< Banzembo 76 >
1 Wuta na buku ya mokambi ya bayembi. Ezali ya koyemba na lindanda. Nzembo ya Azafi. Nzambe ayebani kati na Yuda; Kombo na Ye ezali monene kati na Isalaele.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu. Mulungu amadziwika mu Yuda; dzina lake ndi lotchuka mu Israeli.
2 Ndako na Ye ya kapo ezali na Salemi; mpe esika na Ye ya kovanda ezali na Siona.
Tenti yake ili mu Salemu, malo ake okhalamo mu Ziyoni.
3 Ezali kuna nde abukaki makonga ya makasi, banguba, mipanga mpe bibundeli nyonso ya bitumba.
Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka, zishango ndi malupanga, zida zankhondo. (Sela)
4 Ozali kongenga lokola mwinda, otonda na lokumu koleka bangomba ya babotoli bomengo ya bitumba.
Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.
5 Bilombe nyonso ya mpiko bakweyisamaki, balalaki pongi na bango ya suka; basoda nyonso bakokaki lisusu te kotombola maboko.
Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma, Iwowo amagona tulo tawo totsiriza; palibe mmodzi wamphamvu amene angatukule manja ake.
6 Nzambe ya Jakobi, na kanda na Yo, bato oyo babundaka likolo ya bampunda elongo na bampunda bakweyi na somo.
Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo, kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi.
7 Solo, ozali somo! Nani akokoka kotelema liboso na Yo soki osiliki?
Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa. Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?
8 Wuta na likolo, osalaka ete mokano na Yo eyokana na matoyi ya bato; mokili ekomaka na kobanga mpe evandaka kimia
Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo, ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete,
9 tango, Yo Nzambe, otelemaka mpo na kosambisa mpe kobikisa banyokolami nyonso ya mokili.
pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze, kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko. (Sela)
10 Pamba te kanda makasi ya bato esanzolaka Yo, mpe olataka kanda ya batikali.
Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu.
11 Epai ya Yawe, Nzambe na bino, bopesa bilaka mpe bokokisa yango. Tika ete bato nyonso oyo bazingeli Ye bamemela Nzambe ya somo makabo!
Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse; anthu onse omuzungulira abweretse mphatso kwa Iye amene ayenera kuopedwa.
12 Abukaka lolendo ya bakambi, mpe bakonzi ya mokili babangaka Ye.
Iye amaswa mzimu wa olamulira; amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi.