< Salamo 87 >

1 Salamo nataon’ ny Koraïta. Tonon-kira.
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Ny vavahadin’ i Ziona dia tian’ i Jehovah mihoatra noho ny fonenana rehetra izay an’ i Jakoba.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Zava-malaza no anambarana anao Ry tanànan’ Andriamanitra. (Sela)
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Hanonona an-dRahaba sy Babylona Aho ho isan’ izay mahalala ahy; Indro Filistia sy Tyro mbamin’ i Etiopia, Ity no efa teraka teo.
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 Ary Ziona hilazana hoe: Ireto sy ireroa samy efa teraka teo; Ary ny Avo Indrindra no mampitoetra azy.
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Jehovah hanisa, raha manoratra ny firenena Izy: Ity no efa teraka teo. (Sela)
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Hoy izay mihira sy mandihy: Ny loharanoko rehetra dia ao aminao.
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Salamo 87 >