< Zabbuli 50 >
1 Zabbuli ya Asafu. Oyo Owaamaanyi, Mukama Katonda, akoowoola ensi okuva enjuba gy’eva okutuuka gy’egwa.
Salimo la Asafu. Wamphamvuyo, Yehova Mulungu, akuyankhula ndi kuyitanitsa dziko lapansi kuyambira kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.
2 Katonda ayakaayakana ng’ava mu Sayuuni n’obulungi bw’ekitiibwa kye ekituukiridde.
Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri Mulungu akuwala.
3 Katonda waffe ajja, naye tajja kasirise, omuliro ogusaanyaawo buli kintu gwe gumukulembera, n’omuyaga ogw’amaanyi ne gumwetooloola.
Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete; moto ukunyeketsa patsogolo pake, ndipo pomuzungulira pali mphepo yamkuntho
4 Akoowoola abali mu ggulu ne ku nsi, azze okusalira abantu be omusango.
Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake.
5 Agamba nti, “Munkuŋŋaanyize abantu bange abaayawulibwa, abaakola nange endagaano nga bawaayo ssaddaaka.”
Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe.
6 Eggulu litegeeza obutuukirivu bwa Katonda kubanga Katonda yennyini ye mulamuzi.
Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza.
7 “Muwulirize, mmwe abantu bange, nange nnaayogera. Ggwe Isirayiri bino bye nkuvunaana: Nze Katonda, Katonda wo.
Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako.
8 Sikunenya lwa ssaddaaka zo, oba ebiweebwayo ebyokebwa by’ossa mu maaso gange bulijjo.
Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.
9 Sikyakkiriza nte nnume n’emu evudde mu kiralo kyo, wadde embuzi ennume ezivudde mu bisibo byo.
Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,
10 Kubanga buli nsolo ey’omu kibira yange, awamu n’ente eziri ku nsozi olukumi.
pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka.
11 Ennyonyi zonna ez’oku nsozi nzimanyi, n’ebiramu byonna eby’omu nsiko byange.
Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri ndiponso zolengedwa zonse zakutchire ndi zanga.
12 Singa nnumwa enjala sandikubuulidde: kubanga ensi n’ebigirimu byonna byange.
Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga.
13 Ndya ennyama y’ente ennume, wadde okunywa omusaayi gw’embuzi?
Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna kapena kumwa magazi a mbuzi?
14 “Owangayo ssaddaaka ey’okwebaza eri Katonda; era otuukirizanga obweyamo bwo eri oyo Ali Waggulu Ennyo.
“Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba.
15 Bw’obanga mu buzibu, nnaakuwonyanga, naawe onongulumizanga.”
Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso; Ine ndidzakulanditsa, ndipo udzandilemekeza.”
16 Naye omubi Katonda amugamba nti, “Lekeraawo okwatulanga amateeka gange, n’endagaano yange togyogerangako.
Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako?
17 Kubanga okyawa okuluŋŋamizibwa, n’ebigambo byange tobissaako mwoyo.
Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.
18 Bw’olaba omubbi, ng’omukwana; era weetaba n’abenzi.
Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo
19 Okolima era olimba; olulimi lwo lwogera ebitali bya butuukirivu.
Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa ndipo umakonza lilime lako kuchita chinyengo.
20 Muganda wo omwogerako bibi byereere buli kiseera, era owayiriza omwana wa nnyoko yennyini.
Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni.
21 Ebyo byonna obikoze, ne nsirika, n’olowooza nti twenkanankana. Naye kaakano ka nkunenye, ebisobyo byonna mbikulage.
Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako.
22 “Ggwe eyeerabira Katonda, ebyo bisseeko omwoyo, nneme kukuyuzaayuza nga tewali na wa kukuwonya.
“Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa:
23 Oyo awaayo ssaddaaka ey’okwebaza angulumiza, era ateekateeka ekkubo ndyoke mulage obulokozi bwa Katonda.”
Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza, ndipo amakonza njira zake kuti ndimuonetse chipulumutso cha Mulungu.”