< 1 Mpanjaka 20 >
1 Nanontoñe i hene valobohò’ey amy zao t’i Benehadade mpanjaka’ i Arame, reketse mpanjaka telopolo-ro’amby naho soavala vaho sarete le nionjomb’eo nañarikatoke i Somerone hialia’e,
Tsono Beni-Hadadi mfumu ya ku Aramu inasonkhanitsa magulu ake onse a ankhondo. Iye pamodzi ndi mafumu 32, akavalo awo ndi magaleta awo, anapita kukawuzungulira mzinda wa Samariya ndi kuwuthira nkhondo.
2 le nampihitrife’e mb’amy Akabe mpanjaka’ Israele an-drova ao,
Iye anatuma amithenga ake mu mzindamo kwa Ahabu mfumu ya Israeli, kukanena kuti,
3 ty nampanoa’e ty hoe: Hoe t’i Benehadade: Ahy o volafoty naho volamena’oo; o vali’oo vaho o ana’oo, ahy ze hene soa ama’e.
“Beni-Hadadi akuti, ‘Siliva wako ndi golide wako ndi wanga, ndipo akazi ako okongola ndi ana ako ndi anganso.’”
4 Nanoiñe aze ty mpanjaka’ Israele nanao ty hoe: Ie i sinaontsi’oy, ry talèko mpanjaka, azo iraho naho ze hene hanañako.
Mfumu ya Israeli inayankha kuti, “Monga mmene mwanenera, mbuye wanga mfumu, ine pamodzi ndi zonse zomwe ndili nazo ndi zanu.”
5 Nibalike mb’eo indraike o ìrakeo, nanao ty hoe: Zao ty asa’ i Benehadade: Toe nahitriko ama’o ty hoe: Haseseo amako o volafoti’oo, naho o volamena’oo naho o vali’oo vaho o ana’oo;
Amithenga aja anabwereranso kwa Ahabu ndipo anamuwuza kuti, “Beni-Hadadi akuti, ‘Ine ndinakulamula kuti undipatse siliva wako ndi golide wako, akazi ako ndi ana ako.
6 fa hiraheko mb’ ama’o mb’eo hamaray ami’ty andro hoe zao o mpitorokoo, le ho kodebe’ iereo ty anjomba’o, naho o anjombam-pitoro’oo; le ze soa am-pihaino’o ty hapo’ iareo am-pità’e vaho hendese’e añe.
Koma mawa nthawi ngati yomwe ino ndidzatuma atumiki anga kudzafufuza mʼnyumba yako yaufumu ndi nyumba za akuluakulu ako. Iwo adzatenga chilichonse chimene umachidalira ndi kupita nacho.’”
7 Aa le songa kinoi’ i mpanjaka’ Israeley o roandria’ i taneio, nanao ty hoe: Ehe, isaho naho mahaoniña te midoha raha indatiy; fa pinai’e amako o valikoo naho o anakoo naho o volafotikoo naho o volamenakoo, le tsy niraràko.
Pamenepo mfumu ya Israeli inayitanitsa akuluakulu a mʼdzikomo niwawuza kuti, “Taonani momwe munthuyu akufunira kutibweretsera mavuto! Atatumiza mawu oti ndimupatse akazi anga ndi ana anga, siliva wanga ndi golide wanga, ine sindinamukanize.”
8 Le hoe o androanavio naho ze hene ondaty ama’e, Ko mañaoñe aze, vaho ko miantoke.
Akuluakulu onse ndi anthu onse anayankha kuti, “Musamumvere kapena kuvomereza zofuna zake.”
9 Aa le hoe re amy ìra’ i Benehadade rey: Saontsio ty hoe i talèko mpanjakay: Hene hanoeko o nañiraha’o amy mpitoro’oy am-baloha’eo; fe tsy hanoeko o raha zao. Aa le nienga o ìrakeo, ninday i entañe zay.
Tsono Ahabu anayankha amithenga a Beni-Hadadi kuti, “Kamuwuzeni mbuye wanga mfumu kuti, ‘Mtumiki wanu adzachita zonse zimene munazifuna nthawi yoyamba ija, koma izi mwazifunazi sindingazikwanitse.’” Iwo anachoka nakapereka yankho kwa Beni-Hadadi.
10 Le hoe ty nañiraha’ i Benehadade ama’e: Ee te hanoe’ o ‘ndrahareo amako ndra mandikoatse naho mahaatsam-pità’ ze hene ondaty mañorik’ ahikoo ty debo’ i Somerone.
