< Salamo 120 >

1 Fihirana fiakarana.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Jehovah ô, vonjeo ny fanahiko amin’ ny molotra mandainga, Eny, amin’ ny lela mamitaka
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Inona no homeny anao, ary inona koa no hataony aminao, Ry lela mamitaka?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Zana-tsipìkan’ ny mahery sady voaranitra, Mbamin’ ny vain’ afon’ anjavidy.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Lozako, fa mivahiny eto amin’ ny Maseka aho Ary mitoetra ato an-dain’ ny Kedarita!
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Ela loatra izay no nitoeran’ ny fanahiko teo amin’ Izay tsy tia fihavanana.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Raha izaho, dia fihavanana; Kanjo nony miteny aho, dia mila ady kosa ireny.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

< Salamo 120 >