< Psalmi 12 >
1 Dāvida dziesma, dziedātāju vadonim uz astoņām stīgām. Palīdz, ak Kungs! Jo svētie ir zustin zuduši, un ticīgo ir maz starp cilvēku bērniem.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide. Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika; okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
2 Tie runā nelietību ikviens ar savu tuvāko; lūpām smaidīdami, ar divējādu sirdi tie runā.
Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
3 Lai Tas Kungs izdeldē visu liekulību, to mēli, kas runā lielību,
Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo ndi pakamwa paliponse podzikuza.
4 Kas saka: mēs pārvarēsim ar savu mēli, mūsu mute ir ar mums; kas mums ir par kungu?
Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu; pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
5 Tad nu nabagu postīšanas dēļ un bēdīgo nopūšanās dēļ Es celšos, saka Tas Kungs: Es došu pestīšanu tam, kas pēc tās ilgojās.
“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu ndi kubuwula kwa anthu osowa, Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova, “Ndidzawateteza kwa owazunza.”
6 Tā Kunga vārdi ir šķīsti vārdi, kā sudrabs mālu traukā kausēts un septiņkārt šķīstīts.
Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri.
7 Kaut Tu, ak Kungs, tos gribētu pasargāt, kaut Tu mūs gribētu paglabāt no šīs cilts mūžīgi.
Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
8 Bezdievīgie lepni staigā visapkārt, kur netiklība augsti ceļas starp cilvēku bērniem.
Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.