< Nechemijas 7 >
1 Kad nu mūris bija uztaisīts, tad es iecēlu durvis, un vārtu sargi un dziedātāji un leviti tapa iecelti,
Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
2 Un es pavēlēju savam brālim Hananum un Hananijam, Jeruzālemes pils virsniekam, (jo tas bija uzticams vīrs un dievbijīgs pār daudziem),
Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
3 Un uz tiem sacīju: Lai Jeruzālemes vārti netop atdarīti, pirms saule nesilda, un tiem vēl klāt esot durvis lai atkal aizslēdz un aizšauj. Un Jeruzālemes iedzīvotājus ieceļat par sargiem, ikkatru uz savu vakti un ikkatru savam namam pretim.
Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
4 Bet pilsēta bija plata un liela un ļaužu tur bija maz un nami nebija uzcelti,
Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
5 Tad mans Dievs man iedeva sirdī, sapulcināt virsniekus un priekšniekus un tos ļaudis, lai sarakstītu radu rakstus. Un es atradu vienu radu rakstu grāmatu par tiem, kas pirmie bija pārnākuši, un es atradu, ka tur tā bija rakstīts:
Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
6 Šie ir tie valsts bērni, kas bija pārnākuši no tā cietuma, kur NebukadNecars, Bābeles ķēniņš, tos bija aizvedis, un kas ir griezušies atpakaļ uz Jeruzālemi un uz Jūdu, ikviens savā pilsētā;
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
7 Kas nākuši ar Zerubabeli, ar Ješuū, Nehemiju, Azariju, Raāmiju, Naēmanu, Mordohaju, Bilšanu, Mizperetu, Biģevaju, Neūmu, Baēnu. Šis ir Israēla vīru skaits.
Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
8 Pareūs bērni bija divtūkstoš simt septiņdesmit divi;
Zidzukulu za Parosi 2,172
9 Zeroatijas bērni: trīssimt septiņdesmit divi;
Zidzukulu za Sefatiya 372
10 Arus bērni: sešsimt piecdesmit divi;
Zidzukulu za Ara 652
11 PaātMoaba bērni, no Ješuūs un Joaba bērniem: divtūkstoš astoņsimt astoņpadsmit;
Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
12 Elama bērni: tūkstoš divsimt piecdesmit četri;
Zidzukulu za Elamu 1,254
13 Zatus bērni: astoņsimt četrdesmit pieci;
Zidzukulu za Zatu 845
14 Zakajus bērni: septiņsimt sešdesmit;
Zidzukulu za Zakai 760
15 Banus bērni: sešsimt četrdesmit astoņi;
Zidzukulu za Binuyi 648
16 Bebajus bērni: sešsimt divdesmit astoņi;
Zidzukulu za Bebai 628
17 Azgada bērni: divtūkstoš trīssimt divdesmit divi;
Zidzukulu za Azigadi 2,322
18 Adonikama bērni: sešsimt sešdesmit septiņi;
Zidzukulu za Adonikamu 667
19 Biģevajus bērni: divtūkstoš sešdesmit septiņi;
Zidzukulu za Abigivai 2,067
20 Adina bērni: sešsimt piecdesmit pieci;
Zidzukulu za Adini 655
21 Atera bērni no Hizkijas (nama): deviņdesmit astoņi;
Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
22 Hašuma bērni: trīssimt divdesmit astoņi;
Zidzukulu za Hasumu 328
23 Becajus bērni: trīssimt divdesmit četri;
Zidzukulu za Bezayi 324
24 Ariva bērni: simts divpadsmit;
Zidzukulu za Harifu 112
25 Gibeona bērni: deviņdesmit pieci;
Zidzukulu za Gibiyoni 95.
26 Bētlemes un Netofas vīri: simts astoņdesmit astoņi;
Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
27 Anatotas vīri: simts divdesmit astoņi;
Anthu a ku Anatoti 128
28 BetAsmavetas vīri: četrdesmit divi;
Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
29 KiriatJearimas, Kaviras un Beērotas vīri: septiņsimt četrdesmit trīs;
Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
30 Rāmas un Gabas vīri: sešsimt divdesmit viens;
Anthu a ku Rama ndi Geba 621
31 Mikmasas vīri: simts divdesmit divi;
Anthu a ku Mikimasi 122
32 Bēteles un Ajas vīri: simts divdesmit trīs;
Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
33 Otra Nebus vīri: piecdesmit divi;
Anthu a ku Nebo winayo 52
34 Otra Elama bērni: tūkstoš divsimt piecdesmit četri;
Ana a Elamu wina 1,254
35 Harima bērni: trīssimt divdesmit;
Zidzukulu za Harimu 320
36 Jērikus bērni: trīssimt četrdesmit pieci;
Zidzukulu za Yeriko 345
37 Lodas, Adidas un Onus bērni: septiņsimt divdesmit viens;
Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
38 Zenaūs bērni: trīstūkstoš deviņsimt trīsdesmit.
Zidzukulu za Senaya 3,930.
