< Psalmi 112 >

1 Alleluja! Svētīgs ir tas vīrs, kas To Kungu bīstas, kam pie Viņa baušļiem labs prāts.
Tamandani Yehova. Wodala munthu amene amaopa Yehova, amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
2 Tā dzimums būs varens virs zemes; taisno cilts taps svētīta.
Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
3 Padoms un bagātība ir viņa namā, un viņa taisnība pastāv mūžīgi.
Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Taisniem tumsībā aust gaišums; jo Viņš ir žēlīgs, sirds žēlīgs un taisns.
Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima; wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
5 Labi tam cilvēkam, kas apžēlojās un aizdod, tiesā tas savu lietu vedīs galā.
Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
6 Jo tas nešaubīsies ne mūžam; taisnais paliks mūžīgā piemiņā.
Ndithu sadzagwedezeka; munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
7 No ļaunas slavas tas nebīstas viņa sirds ir stipra un paļaujas uz To Kungu.
Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
8 Viņa sirds ir droša un nebīstas; tiekams ar prieku skatās uz saviem pretiniekiem.
Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
9 Viņš izdala un dod nabagiem; viņa taisnība paliek mūžīgi, viņa rags top paaugstināts ar godu.
Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya; nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
10 Bezdievīgais to redzēs un apskaitīsies, viņš sakodīs savus zobus un iznīks; ko bezdievīgie kāro, ies bojā.
Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.

< Psalmi 112 >