Pamenepo Beni-Hadadi anatumizanso uthenga wina kwa Ahabu kuti, “Milungu indilange koopsa, ngati mu Samariya mudzakhale fumbi loti nʼkudzaza dzanja la aliyense wa anthu anga.”
11 Le hoe ty natoi’ i mpanjaka’ Israeley: Taroño ama’e: Ee te tsy hirengevoke manahake ty mañafake fikalañe ty mañombe aze.
Mfumu ya Israeli inayankha kuti, “Kamuwuzeni kuti, ‘Mwamuna mnzako nʼpachulu, nʼkulinga utakwerapo.’”
12 Ie nahajanjiñe izay t’i Benehadade, ie ninon-toake miharo amy mpanjaka rey an-kibohotse ao, le hoe re amo mpitoro’eo, Midadaña! Le nijadoñe niatreatre i rovay iereo.
Beni-Hadadi anamva uthenga umenewu pamene iye ankamwa ndi mafumu anzake mʼmatenti awo, ndipo analamula anthu ake kuti, “Konzekerani kukathira nkhondo.” Choncho anakonzekera kukathira nkhondo mzindawo.
13 Niheo amy Akabe mpanjaka amy zao ty mpitoky, nanao ty hoe: Hoe ty tsara’ Iehovà, Fa niisa’o hao o valobohòke miheneheneo? Ingo, hatoloko am-pità’o te anito, soa te ho fohi’o te Izaho Iehovà.
Ndipo taonani, mneneri wina anabwera kwa Ahabu mfumu ya Israeli nadzalengeza kuti, “Yehova akuti, ‘Kodi ukuchiona chigulu chachikulu cha ankhondochi? Taona, ndikuchipereka chimenechi lero mʼdzanja lako, ndipo pamenepo udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
14 Le hoe t’i Akabe: Añama’ ia? le hoe re: Hoe ty nafè’ Iehovà, o ajalahi’ o mpifehem-pokotaneo. Le hoe re: Ia ty hamototse i hotakotakey: le hoe ty natoi’e: Ihe.
Ahabu anafunsa kuti, “Koma ndani adzachita zimenezi?” Mneneri anayankha kuti, “Yehova akuti, ‘Adzachita zimenezi ndi asilikali a nduna za mʼzigawo.’” Ndipo iye anafunsa kuti, “Kodi ndani adzayambe nkhondoyi?” Mneneriyo anayankha kuti, “Ndinu.”
15 Aa le tinendre’e ty ajalahi’ o mpifehem-pokotaneo: roanjato-tsi-telopolo-ro’amby iereo; ie amy zao tinendre’e ka o fonga ondatio, ze hene ana’ Israele: fito-arivo.
Choncho Ahabu anawerenga asilikali achinyamata a nduna za mʼzigawo ndipo onse analipo 232. Ndipo anawerenganso ankhondo a ku Israeli ndipo onse analipo 7,000.
16 Niavotse an-tsingilingilieñe iereo. Fe ninoñe an-kibohotse ao t’i Benehadade himamoa’e, ie naho o mpanjakao, i mpanjaka telopolo-ro’ amby mpañolotse aze rey.
Iwo ananyamuka nthawi yamasana pamene Beni-Hadadi ndi mafumu 32 othandizana naye ankamwa mpaka kuledzera mʼmatenti awo.
17 Niavotse mb’eo valoha’e i ajalahi’ o mpifehem-pokotaneo rey; aa le nañirake t’i Benehadade, le nitaliliañe ty hoe: Ey ondaty miakatse i Someroneo.
Asilikali achinyamata a nduna za mʼzigawo ndiwo amene anayamba kupita ku nkhondo. Nthawi imeneyi Beni-Hadadi nʼkuti atatumiza anthu oti akazonde, amene anadzafotokoza kuti, “Anthu ankhondo akubwera kuchokera ku Samariya.”
18 Le hoe re, He niakatse an-kanintsiñe iereo, endeso veloñe; ke niakatse hifandrapake, endeso veloñe.
Iye anati, “Kaya akubwera mwamtendere kapena mwankhondo, muwagwire amoyo.”
19 Aa le niavotse i rovay iereo, i ajalahi’ o mpifehem-pokotaneo rey naho nañorike iareo o lahindefoñeo.
Choncho asilikali achinyamata a nduna za mʼzigawo anatuluka mu mzinda, gulu lankhondo lili pambuyo pawo.