39 Priesteri: Jedajas bērni, no Ješuūs nama: deviņsimt septiņdesmit trīs;
Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
40 Imera bērni: tūkstoš piecdesmit divi;
Zidzukulu za Imeri 1,052
41 Pašhura bērni: tūkstoš divsimt četrdesmit septiņi;
Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
42 Harima bērni: tūkstoš septiņpadsmit.
Zidzukulu za Harimu 1,017.
43 Leviti: Ješuūs bērni no Kadmiēļa, no Odavijas bērniem: septiņdesmit četri.
Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
44 Dziedātāji, - Asafa bērni: simts četrdesmit astoņi.
Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
45 Vārtu sargi: Šaluma bērni, Atera bērni, Talmona bērni, Akuba bērni, Atita bērni, Zobaja bērni: simts trīsdesmit astoņi.
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
46 Dieva nama kalpotāji: Cikus bērni, Azuva bērni, Tabaota bērni,
Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
47 Ķerus bērni, Ziūs bērni, Padona bērni,
Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
48 Lebana bērni, Agaba bērni, Zalmajus bērni,
Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
49 Anana bērni, Ģideļa bērni, Gaāra bērni.
Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
50 Reajus bērni, Recina bērni, Nekoda bērni,
Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
51 Gazama bērni, Uzus bērni, Paseūs bērni,
Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
52 Besajus bērni, Meūnima bērni, Nevusima bērni,
Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
53 Bakbuka bērni, Akuva bērni, Arura bērni,
Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
54 Baceluta bērni, Mekida bērni, Arsas bērni,
Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
55 Barkus bērni, Sisera bērni, Tamus bērni,
Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
56 Necius bērni, Ativus bērni,
Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
57 Salamana kalpu bērni, Sotajus bērni, Sofereta bērni, Pridus bērni,
Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
58 Jaēlus bērni, Darkona bērni, Ģideļa bērni,
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
59 Šefatijas bērni, Atila bērni, Poķereta bērni no Cebaīm, Amona bērni,
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
60 Dieva nama kalpotāju un Salamana kalpu bērnu bija pavisam trīssimt deviņdesmit divi.
Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
61 Un šie pārnāca līdz no TelMelakas, TelArzus, Ķeruba, Adona, Imera. Bet tie sava tēva namu un savu dzimumu nevarēja pierādīt, vai tie bija no Israēla.
Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
62 Delajas bērni, Tobijas bērni, Nekoda bērni: sešsimt četrdesmit divi.
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
63 Un no priesteriem: Abajus bērni, Akoca bērni, Barzilajus bērni, kas no Barzilajus, tā Gileādieša, meitām sievu bija ņēmis, un pēc viņa vārda bija nosaukts.
Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
64 Šie savus radu rakstus meklēja bet neatrada; tāpēc tie no priestera amata tapa atmesti.
Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
65 Un zemes soģis uz tiem sacīja: lai neēd no tā vissvētākā, tiekams priesteris celtos ar urim un tumim.
Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
66 Visa šī draudze bija kopā: četrdesmit divi tūkstoši trīssimt sešdesmit,
Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
67 Bez kalpiem un kalponēm, - šo bija septiņtūkstoš trīssimt trīsdesmit septiņi. Un tiem bija divsimt četrdesmit pieci dziedātāji un dziedātājas.
Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
68 Viņu zirgu bija septiņsimt trīsdesmit seši, viņu zirgēzeļu divsimt četrdesmit pieci,
Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
69 Kamieļu četrsimt trīsdesmit pieci, ēzeļu seštūkstoš septiņsimt divdesmit.
Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
70 Un no cilts virsniekiem šie deva ko pie tā darba: zemes soģis piemeta pie tās mantas tūkstoš zelta gabalus, piecdesmit bļodas un piecsimt trīsdesmit priesteru svārkus.
Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
71 Un no cilts virsniekiem piemeta pie tās mantas uz to darbu divdesmit tūkstoš zelta gabalus un divtūkstoš divsimt mārciņas sudraba.
Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
72 Un ko tie citi ļaudis meta, tas bija divdesmit tūkstoš zelta gabali un divtūkstoš mārciņas sudraba un sešdesmit septiņi priesteru svārki.
Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
73 Un priesteri un leviti un vārtu sargi un dziedātāji un tie ļaudis un tie Dieva nama kalpotāji un viss Israēls dzīvoja savās pilsētās.
Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.