha pa nyumba yake, kuwonjezera pa migolo ya mafuta a olivi yokwana 20,000. Solomoni anapitiriza kupereka zimenezi chaka ndi chaka.
12 Tinolo’ Iehovà hihitse t’i Selomò, ty amy nitsa­rae’e ama’ey le nifampilongo t’i Kirame naho i Se­lomò; vaho nifanao fañina.
Yehova anamupatsa Solomoni nzeru monga momwe analonjezera. Panali ubale wa mtendere pakati pa Solomoni ndi Hiramu, ndipo awiriwa anachita pangano.
13 Aa le hene nampi­tsatoha’ i Selomò haba t’Israele, ondaty telo-ale i haba zay
Mfumu Solomoni inasonkhanitsa anthu ogwira ntchito ya thangata mʼdziko lonse la Israeli ndipo anthu athangatawo analipo 30,000.
14 vaho nampihitrife’e mb’e Lebanone mb’eo, rai-ale boa-bolañe ty nifandimbe, volañe raike e Lebanone añe naho roe volañe añ’ anjomba’e ao; i Adonirame ty nifehe i hàbay.
Iye ankatumiza anthu 10,000 ku Lebanoni pa mwezi mosinthanasinthana, kotero kuti ankakhala ku Lebanoniko mwezi umodzi ndipo kwawo ankakhalako miyezi iwiri. Adoniramu ndiye ankayangʼanira ogwira ntchito yathangatayo.
15 Fito-ale ty mpijiny kilanka’ i Selo­mò naho valo-ale ty namira am-bohitse añe;
Solomoni anali ndi anthu amtengatenga 70,000, anthu 80,000 osema miyala ku mapiri,
16 mandikoatse izay o mpifehe’ i Selomò nifelek’ o fitoloñañeoo: telo-arivo-tsi-telon-jato ty nifeleke ondatio amo fitoloña’eo.
ndi akapitawo 33,000 amene ankayangʼanira ntchitoyi ndiponso anthu ogwira ntchito zina.
17 Nandily t’i Selo­mò vaho nihaliañe vato jabajaba, vato soa, handranjiañe o mananta’ i anjombaio am-bato pinèke.
Molamulidwa ndi mfumu, anakumba ndi kusema miyala ikuluikulu kwambiri yoti akamangire maziko a Nyumba ya Mulungu.
18 Aa le rinamerame’ o mpandranji’ i Selomòo naho o mpamboa’ i Kirameo naho o nte-Gebaleo irezay, naho nañalankañe o hatae vaho vato nandranjiañe i anjombaio.
Amisiri a Solomoni ndi a Hiramu ndiponso anthu a ku Gebala anasema miyala ndi kukonza matabwa ndi miyala yomangira Nyumba ya Mulungu.

< 1 Mpanjaka 5 >