20 Songa zinevo’ iareo ty ondati’e; vaho nitriban-day o nte-Arameo, le nihoridañe’ Israele; nipoliotse an-tsoavala reke-piningi-tsoavala t’i Benehadade mpanjaka’ i Arame.
Ndipo aliyense wa iwo anapha munthu wake. Ataona izi, Aaramu anathawa Aisraeli ali pambuyo pawo kuwapirikitsa. Koma Beni-Hadadi mfumu ya ku Aaramu anathawa atakwera pa kavalo pamodzi ndi ankhondo ena okweranso pa akavalo.
21 Niavotse amy zao i mpanjaka’ Israeley le zinama’e o soavala-aman-tsareteo vaho zinevo’e o nte-Arameo am-pizamanam-bey.
Mfumu ya Israeli inapita chitsogolo ndi kugwira akavalo ndi magaleta ndipo Aaramu ambiri anaphedwa.
22 Nimb’amy mpanjaka’ Israeley i mpitokiy, le nanoa’e ty hoe: Akia, mihaozara, le tsikarato naho hotsohotso o hanoe’oo; amy te hionjo-mb’etoa hiatreatre azo ty mpanjaka’ i Arame ami’ty fibalihan-taoñe.
Zitachitika izi, mneneri wina anabwera kwa mfumu ya Israeli ndipo anati, “Mulimbike ndipo muganize bwino zoti mudzachite, chifukwa chaka chikudzachi mfumu ya Aramu idzakuthiraninso nkhondo.”
23 Fa nanao ty hoe amy mpanjaka’ i Aramey o mpitoro’eo: Andrianañahare’ o haboañeo t’i Andrianañahare’ iareo; aa le naozatse te aman-tika iereo; antao arè hialy ama’e amontoñe añe; fa toe haozatse te am’ iereo tika.
Nthawi imeneyi, akuluakulu a mfumu ya Aramu anamulangiza kuti, “Milungu ya anthu a ku Israeli ndi milungu ya mʼmapiri. Nʼchifukwa chake anali ndi mphamvu zotipambana ife. Koma ngati tidzamenyana nawo ku chigwa, ndithudi ife tidzakhala ndi mphamvu kuposa iwo.
24 Le ano zao: Songa asitaho an-toe’e o mpanjakao vaho solò mpifeleke ty an-toe’ iareo;
Inu chitani izi: chotsani mafumu onse pa maudindo awo ndipo mʼmalo mwawo muyikemo atsogoleri a ankhondo.
25 mamolilia valobohòke manahake i valobohòke nimotso ama’oy, soavala hasolo soavala, sarete hasolo sarete; hifandrapak’ am’ iereo amontoñe ao tika vaho toe ho fatratse te ama’e. Hinao’e ty feo’ iareo le nanoe’e.
Musonkhanitsenso gulu lankhondo lofanana ndi lomwe linaphedwa lija, akavalo monga omwe anaphedwa aja, ndi magaleta monga omwe anawonongedwa aja, kuti tikamenyane ndi Israeli ku chigwa. Pamenepo, ife tidzapambana iwowo.” Beni-Hadadi anagwirizana nawo ndipo anachita momwemo.
26 Aa ie nihereñe ty taoñe le natonto’ i Benehadade o nte-Arameo, vaho nionjomb’e Afeke mb’eo hialy am’ Israele.
Chaka chinacho Beni-Hadadi anasonkhanitsa Aaramu, napita ku Afeki kukamenyana ndi Israeli.
27 Tinendre amy zao o ana’ Israeleo naho nivatieñe vaho niavotse niatrek’ ama’e; le nitobe aolo’ iereo o ana’ Israeleo hoe mpirai-liam-bik’ ose roe kedekedeke, ie nañatseke i taney o nte-Arameo.
Aisraeli atasonkhananso, napatsidwa zakudya zawo anapita kukakumana nawo. Aisraeli anamanga misasa yawo moyangʼanana ndi Aaramu ndipo ankaoneka ngati timagulu tiwiri ta mbuzi, pomwe Aaramu anali atakuta dera lonselo.
28 Nitotoke mb’eo amy zao ty ‘ndatin’ Añahare ninday tsara amy mpanjaka’ Israeley, ami’ty hoe: Hoe ty nafè’ Iehovà: Kanao nanao ty hoe o nte-Arameo: Andrianañahare’ o haboañeo t’Iehovà, fa tsy Andrianañahare’ o vavataneo; le fonga hatoloko am-pità’o i valobohòke bey heneheney vaho ho fohi’o te Izaho Iehovà.
