< Psalmi 3 >
1 Dāvida dziesma, kad tas bēga no sava dēla Absaloma. Ak Kungs! cik daudz manu pretinieku! Daudz, kas ceļas pret mani
Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu. Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira!
2 Daudz saka uz manu dvēseli: tai pestīšanas nav pie Dieva.(Sela.)
Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” (Sela)
3 Bet Tu, Kungs, esi par bruņām ap mani, mana godība un kas paceļ manu galvu.
Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza, Inu mwandiveka ulemerero ndipo mwanditukula.
4 Es piesaucu To Kungu ar savu balsi, un Viņš mani paklausa no Sava svētā kalna. (Sela)
Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera. (Sela)
5 Es apgūlos un aizmigu, un atmodos, jo Tas Kungs mani uztur
Ine ndimagona ndi kupeza tulo; ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza.
6 Es nebīstos no daudz tūkstošiem ļaužu, kas visapkārt pret mani stājās.
Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene abwera kulimbana nane kuchokera ku madera onse.
7 Celies, Kungs, glābi mani, mans Dievs, jo Tu visiem maniem ienaidniekiem siti vaigā, Tu bezdievīgiem salauzi zobus.
Dzukani, Inu Yehova! Pulumutseni, Inu Mulungu wanga. Akantheni adani anga onse pa msagwada; gululani mano a anthu oyipa.
8 Pie Tā Kunga ir pestīšana! Tava svētība pār Taviem ļaudīm! (Sela)
Chipulumutso chimachokera kwa Yehova. Madalitso akhale pa anthu anu. (Sela)