< Psalmorum 2 >

1 psalmus David quare fremuerunt gentes et populi meditati sunt inania adstiterunt reges terrae et principes convenerunt in unum adversus Dominum et adversus christum eius diapsalma
Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 disrumpamus vincula eorum et proiciamus a nobis iugum ipsorum
Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
3 qui habitat in caelis inridebit eos et Dominus subsannabit eos
Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
4 tunc loquetur ad eos in ira sua et in furore suo conturbabit eos
Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 ego autem constitutus sum rex ab eo super Sion montem sanctum eius praedicans praeceptum eius
Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 Dominus dixit ad me filius meus es tu ego hodie genui te
“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 postula a me et dabo tibi gentes hereditatem tuam et possessionem tuam terminos terrae
Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
8 reges eos in virga ferrea tamquam vas figuli confringes eos
Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 et nunc reges intellegite erudimini qui iudicatis terram
Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 servite Domino in timore et exultate ei in tremore
Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 adprehendite disciplinam nequando irascatur Dominus et pereatis de via iusta
Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 cum exarserit in brevi ira eius beati omnes qui confidunt in eo
Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.

< Psalmorum 2 >