Munthu wa Mulungu anabwera, nawuza mfumu ya Israeli kuti, “Yehova akuti, ‘Popeza Aaramu akuganiza kuti Yehova ndi mulungu wa ku mapiri, osati wa ku zigwa, Ine ndidzapereka chigulu chonsechi kwa iwe, ndipo iwe udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
29 Aa le nitobe nifañatreke fito andro iereo. Ie amy andro faha-fitoy le nionjoñe ty hotakotake; vaho zinevo’ o ana’ Israeleo ami’ty andro raike ty rai-hetse amo nte-Arame am-pandiao.
Kwa masiku asanu ndi awiri anakhala moyangʼanana mʼmisasa yawo, ndipo pa tsiku lachisanu ndi chiwiri nkhondo inayambika. Aisraeli anapha Aaramu okwana 100,000 tsiku limodzi lokha.
30 Le nitriban-day mb’e Afeke añe o ila’eo, mb’ an-drova ao; fe nikorovok’ am’ ondaty ro’ ale-tsi-fito-arivo sehanga’eo i kijoliy. Aa le nipolititse mb’ amy rovay t’i Benehadade, ami’ty efe’e am-po’e ao.
Ena onse otsala anathawira ku Afeki, kumene khoma linagwera anthu 27,000. Ndipo Beni-Hadadi anathawira mu mzinda, nakabisala mʼchipinda chamʼkati.
31 Le hoe o mpitoro’eo ama’e: Mahaoniña, fa tsinano’ay te mpanjaka mpitretrè o mpanjakan’ anjomba’ Israeleo; antao arè, mihalaly ama’o te hidian-gony am-bania tika naho hanampe vahotse añ’ambonen-tika vaho hiavotse mb’ amy mpanjaka’ Israeley mb’eo; he havotso’e ty fiai’o.
Atumiki ake anamuwuza kuti, “Taonani, ife tamva kuti mafumu a fuko la Israeli ndi achifundo. Tiyeni tipite kwa mfumu ya ku Israeli titavala ziguduli mʼchiwuno mwathu ndi kumanga zingwe mʼmakosi mwathu. Mwina iye sakakuphani.”
32 Aa le nisikin-gony am-bania iereo naho nanampe vahotse añ’ambone eo, vaho niavotse mb’amy mpanjaka’ Israeley mb’eo nanao ty hoe: Manao ty hoe ama’o i mpitoro’o Benehadadey: Miambane ama’o: angao ho velon-draho. Le hoe re: Toe mbe veloñe hao re? Rahalahiko ‘nio.
Atavala ziguduli mʼchiwuno mwawo ndi kumanga zingwe mʼmakosi mwawo, anapita kwa mfumu ya ku Israeli ndipo anayiwuza kuti, “Mtumiki wanu Beni-Hadadi akunena kuti, ‘Chonde loleni kuti ndikhale moyo.’” Mfumu inayankha kuti, “Kodi iye akanali ndi moyo? Iye ujatu ndi mʼbale wanga.”
33 Aa le rinambe’ indaty rey ho viloñe, ie tsinepak’ am-palie’e i saontsy zay vaho nanao ty hoe: I rahalahi’o Benehadadey ‘nio. Le hoe re: Akia hitrifo. Aa le niakatse mb’ama’e mb’eo t’i Benehadade naho najò’e an-tsarete’e ao,
Anthuwo ankaganiza kuti mawuwo anali abwino ndipo anavomereza mawuwa mofulumira. Iwo anati, “Inde, Beni-Hadadi ndi mʼbale wanu!” Mfumu inati, “Pitani kamutengeni.” Beni-Hadadi atatuluka, Ahabu anamukweza mʼgaleta lake.
34 vaho hoe t’i Benehadade ama’e: Hampoliko o rova rinamben-draeko aman-drae’oo naho hamboare’o dokany e Damesèk’ ao manahake o namboaren-draeko e Someroneo. Izaho ka, hoe t’i Akabe, havotsoko irehe amy fañina zay. Aa le nifañina’e vaho navotso’e.
Beni-Hadadi anawuza Ahabu kuti, “Ndidzabweza mizinda imene abambo anga analanda abambo anu. Ndipo mutha kumanga nyumba zanu zamalonda mu Damasiko, monga anachitira abambo anga ku Samariya.” Ahabu anati, “Chifukwa cha mgwirizano umenewu, ine ndidzakumasula.” Choncho anachita naye mgwirizano, ndipo anamulola kuti apite.
35 Teo amy zao t’indaty, ana-dahi’ o mpitokio, nisaontsy an-drañetse ty amy nitsara’ Iehovày, ty hoe: Ehe, lafao iraho. Fe tsy nimete handafa aze indatiy.
Molamulidwa ndi Yehova, mmodzi mwa ana a aneneri anawuza mnzake kuti, “Chonde, menye ndi chida chako,” koma mnzakeyo anakana.
36 Le hoe re tama’e, Kanao tsy nihaoñe’o ty fiarañanaña’ Iehovà, Inao! vata’e mieng’ ahy irehe le ho zevoñe’ ty liona. Aa le vata’e niavotse re, tendrek’ aze ty liona nañe-doza ama’e.
Choncho mneneriyo anati, “Chifukwa sunamvere Yehova, ukangochoka pano, mkango ukupha.” Ndipo munthuyo atangochoka pamenepo, mkango unamupeza ndi kumupha.
37 Nanjo ondaty indraike re, le nanoa’e ty hoe: Ehe, Lafao iraho. Aa le linafa’ indatiy, finofo’e vaho nahafere aze.
Mneneriyo anapeza munthu wina ndipo anamuwuza kuti, “Chonde, menye.” Choncho munthuyo anamumenya ndi kumuvulaza.
38 Le nienga mb’eo i mpitokiy, nandiñe i mpanjakay añ’olon-dalañe eo, ie nihonohono am-bandy ambonem-pihaino’e.
Pamenepo mneneriyo anapita nakayima pa msewu kudikirira mfumu. Iye anadzibisa nakulunga nsalu nkhope yake.
39 Aa ie niary eo i mpanjakay le kinanji’e i mpanjakay, nanoe’e ty hoe: Naneñateña i hotakotakey ty mpitoro’o, le teo te nivike t’indaty nanese t’indaty amako nanao ty hoe: Tano ondatio; fa ndra ino ty maha-tsi-eo aze, le ty fiai’o ho a’ ty fiai’e, ke hondroha’o volafoty talenta raike.
Mmene mfumu inkadutsa pamenepo, mneneriyo anafuwula kwa mfumuyo kuti, “Ine mtumiki wanu ndinalowa pakati pa nkhondo, ndipo munthu wina anabwera kwa ine atatenga mmodzi mwa anthu ogwidwa pa nkhondo, nandiwuza kuti, ‘Sunga munthu uyu. Ngati asowa, ndiye kuti ndidzakupha, kapena udzalipira ndalama 3,000 za siliva.’
40 Aa ie nitoloñe atoy naho aroy ty mpitoro’o, le nimosao re. Le hoe ty mpanjaka’ Israele ama’e: Aa le izay ty izakañ’ azo; izay ty linaha’o.
Pamene ine mtumiki wanu ndinali wotanganidwa apa ndi apa, munthuyo anasowa.” Mfumu ya Israeli inati, “Chimenechi ndiye chilango chako. Iwe wadziweruza wekha.”
41 Nafaha’e amy zao i bandy am-pihaino’eoy; le napota’ i mpanjakay t’ie mpiamo mpitokio.
Pamenepo mneneriyo anachotsa msangamsanga nsalu yomwe anakulunga pa nkhope yake, ndipo mfumu ya Israeli inamuzindikira kuti ndi mmodzi mwa aneneri.
42 Le hoe re tama’e: Hoe ty nafè’ Iehovà; Kanao navotso’o am-pità’o indaty tinendreko ho rotsaheñey, le ty fiai’o ty amy fiai’ey vaho ondati’oo ty am’ ondati’eo.
Iye anawuza mfumu kuti, “Yehova akuti, ‘Chifukwa chakuti mwamasula munthu amene Ine ndinati ndi woyenera kuphedwa, inuyo ndi amene mudzaphedwe mʼmalo mwa iyeyo, anthu anu mʼmalo mwa anthu ake.’”
43 Aa le nimpoly mb’ añ’anjomba’e mb’eo i mpanjaka’ Israeley, nilonjetse naho nioremèñe t’ie nipoke e Somerone ao.
Mwachisoni ndi mokwiya, mfumu ya Israeli inapita ku nyumba yake yaufumu ku Samariya.